< Eyüp 25 >
1 Şuahlı Bildat şöyle yanıtladı:
Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
2 “Egemenlik ve heybet Tanrı'ya özgüdür, Yüce göklerde düzen kuran O'dur.
“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
3 Orduları sayılabilir mi? Işığı kimin üzerine doğmaz?
Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
4 İnsan Tanrı'nın önünde nasıl doğru olabilir? Kadından doğan biri nasıl temiz olabilir?
Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
5 O'nun gözünde ay parlak, Yıldızlar temiz değilse,
Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
6 Nerede kaldı bir kurtçuk olan insan, Bir böcek olan insanoğlu!”
nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”