< Yeşaya 20 >

1 Asur ordusunun başkomutanı, Asur Kralı Sargon'un buyruğuyla gelerek Aşdot'a saldırıp kenti ele geçirdiği yıl RAB Amots oğlu Yeşaya aracılığıyla şöyle dedi: “Git, belindeki çulu çöz, ayağındaki çarığı çıkar.” Yeşaya denileni yaptı, çıplak ve yalınayak dolaşmaya başladı.
Mʼchaka chimene mkulu wankhondo wotumidwa ndi mfumu ya ku Asiriya, anabwera ku Asidodi ndi kuwuthira nkhondo ndi kuwulanda,
2
nthawi imeneyo Yehova anawuza Yesaya mwana wa Amozi kuti, “Pita kavule chiguduli ndi nsapato zako.” Ndipo iye anaterodi, ankangoyenda wamaliseche ndiponso wopanda nsapato.
3 RAB dedi ki, “Mısır'a ve Kûş'a belirti ve ibret olsun diye kulum Yeşaya nasıl üç yıl çıplak ve yalınayak dolaştıysa,
Kenaka Yehova anati, “Monga momwe mtumiki wanga Yesaya wakhala akuyendera wamaliseche ndiponso wopanda nsapato kwa zaka zitatu ngati chizindikiro ndi chenjezo kwa dziko la Igupto ndi Kusi,
4 Asur Kralı da Mısır'a utanç olsun diye Mısırlı tutsaklarla Kûşlu sürgünleri genç yaşlı demeden, çıplak ve yalınayak, mahrem yerleri açık yürütecek.
momwemonso mfumu ya ku Asiriya idzatenga ukapolo anthu a ku Igupto ndi a ku Kusi, anyamata ndi okalamba. Iwo adzakhala amaliseche ndi opanda nsapato, matako ali pa mtunda. Zimenezi zidzachititsa manyazi Igupto.
5 Kûş'a bel bağlayan, Mısır'la övünen halk hüsrana uğrayacak, utanç içinde kalacak.
Amene ankadalira Kusi, ndiponso amene ankadzitukumula chifukwa cha Igupto adzakhumudwa ndi kuchita manyazi.
6 Bu kıyı bölgesinde yaşayanlar o gün, “Asur Kralı'nın elinden kurtulmak için yardımına sığındığımız, bel bağladığımız ulusların başına gelene bakın!” diyecekler, “Biz nasıl kurtulacağız?”
Tsiku limenelo anthu amene amakhala mʼmbali mwa nyanja adzati, ‘Taonani zomwe zawachitikira amene ife tinkawadalira, amene ife tinkathawirako kuti atithandize ndi kutipulumutsa kwa mfumu ya ku Asiriya! Nanga ife tidzapulumuka bwanji?’”

< Yeşaya 20 >