< Job 21 >
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 Hörer dock till min ord, och låter säga eder;
“Mvetserani bwino mawu anga; ichi chikhale chitonthozo changa chochokera kwa inu.
3 Hafver tålamod med mig, att jag ock må tala; och görer sedan spott af mig.
Ndiloleni ndiyankhule ndipo ndikatha kuyankhula munditonzetonze.
4 Månn jag handla med en mennisko, att min ande icke skulle härutinnan ångse varda?
“Kodi ine ndikudandaulira munthu? Tsono ndilekerenji kupsa mtima?
5 Vänder eder hit till mig; I skolen förundra eder, och måsten lägga handena på munnen.
Ndipenyeni ndipo mudabwe; mugwire dzanja pakamwa.
6 När jag tänker deruppå, så förskräckes jag; och ett bäfvande kommer uppå mitt kött.
Ndikamaganiza zimenezi ndimachita mantha kwambiri; thupi langa limanjenjemera.
7 Hvi lefva då de ogudaktige, varda gamle, och växa till i ägodelar?
Chifukwa chiyani anthu oyipa amakhalabe ndi moyo, amakalamba ndi kusanduka amphamvu?
8 Deras säd är säker omkring dem, och deras afföda är när dem.
Amaona ana awo akukhazikika pamodzi nawo, zidzukulu zawo zikukula bwino iwo akuona.
9 Deras hus hafver frid för räddhåga, och Guds ris är icke öfver dem.
Mabanja awo amakhala pa mtendere ndipo sakhala ndi mantha; mkwapulo wa Mulungu suwakhudza nʼkomwe.
10 Deras oxa släpper man till, ock missgår icke; deras ko kalfvar, och är icke ofruktsam.
Ngʼombe zawo zazimuna sizilephera kubereketsa; ngʼombe zawo zazikazi sizipoloza.
11 Deras unga barn gå ut såsom en hjord, och deras barn springa.
Amatulutsa ana awo ngati gulu la nkhosa; makanda awo amavinavina pabwalo.
12 De fröjda sig med trummor och harpor, och äro glade med pipande;
Amayimba nyimbo pogwiritsa ntchito matambolini ndi azeze; amakondwa pakumva kulira kwa chitoliro.
13 De varda gamle med göda dagar, och förskräckas som nogast ett ögnablick för helvetet; (Sheol )
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol )
14 De dock säga till Gud: Gack bort ifrån oss; vi vilje intet veta af dina vägar;
Koma anthuwo amawuza Mulungu kuti, ‘Tichokereni!’ Ife tilibe chikhumbokhumbo chofuna kudziwa njira zanu.
15 Ho är den Allsmägtige, att vi honom tjena skole? Eller hvad kan det båta oss, om vi löpe emot honom?
Kodi Wamphamvuzonseyo ndani kuti timutumikire? Ife tipindula chiyani tikamapemphera kwa Iyeyo?
16 Men si, deras ägodelar stå icke uti deras händer; derföre skall de ogudaktigas sinne vara långt ifrå mig.
Komatu ulemerero wawo suli mʼmanja mwawo, koma ine ndimakhala patali ndi uphungu wa anthu oyipa.
17 Huru varder de ogudaktigas lykta utsläckt; och deras förderf kommer öfver dem? Han skall utskifta jämmer i sine vrede.
“Koma nʼkangati kamene nyale ya anthu oyipa imazimitsidwa? Nʼkangati kamene tsoka limawagwera? Nʼkangati kamene Mulungu amawakwiyira ndi kuwalanga?
18 De skola varda såsom strå för vädret, och såsom agnar, hvilka stormen bortförer.
Nʼkangati kamene iwo amakhala ngati phesi lowuluka ndi mphepo, ngati mungu wowuluzika ndi kamvuluvulu?
19 Gud förvarar hans barnom bedröfvelse; när han skall löna honom, då skall man förnimmat,
Paja amati, ‘Mulungu amalanga ana chifukwa cha machimo abambo awo.’ Koma Mulungu amabwezera chilango munthuyo, kuti adziwe kuti Mulungu amalangadi.
20 Hans ögon skola se hans förderf, och af dens Allsmägtigas vrede skall han dricka.
Mulole kuti adzionere yekha chilango chake, kuti alawe ukali wa Wamphamvuzonse.
21 Ty ho skall hafva behag till hans hus efter honom? Och hans månaders tal skall näppliga halft blifva.
Nanga kodi amalabadira chiyani zabanja lake limene walisiya mʼmbuyo, pamene chiwerengero cha masiku ake chatha?
22 Ho vill lära Gud, den ock dömer de höga?
“Kodi alipo wina amene angaphunzitse Mulungu nzeru, poti Iye amaweruza ngakhale anthu apamwamba?
23 Denne dör frisk och helbregda, rik och säll.
Munthu wina amamwalira ali ndi mphamvu zonse, ali pa mtendere ndi pa mpumulo,
24 Hans mjölkekar äro full med mjölk, och hans ben varda full med märg.
thupi lake lili lonenepa, mafupa ake ali odzaza ndi mafuta.
25 Men en annan dör med bedröfvada själ, och hafver aldrig ätit i glädje.
Munthu wina amamwalira ali wowawidwa mtima, wosalawapo chinthu chabwino chilichonse.
26 Och de ligga tillhopa med hvarannan i jordene, och matkar öfvertäcka dem.
Olemera ndi osauka omwe amamwalira ndi kuyikidwa mʼmanda ndipo onse amatuluka mphutsi.
27 Si, jag känner väl edra tankar, och edor vrånga anslag emot mig.
“Ndikudziwa bwino zimene mukuganiza, ziwembu zanu zomwe mukuti mundichitire.
28 Ty I sägen: Hvar är Förstans hus? Och hvar äro hyddorna, der de ogudaktige bodde?
Inu mukuti, ‘Kodi nyumba ya mkulu uja ili kuti, matenti amene munkakhala anthu oyipa aja ali kuti?’
29 Talen I dock derom såsom meniga folket; och veten icke hvad de andras väsende betyder?
Kodi munawafunsapo anthu amene ali pa ulendo? Kodi munaganizirapo zimene iwo amanena?
30 Ty den onde varder behållen intill förderfvelsens dag, och intill vredenes dag blifver han.
Zakuti munthu woyipa amasungidwa chifukwa cha tsiku la tsoka, kuti amapulumutsidwa chifukwa cha tsiku la ukali wa Mulungu?
31 Ho vill säga hvad han förtjenar, när man det utvärtes anser? Ho vill vedergälla honom hvad han gör?
Kodi ndani amadzudzula munthu wochimwayo? Ndani amamubwezera zoyipa zimene anachita?
32 Men han varder bortdragen till grafvena, och man vaktar efter honom i högomen.
Iye amanyamulidwa kupita ku manda ndipo anthu amachezera pa manda ake.
33 Bäckaslem behagar honom väl, och alla menniskor varda dragna efter honom; och uppå dem, som för honom varit hafva, är intet tal.
Dothi la ku chigwa limamukomera; anthu onse amatsatira mtembo wake, ndipo anthu osawerengeka amakhala patsogolo pa chitanda chakecho.
34 Huru trösten I mig så fåfängt, och edor svar finnas dock orätt?
“Nanga inu mudzanditonthoza bwanji ine ndi mawu anu opandapakewo palibe chimene chatsala kuti muyankhe koma mabodza basi!”