< Psaltaren 122 >

1 En vallfartssång; av David. Jag gladdes, när man sade till mig: "Vi skola gå till HERRENS hus."
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
2 Våra fötter fingo träda in i dina portar, Jerusalem,
Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
3 Jerusalem, du nyuppbyggda stad, där hus sluter sig väl till hus,
Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
4 dit stammarna draga upp, HERRENS stammar, efter lagen för Israel, till att prisa HERRENS namn.
Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
5 Ty där äro ställda domarstolar, stolar för Davids hus.
Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
6 Önsken Jerusalem frid; ja, dem gånge väl, som älska dig.
Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
7 Frid vare inom dina murar, välgång i dina palats!
Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
8 För mina bröders och vänners skull vill jag tillsäga dig frid.
Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
9 För HERRENS, vår Guds, hus' skull vill jag söka din välfärd.
Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.

< Psaltaren 122 >