< Hioba 17 >

1 Dech mój skażony jest; dni moje giną; groby mię czekają.
“Mtima wanga wasweka, masiku anga atha, manda akundidikira.
2 Zaiste naśmiewcy są przy mnie, a w ich draźnieniu mieszka oko moje.
Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira; maso anga akupenyetsetsa mdani wanga.
3 Staw mi, proszę, rękojmię za się. Któż jest ten? Niech mi na to da rękę.
“Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna. Ndani wina amene adzandiperekera ine chikole?
4 Boś serce ich ukrył przed wyrozumieniem; przetoż ich nie wywyższysz.
Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu; choncho simudzawalola kuti apambane.
5 Kto pochlebia przyjaciołom, oczy synów jego ustaną.
Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma, ana ake sadzaona mwayi.
6 Wystawił mię zaiste na przypowieść ludziom, i jako śmiechowisko przed nimi.
“Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense, munthu amene anthu amalavulira malovu nkhope yake.
7 Zaćmione jest dla żałości oko moje, a wszystkie myśli moje są jako cień.
Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni; ndawonda ndi mutu womwe.
8 Zdumieją się szczerzy nad tem; a niewinny przeciwko obłudnikowi powstanie.
Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi; anthu osachimwa akupsera mtima anthu osapembedza Mulungu.
9 Będzie się trzymał sprawiedliwy drogi swojej; a kto ma czyste ręce, przyczyni mocy.
Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo, ndipo anthu a makhalidwe abwino mphamvu zawo zidzanka zikuchuluka.
10 Wy tedy wszyscy nawróćcie się, a pójdźcie, proszę; bo nie znajduję między wami mądrego.
“Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo, sindidzapezapo munthu wanzeru pakati panupo.
11 Dni moje przeminęły; myśli moje rozerwane są, to jest, zamysły serca mego.
Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka, pamodzinso ndi zokhumba za mtima wanga.
12 Noc mi się w dzień obraca; a światłość skraca się dla ciemości.
Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana, nthawi ya usiku iwo amati ‘kwatsala pangʼono kucha.’
13 Jeźlibym czego oczekiwał, grób będzie domem moim, a w ciemnościach uścielę łoże moje. (Sheol h7585)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
14 Do dołu rzekę: Ojcem moim jesteś; a do robaków: Wy jesteście matką moją, i siostrą moją.
ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’ ndiponso kwa mphutsi kuti, ‘ndinu amayi anga’ kapena ‘mlongo wanga,’
15 Bo gdzież teraz jest nadzieja moja? a oczekiwanie moje któż ogląda?
tsono chiyembekezo changa chili kuti? Ndani angaone populumukira panga?
16 W głębię grobu zstąpię, ponieważ w prochu spólny odpoczynek wszystkich. (Sheol h7585)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)

< Hioba 17 >