Aionian Verses

I zeszli się wszyscy synowie jego, i wszystkie córki jego, aby go cieszyli, lecz nie dał się cieszyć, ale mówił: Zaprawdę zstąpię za synem moim do grobu; i płakał go ojciec jego. (Sheol h7585)
Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol h7585)
Ale on rzekł: Nie pójdzie syn mój z wami, gdyż brat jego umarł, a on sam tylko został; a jeźliby nań przypadło co złego na drodze, którą pójdziecie, tedy doprowadzicie sędziwość moję z żałością do grobu. (Sheol h7585)
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol h7585)
A weźmiecieli i tego od oblicza mego, a przypadnie nań śmierć, tedy doprowadzicie sędziwość moję z żałością do grobu. (Sheol h7585)
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol h7585)
Stanie się, skoro ujrzy, iż dziecięcia nie będzie, że umrze; a odprowadzą słudzy twoi sędziwość sługi twego, ojca naszego, z żałością do grobu. (Sheol h7585)
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol h7585)
Ale jeźliż co nowego uczyni Pan, że otworzy ziemia usta swe, i pożre je i wszystkiego co mają, i zstąpią żywo do piekła, tedy poznacie, że rozdraźnili ci mężowie Pana. (Sheol h7585)
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol h7585)
I zstąpili oni ze wszystkiem co mieli, żywo do piekła, i okryła je ziemia, i poginęli z pośrodku zgromadzenia. (Sheol h7585)
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol h7585)
Albowiem ogień rozpalił się w popędliwości mojej, i będzie gorzał aż do najgłębszego piekła, i pożre ziemię, i urodzaj jej, i wypali grunty gór. (Sheol h7585)
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol h7585)
Pan zabija i ożywia, wwodzi do grobu i wywodzi. (Sheol h7585)
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol h7585)
Boleści grobu ogarnęły mię, zachwyciły mię sidła śmierci. (Sheol h7585)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
Uczynisz tedy według mądrości twojej, a nie dopuścisz zejść sędziwości jego w pokoju do grobu. (Sheol h7585)
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
Teraz jednak nie przepuszczaj mu tego, a iżeś jest mężem mądrym, będziesz wiedział, co mu masz uczynić, abyś wprowadził sędziwość jego ze krwią do grobu. (Sheol h7585)
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol h7585)
Jako niszczeje obłok i przemija, tak zstępujący do grobu nie wynijdzie; (Sheol h7585)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol h7585)
Wyższe są niż niebiosa, cóż uczynisz? Głębsze niż piekło, jakoż poznasz? (Sheol h7585)
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol h7585)
Obyżeś mię w grobie ukrył i utaił, ażby się uciszył gniew twój, a iżbyś mi zamierzył kres, kędy chcesz wspomnieć na mię! (Sheol h7585)
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol h7585)
Jeźlibym czego oczekiwał, grób będzie domem moim, a w ciemnościach uścielę łoże moje. (Sheol h7585)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
W głębię grobu zstąpię, ponieważ w prochu spólny odpoczynek wszystkich. (Sheol h7585)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)
Trawią w dobrem dni swoje, a we mgnieniu oka do grobu zstępują. (Sheol h7585)
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
Jako susza i gorącość trawią wody śnieżne, tak grób grzeszników. (Sheol h7585)
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol h7585)
Odkryte są przepaści przed nim, a nie ma przykrycia zatracenie. (Sheol h7585)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
Albowiem w śmierci niemasz pamiątki o tobie, a w grobie któż cie wyznawać będzie? (Sheol h7585)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol h7585)
Niepobożni się obrócą do piekła, wszystkie narody, które zapominają Boga. (Sheol h7585)
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol h7585)
Bo nie zostawisz duszy mojej w grobie, ani dopuścisz świętemu twemu oglądać skażenia. (Sheol h7585)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
Boleści grobu ogarnęły mię były, zachwyciły mię sidła śmierci. (Sheol h7585)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
Panie! wywiodłeś z piekła duszę moję; zachowałeś mię przy żywocie, abym nie zstąpił do grobu. (Sheol h7585)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol h7585)
Panie! niech nie będę pohańbiony, ponieważ cię wzywam; niech się zawstydzą niezbożni, i zamilkną w grobie. (Sheol h7585)
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol h7585)
Jako owce w grobie złożeni będą, śmierć ich strawi; ale sprawiedliwi panować będą nad nimi z poranku, a kształt ich zniszczony będzie w grobie, gdy ustąpią z mieszkania swego. (Sheol h7585)
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol h7585)
Ale Bóg wykupi duszę moję z mocy grobu, gdy mię przyjmie. (Sela) (Sheol h7585)
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol h7585)
Oby ich śmierć z prędka załapiła, tak aby żywo zstąpili do piekła! albowiem złość jest w mieszkaniu ich, i w pośrodku ich. (Sheol h7585)
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol h7585)
Ponieważ miłosierdzie twoje wielkie jest nademną, a tyś wyrwał duszę moję z dołu głębokiego. (Sheol h7585)
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol h7585)
Bo nasycona jest utrapieniem dusza moja, a żywot mój przybliżył się aż do grobu. (Sheol h7585)
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol h7585)
Któż z ludzi tak żyć może, aby nie oglądał śmierci? któż wyrwie duszę swą z mocy grobu? (Sela) (Sheol h7585)
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol h7585)
Ogarnęły mię były boleści śmierci, a utrapienia grobu zjęły mię; ucisk i boleść przyszła na mię. (Sheol h7585)
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol h7585)
Jeźlibym wstąpił do nieba, jesteś tam; i jeźlibym sobie posłał w grobie, i tameś przytomny. (Sheol h7585)
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol h7585)
Jako gdyby kto rąbał i łupał drwa na ziemi, tak się rozlatują kości nasze aż do ust grobowych. (Sheol h7585)
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol h7585)
Pożremyż ich żywo, jako grób, a całkiem, jako zstępujących w dół; (Sheol h7585)
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol h7585)
Nogi jej zstępują do śmierci, a do piekła chód jej prowadzi. (Sheol h7585)
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol h7585)
Dom jej jest jako drogi piekielne, wiodące do gmachów śmierci. (Sheol h7585)
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol h7585)
Ale prostak nie wie, że tam są umarli, a ci, których wezwała, są w głębokościach grobu. (Sheol h7585)
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol h7585)
Piekło i zatracenie są przed Panem; jakoż daleko więcej serca synów ludzkich. (Sheol h7585)
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol h7585)
Drogę żywota rozumny ma ku górze, aby się uchronił piekła głębokiego. (Sheol h7585)
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol h7585)
Ty go bij rózgą, a duszę jego z piekła wyrwiesz. (Sheol h7585)
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol h7585)
Piekło i zatracenie nie mogą być nasycone; także i oczy ludzkie nasycić się nie mogą. (Sheol h7585)
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol h7585)
Grób, i żywot niepłodny, ziemia też nie bywa nasycona wodą, a ogień nie mówi: Dosyć. (Sheol h7585)
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol h7585)
Wszystko, co przedsięweźmie ręka twoja do czynienia, czyń według możności twojej, albowiem niemasz żadnej pracy, ani myśli, ani umiejętności, ani mądrości w grobie, do którego ty idziesz. (Sheol h7585)
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol h7585)
Przyłóż mię jako pieczęć na serce swoje, jako sygnet do ramienia swego! albowiem miłość mocna jest jako śmierć, twarda jako grób zawistna miłość; węgle jej jako węgle ogniste i jako płomień gwałtowny. (Sheol h7585)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol h7585)
Dlatego rozszerzyło piekło gardło swoje, a rozdarło nad miarę paszczękę swoję, i zstąpią do niego szlachta i pospólstwo jego, i zgiełk jego, i ci, którzy się weselą w niem. (Sheol h7585)
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol h7585)
Żądaj sobie znaku od Pana, Boga twego, bądź na dole nisko, bądź wysoko w górze. (Sheol h7585)
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol h7585)
I piekło ze spodku wzruszyło się dla ciebie, aby tobie przychodzącemu zaszło; wzbudziło dla ciebie umarłych, wszystkich książąt ziemi; rozkazało powstać z stolic swoich i wszystkim królom narodów. (Sheol h7585)
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol h7585)
Strącona jest do piekła, pycha twoja i dźwięk muzyki twojej; podesłanoć mole, a robaki cię przykrywają. (Sheol h7585)
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol h7585)
Wszakże strącon jesteś aż do piekła, w głębokość dołu. (Sheol h7585)
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol h7585)
Dlatego, że mówicie: Uczyniliśmy przymierze z śmiercią, i z piekłem mamy porozumienie, bicz gwałtowny nas nie dojdzie, gdy przechodzić będzie; bośmy położyli kłamstwo za ucieczkę swoję, a pod fałszem utailiśmy się; (Sheol h7585)
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol h7585)
A tak zgładzone będzie przymierze wasze z śmiercią, a porozumienie wasze z piekłem nie ostoi się; gdy bicz gwałtowny przechodzić będzie, będziecie od niego podeptani. (Sheol h7585)
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol h7585)
Jam rzekł w ukróceniu dni moich: Wnijdę do bram grobu, pozbawion będę ostatka lat swoich; (Sheol h7585)
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol h7585)
Albowiem nie grób wysławia cię, ani śmierć chwali cię, ani ci, którzy w dół wstępują, oczekują prawdy twojej. (Sheol h7585)
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol h7585)
Chodzisz i do króla, z olejkiem i z rozmaitemi wonnemi maściami twemi; posyłasz bowiem posłów swych daleko, a poniżasz się aż do grobu. (Sheol h7585)
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol h7585)
Tak mówi panujący Pan: Dnia, którego on zstąpił do grobu, uczyniłem lament, zawarłem dla niego przepaść, i zahamowałem strumienie jej, aby się zastanowiły wody wielkie; i uczyniłaem, że się zaćmił dla niego Liban, a wszystkie drzewa polne dla nie go zemdlały. (Sheol h7585)
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol h7585)
Od grzmotu upadku jego zatrwożyłem narody, gdym go wepchnął do grobu z tymi, co w dół zstępują, nad czem się ucieszyły na ziemi na dole wszystkie drzewa Eden, i co jest najwyborniejszego, i najlepszego na Libanie, i wszystko, co jest opojone wodą. (Sheol h7585)
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol h7585)
I ci z nim zstąpili do grobu, do pobitych mieczem, którzy byli ramieniem jego, i którzy siadali w cieniu jego w pośrodku narodów. (Sheol h7585)
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol h7585)
Mówić do niego będą najmocniejsi z mocarzów z pośrodku grobu z pomocnikami jego, którzy tam zstąpiwszy, leżą z nieobrzezańcami pobitymi mieczem. (Sheol h7585)
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol h7585)
Aczkolwiekci jeszcze nie polegli z mocarzami, którzy upadli z nieobrzezańców, co zstąpili do grobu z wojennym orężem swoim, i położyli miecze swe pod głowy swe; a wszakże przyjdzie nieprawość ich na kości ich, chociaż strach tych mocarzów był w ziemi żyjących. (Sheol h7585)
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol h7585)
Z ręki grobu wybawię ich, od śmierci wykupię ich. O śmierci! będę śmiercią twoją; o grobie! będę skażeniem twojem; żałość skryta będzie od oczów moich. (Sheol h7585)
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol h7585)
Choćby się zakopali w ziemię, i stamtądby ich ręka moja wzięła; choćby wstąpili aż do nieba, i stamtądby ich stargnął. (Sheol h7585)
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol h7585)
I rzekł: Wołałem z ucisku swego do Pana, a ozwał mi się; z głębokości grobu wołałem, a wysłuchałeś głos mój. (Sheol h7585)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol h7585)
Dopieroż człowiek opiły, przewrotny i hardy nie ostoi się w mieszkaniu swojem, który rozszerza jako piekło duszę swoję, a jest jako śmierć, która się nie może nasycić, choćby zgromadził do siebie wszystkie narody, a zebrał do siebie wszystkich lud zi. (Sheol h7585)
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol h7585)
Ale ja wam powiadam: Iż każdy, kto się gniewa na brata swego bez przyczyny, będzie winien sądu; a ktokolwiek rzecze bratu swemu: Racha; będzie winien rady, a ktokolwiek rzecze: Błaźnie! będzie winien ognia piekielnego. (Geenna g1067)
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna g1067)
Jeźli cię tedy oko twoje prawe gorszy, wyłup je, a zarzuć od siebie; albowiem pożyteczniej jest tobie, aby zginął jeden z członków twoich, a wszystko ciało twoje nie było wrzucone do ognia piekielnego. (Geenna g1067)
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
A jeźliż cię prawa ręka twoja gorszy, odetnij ją, i zarzuć od siebie; albowiem pożyteczniej jest tobie, aby zginął jeden z członków twoich, a wszystko ciało twoje nie było wrzucone do ognia piekielnego. (Geenna g1067)
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
A nie bójcie się tych, którzy zabijają ciało, lecz duszy zabić nie mogą; ale raczej bójcie się tego, który może i duszę i ciało zatracić w piekielnym ogniu. (Geenna g1067)
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna g1067)
A ty Kapernaum! któreś aż do nieba wywyższone, aż do piekła strącone będziesz; bo gdyby się były w Sodomie te cuda działy, które się działy w tobie, zostałaby była aż do dnia dzisiejszego. (Hadēs g86)
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs g86)
I ktobykolwiek rzekł słowo przeciwko Synowi człowieczemu, będzie mu odpuszczono; ale kto by mówił przeciwko Duchowi Świętemu, nie będzie mu odpuszczono, ani w tym wieku ani w przyszłym. (aiōn g165)
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn g165)
A między ciernie posiany, ten jest, który słucha słowa; ale pieczołowanie świata tego i omamienie bogactw zadusza słowo, i staje się bez pożytku. (aiōn g165)
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn g165)
Nieprzyjaciel zasię, który go rozsiał, jestci dyjabeł, a żniwo jest dokonanie świata, a żeńcy są Aniołowie. (aiōn g165)
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn g165)
Jako tedy zbierają kąkol, a palą go ogniem, tak będzie przy dokonaniu świata tego. (aiōn g165)
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn g165)
Takci będzie przy dokonaniu świata; wynijdą Aniołowie, i wyłączą złe z pośrodku sprawiedliwych, (aiōn g165)
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn g165)
A Ja ci też powiadam, żeś ty jest Piotr; a na tej opoce zbuduję kościół mój, a bramy piekielne nie przemogą go: (Hadēs g86)
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs g86)
Przetoż jeźli ręka twoja albo noga twoja gorszy cię, odetnij ją i zarzuć od siebie; lepiej jest tobie wnijść do żywota chromym albo ułomnym, niżeli dwie ręce albo dwie nogi mając, wrzuconym być do ognia wiecznego. (aiōnios g166)
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios g166)
A jeźli cię oko twoje gorszy, wyłup je i zarzuć od siebie; lepiej jest tobie jednookim wnijść do żywota, niżeli oba oczy mając, być wrzuconym do ognia piekielnego. (Geenna g1067)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna g1067)
A oto jeden przystąpiwszy, rzekł mu: Nauczycielu dobry! co dobrego mam czynić, abym miał żywot wieczny? (aiōnios g166)
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios g166)
A każdy, kto by opuścił domy, albo braci, albo siostry, albo ojca, albo matkę, albo żonę, albo dzieci, albo rolę, dla imienia mego, stokroć więcej weźmie, i żywot wieczny odziedziczy. (aiōnios g166)
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios g166)
I ujrzawszy jedno figowe drzewo przy drodze, przyszedł do niego, i nie znalazł nic na niem, tylko same liście, i rzekł mu: Niechaj się więcej z ciebie owoc nie rodzi na wieki. I uschło zarazem one figowe drzewo. (aiōn g165)
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn g165)
Biada wam, nauczeni w Piśmie i Faryzeuszowie obłudni! iż obchodzicie morze i ziemię, abyście uczynili jednego nowego Żyda; a gdy się stanie, czynicie go synem zatracenia, dwakroć więcej niżeliście sami. (Geenna g1067)
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna g1067)
Wężowie! rodzaju jaszczurczy! i jakoż będziecie mogli ujść przed sądem ognia piekielnego? (Geenna g1067)
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna g1067)
A gdy siedział na górze oliwnej, przystąpili do niego uczniowie osobno, mówiąc: Powiedz nam, kiedy się to stanie, i co za znak przyjścia twego i dokonania świata? (aiōn g165)
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn g165)
Potem rzecze i tym, którzy będą po lewicy: Idźcie ode mnie, przeklęci! w ogień wieczny, który zgotowany jest dyjabłu i Aniołom jego. (aiōnios g166)
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios g166)
I pójdą ci na męki wieczne; ale sprawiedliwi do żywota wiecznego. (aiōnios g166)
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios g166)
Ucząc je przestrzegać wszystkiego, com wam przykazał. A oto Jam jest z wami po wszystkie dni, aż do skończenia świata. Amen. (aiōn g165)
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn g165)
Ale kto bluźni przeciwko Duchowi Świętemu, nie ma odpuszczenia na wieki, ale winien jest sądu wiecznego. (aiōn g165, aiōnios g166)
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
Ale pieczołowanie świata tego i omamienie bogactw, i pożądliwości innych rzeczy, wszedłszy zaduszają słowo, i staje się bez pożytku. (aiōn g165)
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn g165)
A jeźliby cię gorszyła ręka twoja, odetnij ją; bo lepiej jest tobie ułomnym wnijść do żywota, niżeli dwie ręce mając, iść do piekła w on ogień nieugaszony, (Geenna g1067)
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna g1067)
A jeźliby cię noga twoja gorszyła, odetnij ją; bo lepiej tobie chromym wnijść do żywota, niżeli dwie nogi mając, być wrzuconym do piekła, w ogień nieugaszony, (Geenna g1067)
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna g1067)
A jeźliby cię oko twoje gorszyło, wyłup je; bo lepiej tobie jednookim wnijść do królestwa Bożego, niżeli dwoje oczu mając, wrzuconym być do ognia piekielnego. (Geenna g1067)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna g1067)
A gdy on wychodził w drogę, przybieżał jeden, i upadłszy przed nim na kolana, pytał go: Nauczycielu dobry! cóż czynić mam, abym odziedziczył żywot wieczny? (aiōnios g166)
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Żeby nie miał wziąć stokrotnie teraz w tym czasie domów, i braci, i sióstr, i matek, i dzieci, i ról z prześladowaniem, a w przyszłym wieku żywota wiecznego. (aiōn g165, aiōnios g166)
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn g165, aiōnios g166)
A odpowiadając Jezus, rzekł mu: Niechajże więcej na wieki nikt z ciebie owocu nie je. A słyszeli to uczniowie jego. (aiōn g165)
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn g165)
I będzie królował nad domem Jakóbowym na wieki, a królestwu jego nie będzie końca. (aiōn g165)
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn g165)
Jako mówił do ojców naszych, do Abrahama i nasienia jego na wieki. (aiōn g165)
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn g165)
Tak jako mówił przez usta świętych proroków swoich, którzy byli od wieku: (aiōn g165)
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn g165)
Tedy go prosili, aby im nie rozkazywał stamtąd odejść w przepaść. (Abyssos g12)
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos g12)
A ty, Kapernaum! któreś aż do nieba wywyższone, aż do piekła strącone będziesz. (Hadēs g86)
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs g86)
A oto niektóry zakonnik powstał, kusząc go i mówiąc: Nauczycielu! co czyniąc odziedziczę żywot wieczny? (aiōnios g166)
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Ale wam okażę, kogo się bać macie: Bójcie się tego, który, gdy zabije, ma moc wrzucić do piekielnego ognia; zaiste powiadam wam, tego się bójcie. (Geenna g1067)
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna g1067)
I pochwalił pan szafarza niesprawiedliwego, iż roztropnie uczynił; bo synowie tego świata roztropniejsi są nad syny światłości w rodzaju swoim. (aiōn g165)
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn g165)
I jać wam powiadam: Czyńcie sobie przyjacioły z mammony niesprawiedliwości, aby gdy ustaniecie, przyjęli was do wiecznych przybytków. (aiōnios g166)
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios g166)
A będąc w piekle, podniósłszy oczy swe, gdy był w mękach, ujrzał Abrahama z daleka, i Łazarza na łonie jego. (Hadēs g86)
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs g86)
I pytał go niektóry książę, mówiąc: Nauczycielu dobry! co czyniąc odziedziczę żywot wieczny? (aiōnios g166)
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Aby nie wziął daleko więcej w tym czasie, a w przyszłym wieku żywota wiecznego. (aiōn g165, aiōnios g166)
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
Tedy odpowiadając, rzekł im Jezus: Synowie tego wieku żenią się i za mąż wydają. (aiōn g165)
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn g165)
Ale ci, którzy godni są, aby dostąpili onego wieku, i powstaną od umarłych, ani się żenić, ani za mąż dawać będą. (aiōn g165)
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn g165)
Aby każdy, kto weń wierzy, nie zginął, ale miał żywot wieczny. (aiōnios g166)
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Albowiem tak Bóg umiłował świat, że Syna swego jednorodzonego dał, aby każdy, kto weń wierzy, nie zginął, ale miał żywot wieczny. (aiōnios g166)
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Kto wierzy w Syna, ma żywot wieczny; ale kto nie wierzy Synowi, nie ogląda żywota, lecz gniew Boży zostaje nad nim. (aiōnios g166)
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios g166)
Lecz kto by pił onę wodę, którą ja mu dam, nie będzie pragnął na wieki; ale ta woda, którą ja mu dam, stanie się w nim studnią wody wyskakującej ku żywotowi wiecznemu. (aiōn g165, aiōnios g166)
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
A kto żnie, bierze zapłatę, i zbiera owoc do żywota wiecznego, aby i ten, który sieje, radował się wespół, i ten, który żnie. (aiōnios g166)
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios g166)
Zaprawdę, zaprawdę powiadam wam: Kto słowa mego słucha i wierzy onemu, który mię posłał, ma żywot wieczny i nie przyjdzie na sąd, ale przeszedł z śmierci do żywota. (aiōnios g166)
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios g166)
Badajcież się Pism; boć się wam zda, że w nich żywot wieczny macie, a one są, które świadectwo wydawają o mnie. (aiōnios g166)
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios g166)
Sprawujcież nie pokarm, który ginie, ale pokarm, który trwa ku żywotowi wiecznemu, który wam da Syn człowieczy; albowiem tego zapieczętował Bóg Ojciec. (aiōnios g166)
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios g166)
A tać jest wola onego, który mię posłał, aby każdy, kto widzi Syna, a wierzy weń, miał żywot wieczny; a ja go wzbudzę w on ostateczny dzień. (aiōnios g166)
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios g166)
Zaprawdę, zaprawdę powiadam wam: Kto w mię wierzy, ma żywot wieczny. (aiōnios g166)
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios g166)
Jamci jest chleb on żywy, którym z nieba zstąpił: jeźliby kto jadł z tego chleba, żyć będzie na wieki; a chleb, który ja dam, jest ciało moje, które ja dam za żywot świata. (aiōn g165)
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn g165)
Kto je ciało moje, a pije krew moję, ma żywot wieczny, a ja go wzbudzę w on ostateczny dzień. (aiōnios g166)
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios g166)
Tenci jest chleb on, który z nieba zstąpił, nie jako ojcowie wasi jedli mannę, a pomarli; kto je ten chleb, żyć będzie na wieki. (aiōn g165)
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn g165)
I odpowiedział mu Szymon Piotr: Panie! do kogóż pójdziemy? Ty masz słowa żywota wiecznego; (aiōnios g166)
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios g166)
A sługać nie mieszka w domu na wieki, ale Syn mieszka na wieki. (aiōn g165)
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn g165)
Zaprawdę, zaprawdę powiadam wam: Jeźli kto słowa moje zachowywać będzie, śmierci nie ogląda na wieki. (aiōn g165)
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn g165)
Tedy mu rzekli Żydowie: Terażeśmy poznali, że dyjabelstwo masz, Abraham umarł i prorocy, a ty powiadasz: Jeźli kto słowa moje zachowywać będzie, śmierci nie skosztuje na wieki; (aiōn g165)
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn g165)
Od wieku nie słyszano, aby kto otworzył oczy ślepo narodzonego. (aiōn g165)
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn g165)
A ja żywot wieczny daję im i nie zginą na wieki, ani ich żaden wydrze z ręki mojej. (aiōn g165, aiōnios g166)
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn g165, aiōnios g166)
A wszelki, który żyje, a wierzy w mię, nie umrze na wieki. Wierzyszże temu? (aiōn g165)
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn g165)
Kto miłuje duszę swoję, utraci ją, a kto nienawidzi duszy swojej na tym świecie, ku wiecznemu żywotowi strzeże jej. (aiōnios g166)
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios g166)
Odpowiedział mu on lud: Myśmy słyszeli z zakonu, iż Chrystus trwa na wieki; a jakoż ty mówisz, że musi być podwyższony Syn człowieczy? i któryż to jest Syn człowieczy? (aiōn g165)
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn g165)
I wiem, że rozkazanie jego jest żywot wieczny; przetoż to, co ja wam mówię, jako mi powiedział Ojciec, tak mówię. (aiōnios g166)
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios g166)
Rzekł mu Piotr: Nie będziesz ty nóg moich umywał na wieki. Odpowiedział mu Jezus: Jeźli cię nie umyję, nie będziesz miał cząstki ze mną. (aiōn g165)
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn g165)
A ja prosić będę Ojca, a innego pocieszyciela da wam, aby z wami mieszkał na wieki, (aiōn g165)
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn g165)
Jakoś mu dał moc nad wszelkiem ciałem, aby tym wszystkim, któreś mu dał, dał żywot wieczny. (aiōnios g166)
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios g166)
A toć jest żywot wieczny, aby cię poznali samego prawdziwego Boga, i któregoś posłał, Jezusa Chrystusa. (aiōnios g166)
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios g166)
Albowiem nie zostawisz duszy mojej w piekle, a nie dasz świętemu twojemu oglądać skażenia. (Hadēs g86)
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs g86)
To przeglądając, powiedział o zmartwychwstaniu Chrystusowem, iż nie została dusza jego w piekle, ani ciało jego widziało skażenia. (Hadēs g86)
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs g86)
Który zaiste niebiosa ma objąć aż do czasu naprawienia wszystkich rzeczy, co był przepowiedział Bóg przez usta wszystkich świętych swoich proroków od wieków. (aiōn g165)
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn g165)
A Paweł i Barnabasz, bezpiecznie mówiąc, rzekli: Wamci najpierwej miało być opowiadane słowo Boże; ale ponieważ je odrzucacie, a sądzicie się być niegodnymi żywota wiecznego, oto się obracamy do pogan. (aiōnios g166)
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios g166)
A słysząc to poganie, radowali się i wielbili słowo Pańskie, i uwierzyli, ilekolwiek ich było sporządzonych do żywota wiecznego. (aiōnios g166)
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios g166)
Znajomeć są Bogu od wieku wszystkie sprawy jego. (aiōn g165)
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn g165)
Bo rzeczy jego niewidzialne od stworzenia świata, przez rzeczy uczynione widzialne bywają, to jest ona wieczna jego moc i bóstwo, na to, aby oni byli bez wymówki. (aïdios g126)
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios g126)
Jako te, którzy odmienili prawdę Bożą w kłamstwo i chwalili stworzenie, i służyli mu raczej niż Stworzycielowi, który jest błogosławiony na wieki. Amen. (aiōn g165)
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Tym, którzy przez wytrwanie w uczynku dobrym szukają sławy i czci i nieskazitelności, odda żywot wieczny; (aiōnios g166)
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios g166)
Aby jako grzech królował ku śmierci, tak też aby łaska królowała przez sprawiedliwość ku żywotowi wiecznemu przez Jezusa Chrystusa, Pana naszego. (aiōnios g166)
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios g166)
Lecz teraz, będąc uwolnieni od grzechu, a zniewoleni Bogu, macie pożytek swój ku poświęceniu, a koniec żywot wieczny. (aiōnios g166)
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Albowiem zapłata za grzech jest śmierć; ale dar z łaski Bożej jest żywot wieczny, w Chrystusie Jezusie, Panu naszym. (aiōnios g166)
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios g166)
Których są ojcowie i z których poszedł Chrystus ile według ciała, który jest nad wszystkimi Bóg błogosławiony na wieki. Amen. (aiōn g165)
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
Albo kto zstąpi do przepaści? to jest Chrystusa od umarłych wyprowadzić. (Abyssos g12)
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos g12)
Albowiem zamknął je Bóg wszystkie w niedowiarstwo, aby się nad wszystkimi zmiłował. (eleēsē g1653)
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē g1653)
Albowiem z niego i przez niego i w nim są wszystkie rzeczy; jemu niech będzie chwała na wieki. Amen. (aiōn g165)
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
A nie przypodobywajcie się temu światu, ale się przemieńcie przez odnowienie umysłu waszego na to, abyście doświadczyli, która jest wola Boża dobra, przyjemna i doskonała. (aiōn g165)
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn g165)
A temu, który was może utwierdzić według Ewangielii mojej i opowiadania Jezusa Chrystusa, według objawienia tajemnicy od czasów wiecznych zamilczanej, (aiōnios g166)
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios g166)
Lecz teraz objawionej i przez Pisma prorockie według postanowienia wiecznego Boga ku posłuszeństwu wiary między wszystkimi narody oznajmionej; (aiōnios g166)
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios g166)
Temu, samemu mądremu Bogu niech będzie chwała przez Jezusa Chrystusa na wieki. Amen. (aiōn g165)
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn g165)
Gdzież jest mądry? Gdzież jest uczony w Piśmie? Gdzież badacz wieku tego? Izali w głupstwo nie obrócił Bóg mądrości świata tego? (aiōn g165)
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn g165)
A mądrość mówimy między doskonałymi; ale mądrość nie tego świata, ani książąt tego świata, którzy giną; (aiōn g165)
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn g165)
Ale mówimy mądrość Bożą w tajemnicy, która jest zakryta, którą Bóg przeznaczył przed wieki ku chwale naszej, (aiōn g165)
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn g165)
Której żaden z książąt tego świata nie poznał; bo gdyby byli poznali, nigdy by Pana chwały nie ukrzyżowali; (aiōn g165)
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn g165)
Niechajże nikt samego siebie nie zwodzi; jeźli się kto sobie zda być mądrym między wami na tym świecie, niech się stanie głupim, aby się stał mądrym. (aiōn g165)
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn g165)
Przeto, jeźli pokarm gorszy brata mego, nie będę jadł mięsa na wieki, abym brata mego nie zgorszył. (aiōn g165)
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn g165)
A te wszystkie rzeczy przydały się im za wzór, a napisane są dla napomnienia naszego, na których koniec świata przyszedł. (aiōn g165)
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn g165)
Gdzież jest, o śmierci! bodziec twój? Gdzież jest, piekło! zwycięstwo twoje? (Hadēs g86)
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs g86)
W których bóg świata tego oślepił zmysły, to jest w niewiernych, aby im nie świeciła światłość Ewangielii chwały Chrystusowej, który jest wyobrażeniem Bożem. (aiōn g165)
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn g165)
Albowiem ten króciuchny i lekki ucisk nasz nader zacnej chwały wieczną wagę nam sprawuje; (aiōnios g166)
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios g166)
Gdy nie patrzymy na rzeczy widzialne, ale na niewidzialne; albowiem rzeczy widzialne są doczesne, ale niewidzialne są wieczne. (aiōnios g166)
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios g166)
Wiemy bowiem, że jeźli tego naszego ziemskiego mieszkania namiot zburzony będzie, budowanie mamy od Boga, dom nie rękoma urobiony, wieczny w niebiesiech. (aiōnios g166)
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios g166)
Jako napisane: Rozproszył, dał ubogim, sprawiedliwość jego zostaje na wieki. (aiōn g165)
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn g165)
Bóg i Ojciec Pana naszego, Jezusa Chrystusa, który jest błogosławiony na wieki, wie, iż nie kłamię. (aiōn g165)
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn g165)
Który wydał samego siebie za grzechy nasze, aby nas wyrwał z teraźniejszego wieku złego według woli Boga i Ojca naszego; (aiōn g165)
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn g165)
Któremu niech będzie chwała na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Bo kto sieje ciału swemu, z ciała żąć będzie skażenie; ale kto sieje duchowi, z ducha żąć będzie żywot wieczny. (aiōnios g166)
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios g166)
Wysoko nad wszystkie księstwa i zwierzchności, i mocy, i państwa, i nad wszelkie imię, które się mianuje, nie tylko w tym wieku, ale i w przyszłym; (aiōn g165)
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn g165)
W którycheście niekiedy chodzili według zwyczaju świata tego i według książęcia, który ma władzę na powietrzu, ducha tego, który teraz jest skuteczny w synach niedowiarstwa. (aiōn g165)
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn g165)
Aby okazał w przyszłych wiekach ono nader obfite bogactwo łaski swojej, z dobrotliwości swojej przeciwko nam w Chrystusie Jezusie. (aiōn g165)
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn g165)
A iżbym objaśnił wszystkim, jaka by była społeczność onej tajemnicy zakrytej od wieków w Bogu, który wszystko stworzył przez Jezusa Chrystusa; (aiōn g165)
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn g165)
Według postanowienia wiecznego, które uczynił w Chrystusie Jezusie, Panu naszym, (aiōn g165)
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn g165)
Temu niech będzie chwała w kościele przez Chrystusa Jezusa po wszystkie czasy na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Albowiem nie mamy boju przeciwko krwi i ciału, ale przeciwko księstwom, przeciwko zwierzchnościom, przeciwko dzierżawcom świata ciemności wieku tego, przeciwko duchownym złościom, które są wysoko. (aiōn g165)
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn g165)
A Bogu i Ojcu naszemu niech będzie chwała na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
To jest, tajemnicę onę, która była zakryta od wieków i od rodzajów, ale teraz objawiona jest świętym jego. (aiōn g165)
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn g165)
Którzy pomstę odniosą, wieczne zatracenie od obliczności Pańskiej i od chwały mocy jego. (aiōnios g166)
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios g166)
A sam Pan nasz, Jezus Chrystus i Bóg a Ojciec nasz, który nas umiłował i dał pociechę wieczną, i nadzieję dobrą przez łaskę, (aiōnios g166)
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios g166)
Alem dlatego miłosierdzia dostąpił, aby na mnie pierwszym okazał Jezus Chrystus wszelką cierpliwość na przykład tym, którzy weń uwierzyć mają ku żywotowi wiecznemu. (aiōnios g166)
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios g166)
Przetoż królowi wieków nieśmiertelnemu, niewidzialnemu samemu mądremu Bogu, niech będzie cześć i chwała na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Bojuj on dobry bój wiary, chwyć się żywota wiecznego, do któregoś też powołany, i wyznałeś dobre wyznanie przed wieloma świadkami. (aiōnios g166)
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios g166)
Który sam ma nieśmiertelność i mieszka w światłości nieprzystępnej, którego nie widział żaden z ludzi, ani widzieć może; któremu niech będzie cześć i moc wieczna. Amen. (aiōnios g166)
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios g166)
Bogaczom w tym teraźniejszym wieku rozkaż, aby nie byli wysokomyślnymi, ani nadziei pokładali w bogactwie niepewnem, ale w Bogu żywym, który nam wszystkiego obficie ku używaniu dodaje: (aiōn g165)
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn g165)
Który nas zbawił i powołał powołaniem świętem, nie według uczynków naszych, ale według postanowienia swego i łaski, która nam jest dana w Chrystusie Jezusie przed czasy wiecznemi. (aiōnios g166)
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
Przetoż wszystko znoszę dla wybranych, aby i oni zbawienia dostąpili, które jest w Chrystusie Jezusie, z chwałą wieczną. (aiōnios g166)
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios g166)
Albowiem Demas mię opuścił, umiłowawszy ten świat, i poszedł do Tesaloniki, Krescens do Galacyi, Tytus do Dalmacyi; (aiōn g165)
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn g165)
A wyrwie mię Pan z każdego uczynku złego i zachowa do królestwa swego niebieskiego; któremu chwała na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn g165)
Ku nadziei żywota wiecznego, który obiecał przed czasy wiekuistemi ten, który nie kłamie, Bóg, a objawił czasów swoich, (aiōnios g166)
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
Ćwicząca nas, abyśmy odrzekłszy się niepobożności i świeckich pożądliwości, trzeźwie i sprawiedliwie, i pobożnie żyli na tym świecie, (aiōn g165)
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn g165)
Abyśmy usprawiedliwieni będąc łaską jego, stali się dziedzicami według nadziei żywota wiecznego. (aiōnios g166)
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios g166)
Albowiem snać dla tego odłączył się był na chwilę od ciebie, abyś go zaś miał wiecznie, (aiōnios g166)
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios g166)
W te dni ostateczne mówił nam przez Syna swego, którego postanowił dziedzicem wszystkich rzeczy, przez którego i wieki uczynił. (aiōn g165)
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn g165)
Ale do Syna mówi: Stolica twoja, o Boże! na wieki wieków; laska sprawiedliwości jest laska królestwa twego. (aiōn g165)
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn g165)
Jako i na inszem miejscu mówi: Tyś jest kapłanem na wieki według porządku Melchisedekowego. (aiōn g165)
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
A tak doskonałym będąc, stał się wszystkim sobie posłusznym przyczyną zbawienia wiecznego, (aiōnios g166)
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios g166)
Nauki o chrzcie i o wkładaniu rąk, i o powstaniu umarłych, i o sądzie wiecznym; (aiōnios g166)
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios g166)
Skosztowali też dobrego słowa Bożego i mocy przyszłego wieku, (aiōn g165)
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn g165)
Gdzie przewodnik dla nas wszedł, Jezus, stawszy się według porządku Melchisedekowego najwyższym kapłanem na wieki. (aiōn g165)
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn g165)
Albowiem tak świadczy: Tyś jest kapłanem na wieki według porządku Melchisedekowego. (aiōn g165)
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
Boć się oni bez przysięgi kapłanami stawali, a ten z przysięgą przez tego, który rzekł do niego: Przysiągł Pan, a nie będzie tego żałował: Tyś jest kapłanem na wieki według porządku Melchisedekowego, (aiōn g165)
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn g165)
Ale ten, iż na wieki zostaje, wieczne ma kapłaństwo, (aiōn g165)
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn g165)
Albowiem zakon ludzi podległych krewkości stanowił za najwyższych kapłanów: ale słowo przysięgi, które się stało po zakonie, postanowiło Syna Bożego doskonałego na wieki. (aiōn g165)
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn g165)
Ani przez krew kozłów i cielców, ale przez własną krew swoję wszedł raz do świątnicy, znalazłszy wieczne odkupienie. (aiōnios g166)
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios g166)
Jakoż daleko więcej krew Chrystusowa, który przez Ducha wiecznego samego siebie ofiarował nienaganionym Bogu, oczyści sumienie wasze od uczynków martwych ku służeniu Bogu żywemu? (aiōnios g166)
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios g166)
I dlatego jest nowego testamentu pośrednikiem, aby gdyby śmierć nastąpiła na odkupienie onych występków, które były pod pierwszym testamentem, ci którzy są powołani, wzięli obietnicę wiecznego dziedzictwa. (aiōnios g166)
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios g166)
(Bo inaczej musiałby był częstokroć cierpieć od początku świata), lecz teraz przy skończeniu wieków raz objawiony jest ku zgładzeniu grzechu przez ofiarowanie samego siebie. (aiōn g165)
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn g165)
Wiarą rozumiemy, iż świat jest sprawiony słowem Bożem, tak iż rzeczy, które widzimy, nie stały się z rzeczy widzialnych, ale z niczego. (aiōn g165)
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn g165)
Jezus Chrystus wczoraj i dziś, tenże i na wieki. (aiōn g165)
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn g165)
A Bóg pokoju, który wywiódł od umarłych we krwi przymierza wiecznego, onego wielkiego pasterza owiec, Pana naszego Jezusa, (aiōnios g166)
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios g166)
Niech was doskonałymi uczyni w każdym uczynku dobrym ku czynieniu woli swojej, sprawując w was to, co przyjemnego przed obliczem jego, przez Jezusa Chrystusa, któremu niech będzie chwała na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn g165)
I język jest ogień i świat niesprawiedliwości; takci jest postanowiony język między członkami naszemi, który szpeci wszystko ciało i zapala koło urodzenia naszego, i bywa zapalony od ognia piekielnego. (Geenna g1067)
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna g1067)
Odrodzeni będąc nie z nasienia skazitelnego, ale z nieskazitelnego przez słowo Boże żywe i trwające na wieki. (aiōn g165)
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn g165)
Ale słowo Pańskie trwa na wieki. A toć jest słowo, które wam jest zwiastowane. (aiōn g165)
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn g165)
Jeźli kto mówi, niech mówi jako wyroki Boże, jeźli kto posługuje, niech to czyni jako z siły, której Bóg dodaje, aby we wszystkiem chwalony był Bóg przez Jezusa Chrystusa, któremu należy chwała i panowanie na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
A Bóg wszelkiej łaski, który nas powołał do wiecznej chwały swojej w Chrystusie Jezusie, gdy maluczko ucierpicie, ten niech was doskonałymi uczyni, utwierdzi, umocni i ugruntuje; (aiōnios g166)
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios g166)
Jemu niech będzie chwała i panowanie na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
Tak bowiem hojnie wam dane będzie wejście do wiecznego królestwa Pana naszego i Zbawiciela, Jezusa Chrystusa. (aiōnios g166)
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios g166)
Albowiem jeźli Bóg Aniołom, którzy byli zgrzeszyli, nie przepuścił, ale strąciwszy ich do piekła, podał łańcuchom ciemności, aby byli zachowani na sąd: (Tartaroō g5020)
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō g5020)
Ale rośćcie w łasce i w znajomości Pana naszego i Zbawiciela, Jezusa Chrystusa, któremu niech będzie chwała i teraz, i na czasy wieczne. Amen. (aiōn g165)
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
(Bo żywot objawiony jest i widzieliśmy, i świadczymy i zwiastujemy wam on żywot wieczny, który był u Ojca, i objawiony nam jest.) (aiōnios g166)
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios g166)
Światci przemija i pożądliwość jego; ale kto czyni wolę Bożą, trwa na wieki. (aiōn g165)
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn g165)
A tać jest obietnica, którą on nam obiecał, to jest żywot on wieczny. (aiōnios g166)
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios g166)
Każdy, co nienawidzi brata swego, mężobójcą jest; a wiecie, iż żaden mężobójca nie ma żywota wiecznego w sobie zostawającego. (aiōnios g166)
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios g166)
A toć jest świadectwo, iż nam Bóg dał żywot wieczny; a ten żywot jest w Synu jego. (aiōnios g166)
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios g166)
Te rzeczy napisałem wam, którzy wierzycie w imię Syna Bożego, żebyście wiedzieli, iż macie żywot wieczny, i abyście wierzyli w imię Syna Bożego. (aiōnios g166)
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
A wiemy, iż Syn Boży przyszedł i dał nam zmysł, abyśmy poznali onego prawdziwego Boga, i jesteśmy w onym prawdziwym, to jest w Synu jego, Jezusie Chrystusie; tenci jest prawdziwy Bóg i żywot wieczny. (aiōnios g166)
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Dla prawdy, która zostaje w nas i z nami będzie na wieki. (aiōn g165)
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn g165)
Także Aniołów, którzy nie zachowali pierwszego stanu swego, ale opuścili mieszkanie swoje, na sąd dnia wielkiego związkami wiecznemi pod chmurą zachował. (aïdios g126)
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios g126)
Jako Sodoma i Gomorra, i okoliczne miasta, gdy tymże sposobem jako i one zwszeteczniały i udały się za cudzem ciałem, wystawione są na przykład, ognia wiecznego karanie ponosząc: (aiōnios g166)
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios g166)
Wały wściekłe morskie, wyrzucające swoje sprośności, gwiazdy błąkające się, którym chmura ciemności zachowana jest na wieki. (aiōn g165)
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn g165)
Samych siebie w miłości Bożej zachowajcie, oczekując miłosierdzia Pana naszego, Jezusa Chrystusa, ku żywotowi wiecznemu. (aiōnios g166)
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios g166)
Samemu mądremu Bogu, Zbawicielowi naszemu, niech będzie chwała i wielmożność, moc i zwierzchność, i teraz i po wszystkie wieki. Amen. (aiōn g165)
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
I uczynił nas królami i kapłanami Bogu, Ojcu swemu; jemuż niech będzie chwała i moc na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn g165)
I żyjący; a byłem umarły, a otom jest żywy na wieki wieków. I mam klucze piekła i śmierci. (aiōn g165, Hadēs g86)
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn g165, Hadēs g86)
A gdy one zwierzęta dawały chwałę i cześć, i dziękowanie siedzącemu na stolicy, żyjącemu na wieki wieków; (aiōn g165)
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn g165)
Upadli dwadzieścia cztery starcy przed obliczem siedzącego na stolicy i kłaniali się żyjącemu na wieki wieków, i rzucali korony swoje przed stolicą, mówiąc: (aiōn g165)
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn g165)
A wszelkie stworzenie, które jest na niebie i na ziemi, i pod ziemią i w morzu, i wszystko, co w nich jest, słyszałem mówiące: Siedzącemu na stolicy i Barankowi błogosławieństwo i cześć, i chwała, i siła na wieki wieków. (aiōn g165)
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn g165)
I widziałem, a oto koń płowy, a tego, który siedział na nim, imię było śmierć, a piekło szło za nim; i dana im jest moc nad czwartą częścią ziemi, aby zabijali mieczem i głodem, i morem, i przez zwierzęta ziemskie. (Hadēs g86)
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs g86)
Mówiąc: Amen! Błogosławieństwo i chwała, i mądrość, i dziękowanie, i cześć, i moc, i siła Bogu naszemu na wieki wieków. Amen. (aiōn g165)
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn g165)
I zatrąbił piąty Anioł i widziałem, że gwiazda spadła z nieba na ziemię, a dano jej klucz studni przepaści. (Abyssos g12)
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos g12)
I otworzyła studnię przepaści; i wystąpił dym z onej studni, jakoby dym pieca wielkiego, i zaćmiło się słońce i powietrze od dymu onej studni. (Abyssos g12)
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos g12)
A miały nad sobą króla, anioła przepaści, któremu imię po żydowsku Abaddon, a po grecku ma imię Apolijon. (Abyssos g12)
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos g12)
I przysiągł przez Żyjącego na wieki wieków, który stworzył niebo i to, co w niem jest, i ziemię, i to, co na niej jest, i morze, i to, co w niem jest, że czasu już nie będzie. (aiōn g165)
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn g165)
A gdy dokończą świadectwa swojego, bestyja, która występuje z przepaści, stoczy z nimi bitwę, a zwycięży ich i pobije ich. (Abyssos g12)
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos g12)
I zatrąbił Anioł siódmy i stały się głosy wielkie na niebie mówiące: Królestwa świata stały się królestwami Pana naszego i Chrystusa jego, i królować będzie na wieki wieków. (aiōn g165)
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn g165)
I widziałem drugiego Anioła, lecącego przez pośrodek nieba, mającego Ewangieliję wieczną, aby ją zwiastował mieszkającym na ziemi i wszelkiemu narodowi, i pokoleniu, i językowi, i ludowi, (aiōnios g166)
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios g166)
A dym męki ich występuje na wieki wieków, i nie mają odpoczynku we dnie i w nocy, którzy się kłaniają bestyi i obrazowi jej, i jeźli kto bierze piętno imienia jej. (aiōn g165)
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn g165)
A jedno ze czworga zwierząt dało siedmiu Aniołom siedm czasz złotych, pełnych gniewu Boga żyjącego na wieki wieków. (aiōn g165)
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn g165)
Bestyja, którąś widział, była, a nie jest, a ma wystąpić z przepaści, a iść na zginienie; i zadziwią się mieszkający na ziemi, (których imiona nie są napisane w księgach żywota od założenia świata), widząc bestyję, która była, a nie jest, a przecię jest. (Abyssos g12)
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos g12)
I rzekli po wtóre: Halleluja! A dym jej wstępuje na wieki wieków. (aiōn g165)
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn g165)
Ale pojmana jest bestyja, a z nią fałszywy on prorok, który czynił cuda przed nią, któremi zwodził tych, którzy przyjęli piętno bestyi i którzy się kłaniali obrazowi jej, i obaj wrzuceni są żywo do jeziora ognistego, gorejącego siarką. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr g3041 g4442)
I widziałem Anioła zstępującego z nieba, mającego klucz od przepaści i łańcuch wielki w ręce swojej. (Abyssos g12)
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos g12)
I wrzucił go w przepaść i zamknął go, i zapieczętował z wierzchu nad nim, aby nie zwodził więcej narodów, ażeby się wypełniło tysiąc lat; a potem musi być rozwiązany na mały czas. (Abyssos g12)
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos g12)
A dyjabeł, który je zwodził, wrzucony jest w jezioro ognia i siarki, gdzie jest ona bestyja i fałszywy prorok; i będą męczeni we dnie i w nocy, na wieki wieków. (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
I wydało morze umarłych, którzy w niem byli, także śmierć i piekło wydały umarłych, którzy w nich byli; i byli sądzeni każdy według uczynków swoich. (Hadēs g86)
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs g86)
A śmierć i piekło wrzucone są w jezioro ogniste. Tać jest wtóra śmierć. (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
A jeśli się kto nie znalazł napisany w księgach żywota, wrzucony jest w jezioro ogniste. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Lecz bojaźliwym i niewiernym, i obmierzłym, i mężobójcom, i wszetecznikom, i czarownikom, i bałwochwalcom, i wszystkim kłamcom część ich dana będzie w jeziorze gorejącem ogniem i siarką: Tać jest śmierć wtóra. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr g3041 g4442)
I nocy tam nie będzie i nie będą potrzebować świecy i światłości słonecznej; bo je Pan Bóg oświeca, i królować będą na wieki wieków. (aiōn g165)
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn g165)
Questioned verse translations do not contain Aionian Glossary words, but may wrongly imply eternal or Hell
Albowiem dawno już jest nagotowane piekło, i dla samego króla nagotowane jest; które głębokie i szerokie uczynił, podniaty jego ognia i drew siła jest; poddymanie Pańskie jako rzeka siarczana zapala je. (questioned)
Ci są studniami bez wody, obłoki od wichru pędzone, którym chmura ciemności na wieki jest zachowana. (questioned)

POG > Aionian Verses: 264, Questioned: 2
CHW > Aionian Verses: 264