< Psaltaren 19 >

1 En Psalm Davids, till att föresjunga. Himlarna förtälja Guds äro, och fästet förkunnar hans händers verk.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Zakumwamba zimalengeza za ulemerero wa Mulungu; thambo limalalikira ntchito za manja ake.
2 En dag säger det dem andra, och en natt kungör det de andro.
Tsiku ndi tsiku zimayankhula mawu ambiri, usiku ndi usiku zimaonetsa poyera nzeru.
3 Intet mål eller tal är, der man deras röst icke hörer.
Palibe kuyankhula, palibe mawu aliwonse; liwu lawo silimveka.
4 Deras snöre går ut i all land, och deras tal intill verldenes ändar; han hafver gjort solene ena hyddo i dem;
Koma uthenga wawo umapita pa dziko lonse lapansi, mawuwo amafika mpaka kumalekezero a dziko lapansi.
5 Och hon går ut såsom en brudgumme utu sinom kammar, och fröjdar sig såsom en hjelte till att löpa vägen.
Dzuwa lili ngati mkwatibwi wobwera kuchokera ku nsanja yake, ngati katswiri wokondwerera kuthamanga pa mpikisano.
6 Hon går upp vid himmelens ända, och löper omkring åter till samma ändan; och intet blifver för hennes hetta förskyldt.
Limatuluka kuyambira mbali ina ya thambo ndi kuzungulira mpaka mbali inanso; palibe chinthu chotha kupewa kutentha kwake.
7 Herrans lag är utan vank, och vederqvicker själarna; Herrans vittnesbörd är visst, och gör de enfaldiga visa.
Lamulo la Yehova ndi langwiro, kutsitsimutsa moyo. Maumboni a Yehova ndi odalirika, amapereka nzeru kwa wopanda nzeru.
8 Herrans befallningar äro rätta, och fröjda hjertat; Herrans bud äro klar, och upplysa ögonen.
Malangizo a Yehova ndi olungama, amapereka chimwemwe mu mtima. Malamulo a Yehova ndi onyezimira, amapereka kuwala.
9 Herrans fruktan är ren, och blifver evinnerliga; Herrans rätter äro sanne, allesamman rättfärdige.
Kuopa Yehova ndiye chinthu changwiro, chimakhala mpaka muyaya. Maweruzo a Yehova ndi owona ndipo onse ndi olungama;
10 De äro kosteligare än guld, och mycket fint guld; de äro sötare än hannog, och hannogskaka.
ndi a mtengowapatali kuposa golide, kuposa golide weniweni; ndi otsekemera kuposa uchi, kuposa uchi wochokera pa chisa chake.
11 Ock varder din tjenare igenom dem förmanad; och den dem håller, han hafver stor lön.
Mtumiki wanu amachenjezedwa nawo; powasunga pali mphotho yayikulu.
12 Ho kan märka huru ofta han bryter? Förlåt mig mina hemliga brister.
Ndani angathe kudziwa zolakwa zake? Mundikhululukire zolakwa zanga zobisika.
13 Bevara ock din tjenare för de stolta, att de icke få råda öfver mig; så blifver jag utan vank, och oskyldig för stor missgerning.
Muteteze mtumiki wanunso ku machimo ochita akudziwa; iwo asandilamulire. Kotero ndidzakhala wosalakwa, wopanda mlandu wa tchimo lalikulu.
14 Låt dig täckas mins muns tal, och mins hjertans tankar för dig, Herre, min tröst och min förlossare.
Mawu a mʼkamwa mwanga ndi zolingalira za mu mtima mwanga zikhale zokondweretsa pamaso panu, Inu Yehova, Thanthwe langa ndi Mpulumutsi wanga.

< Psaltaren 19 >