< Daniela 4 >

1 Nabuchodonozor król, wszystkim ludziom, narodom, i językom, którzy mieszkają po wszystkiej ziemi: Pokój się wam niech rozmnoży!
Mfumu Nebukadinezara anatumiza mawu awa kwa anthu a mitundu yonse, ndi chiyankhulo chilichonse, amene amakhala pa dziko lonse lapansi: Mtendere uchuluke pakati panu!
2 Znaki i dziwy, które uczynił ze mną Bóg najwyższy, zdało mi się za rzecz przystojną opowiedzieć.
Chandikomera kukuwuzani zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa zimene Mulungu Wammwambamwamba wandichitira.
3 O jakoż są wielkie znaki jego! a dziwy jego jako mocne! królestwo jego królestwo wieczne, i władza jego od narodu do narodu.
Zizindikiro zake ndi zazikulu,
4 Ja Nabuchodonozor żyjąc w pokoju w domu moim, i kwitnąc na pałacu moim,
Ine Nebukadinezara, ndinali kwathu mʼnyumba yanga yaufumu, mwa mtendere ndipo ndinali wokhutitsidwa.
5 Miałem sen, który mię przestraszył, i myśli, którem miał na łożu mojem, a widzenia, którem widział, zatrwożyły mię.
Ndili chigonere pa bedi langa, ndinalota maloto amene anandichititsa mantha. Zinthu ndi masomphenya zimene ndinaziona zinandiopsa.
6 A przetoż wydany jest ode mnie dekret, aby przywiedziono przed mię wszystkich mędrców Babilońskich, którzyby mi wykład snu tego oznajmili.
Choncho ndinalamula kuti anthu onse a nzeru a ku Babuloni abwere pa maso panga kunditanthauzira malotowo.
7 Tedy przyszli mędrcy i praktykarze Chaldejscy, i wieszczkowie; i powiedziałem im sen, a wszakże wykładu jego nie mogli mi oznajmić;
Pamene amatsenga, owombeza, alawuli ndi amawula anabwera, ndinawafotokozera maloto, koma sanathe kunditanthauzira.
8 Aż na ostatek przyszedł przed mię Danijel, którego imię Baltazar według imienia boga mego, a w którym jest duch bogów świętych, a sen powiedziałem przed nim,
Potsiriza, anabwera Danieli uja amatchedwa Belitesezara, potsata dzina la mulungu wanga, ndipo mzimu wa milungu yoyera uli mwa iye. Iyeyu ndinamufotokozera malotowo.
9 Mówiąc: Baltazarze, przedniejszy z mędrców! Ja wiem, iż duch bogów świętych jest w tobie, a żadna tajemnica nie jest ci trudna; widzenia snu mego, którym miał, posłuchaj, a wykład jego powiedz mi.
Ndinati, “Belitesezara, mkulu wa amatsenga, ndikudziwa kuti mzimu wa milungu yoyera uli mwa iwe, ndipo palibe chinsinsi chomwe sungachidziwe. Awa ndi maloto anga; unditanthauzire.
10 Te są widzenia, którem widział na łożu mojem: Widziałem, a oto drzewo w pośrodku ziemi, którego wysokość zbytnia była.
Awa ndi masomphenya amene ine ndinaona pamene ndinali kugona pa bedi: Ndinaona, mtengo wautali kwambiri utayima pakati pa dziko lapansi.
11 Wielkie było ono drzewo i mocne, a wysokość jego dosięgała nieba, a okazałe było aż do granic wszystkiej ziemi;
Mtengowo unakula ndi kulimba ndipo msonga yake inafika mpaka mlengalenga; umaonekera pa dziko lonse lapansi.
12 Gałęzie jego piękne, a owoc jego obfity, i pokarm dla wszystkich był na niem; pod sobą dawało cień zwierzowi polnemu, a na gałęziach jego mieszkało ptastwo niebieskie, a z niego miało pożywienie wszelkie ciało.
Masamba ake anali okongola, zipatso zinali zochuluka, ndipo mu mtengomo munali chakudya chokwanira anthu onse. Zirombo zakuthengo zimapeza mthunzi mʼmunsi mwake, ndipo mbalame zamlengalenga zimakhala pa nthambi zake: Cholengedwa chilichonse chinkadya za mu mtengowu.
13 Widziałem nadto w widzeniach moich na łożu mojem, a oto stróż i Święty z nieba zstąpiwszy,
“Ndikanali chigonere ndinaona mʼmasomphenya mngelo atayima pamaso panga, woyera, atatsika kuchokera kumwamba.
14 Wołał ze wszystkiej mocy, i tak rzekł: Podrąbcie to drzewo, i obetnijcie gałęzie jego, a otłuczcie liście jego, i rozrzućcie owoc jego; niech się rozbieży zwierz, który jest pod niem, i ptastwo z gałęzi jego;
Anayankhula mofuwula kuti, ‘Gwetsa mtengo ndi kusadza nthambi zake; yoyola masamba ake kuti nyama zakuthengo zithawe pa mthunzi pake ndi mbalame zithawe pa nthambi zake.
15 Wszakże pień korzenia jego w ziemi zostawcie, a niech będzie związany łańcuchem żelaznym i miedzianym na trawie polnej, aby rosą niebieską był skrapiany, a z zwierzętami niech się pasie w trawie ziemskiej;
Koma musiye tsinde ndi mizu yake mʼnthaka. Tsindelo mulimange maunyolo a chitsulo ndi mkuwa, zikhalebe mʼnthaka, nʼkudya udzu mʼmunda. “‘Mumulole iye anyowe ndi mame akumwamba, ndipo iye akhale ndi nyama pakati pa zomera za mʼnthaka.
16 Serce jego od człowieczego niech się odmieni, a serce zwierzęce niech mu dane będzie, a siedm lat niech pominą nad nim.
Maganizo ake a umunthu asinthidwe ndipo apatsidwe maganizo a nyama ya kuthengo, mpaka zaka zisanu ndi ziwiri zitadutsa.
17 Ta rzecz według wyroku stróżów, a to żądanie według mowy świętych stanie się, aż do tego przyjdzie, że poznają ludzie, iż Najwyższy panuje nad królestwem ludzkiem, a daje je, komu chce, a najpodlejszego z ludzi stanowi nad niem.
“‘Angelo oyera ndiwo akutsimikiza chilangochi. Tsono anthu adziwe kuti Mulungu Wammwambamwamba ali ndi mphamvu yolamulira maufumu onse, ndipo amawapereka kwa aliyense akumufuna, ngakhale munthu wamba kuti alamulire.’
18 Ten sen widziałem ja król Nabuchodonozor; a ty, Baltazarze! powiedz wykład jego, gdyż wszyscy mędrcy królestwa mego nie mogli mi tego wykładu oznajmić; ale ty możesz, bo duch bogów świętych jest w tobie.
“Amenewa ndi maloto amene ine, mfumu Nebukadinezara, ndinalota. Tsopano Belitesezara, undifotokozere tanthauzo lake, popeza palibe mwa anthu anzeru a mu ufumu wanga amene angathe kunditanthauzira. Koma iwe ukhoza, chifukwa mzimu wa milungu yoyera uli mwa iwe.”
19 Tedy Danijel, którego imię Baltazar, zdumiewał się przez jednę godzinę, a myśli jego trwożyły go. A odpowiadając król rzekł: Baltazarze! sen i wykład jego niech cię nie trwoży. Odpowiedział Baltazar, i rzekł: Panie mój! ten sen niech przyjdzie na tych, którzy cię nienawidzą, a wykład jego na nieprzyjaciół twoich.
Pamenepo Danieli, amene amatchedwa Belitesezara, anavutika mu mtima kwambiri kwa kanthawi, ndipo anasautsidwa mʼmaganizo ake. Choncho mfumu inati, “Belitesezara usalole malotowa kapena tanthauzo lake likuopse.” Belitesezara anayankha kuti, “Mbuye wanga, ndikanakonda malotowa akanakhudza adani anu okha, ndi tanthauzo lake kwa iwo okusautsani!
20 Drzewo, któreś widział rosłe i mocne, którego wysokość dosięgała nieba, a które okazałe było wszystkiej ziemi,
Mtengo munawuona uja, umene unkakulirakulira kwambiri ndi kulimba, ndi msonga yake inafika mlengalenga, ndi kuonekera ku dziko lonse lapansi,
21 Którego gałąź piękna, a owoc jego obfity, a pokarm dla wszystkich na niem, pod którem mieszkał zwierz polny, a na gałęziach jego przebywało ptastwo niebieskie,
mtengo umene masamba ake anali okongola ndiponso unali ndi zipatso zochuluka zokwanira kudya anthu onse a dziko lapansi. Mtengowu unkapereka mthunzi ku zirombo zonse zakuthengo, ndipo mbalame zamlengalenga zinayika zisa pa nthambi zake.
22 Tyś jest tym, o królu! któryś się rozwielmożył i zmocnił, a wielkość twoja urosła, i podniosła się aż do nieba, a władza twoja aż do kończyn ziemi.
Inu mfumu, ndinu mtengo umenewo! Inu mwakhala wamkulu ndi wamphamvu; ukulu wanu wakula mpaka wakhudza mlengalenga, ndipo ufumu wanu wafika mpaka ku malo akutali a dziko lapansi.
23 A iż król widział stróża i Świętego zstępującego z nieba a mówiącego: Podrąbcie to drzewo, a zepsujcie je, wszakże pień i z korzeniem jego w ziemi zostawcie, aby rosą niebieską był skrapiany a z zwierzętami polnemi niech się pasie, ażby się wypeł niło siedm lat nad nim;
“Inu mfumu munaona mthenga woyera, akuchokera kumwamba ndipo anati, ‘Gwetsani mtengo ndipo muwuwononge, koma musiye tsinde ndi mizu yake. Tsindelo mulimange ndi unyolo wa chitsulo ndi mkuwa ndipo mulisiye pakati pa udzu wa mʼmunda. Mulole kuti linyowe ndi mame akumwamba. Likhale ngati nyama zakuthengo, mpaka zaka zidutse zisanu ndi ziwiri.’
24 Tenci jest wykład, o królu! i ten dekret Najwyższego, który wyszedł na króla, pana mego;
“Tanthauzo lake ndi ili mfumu, izi ndi zimene Mulungu Wammwambamwamba watsimikiza kuti zikugwereni mbuye wanga mfumu:
25 Bo cię wyrzucą od ludzi, a z zwierzem polnym będzie mieszkanie twoje, a trawą jako wół paść się będziesz, a rosą niebieską skrapiany będziesz, aż się wypełni siedm lat nad tobą, dokądbyś nie poznał, że Najwyższy panuje nad królestwem ludzkiem, a że je daje, komu chce.
Inu mudzachotsedwa pakati pa anthu ndipo mudzakhala ndi nyama zakuthengo; mudzadya udzu monga ngʼombe ndi kunyowa ndi mame akumwamba. Zaka zisanu ndi ziwiri zidzadutsa mpaka mudzavomereze kuti Mulungu Wammwambamwamba ndiye mwini ulamuliro pa ma ufumu a anthu, ndipo amawapereka kwa aliyense amene Iye wafuna.
26 A iż rozkazano zostawić pień i z korzeniem onego drzewa, znaczy, że królestwo twoje tobie zostanie, gdy poznasz, że niebiosa panują.
Lamulo losiya tsinde la mtengo ndi mizu yake litanthauza kuti ufumu wanu udzabwezeredwa kwa inu mukadzavomereza kuti Mulungu ndiye amalamulira.
27 Przetoż o królu! rada moja niech ci się podoba, a grzechy twoje przerwij sprawiedliwością, a nieprawości twoje miłosierdziem nad utrapionym, owa snać stanie się przedłużenie pokoju twego.
Nʼchifukwa chake mfumu, chikukomereni kulandira malangizo anga: Lekani machimo ndipo muzichita zabwino, lekani mphulupulu zanu ndipo muzikomera mtima anthu opsinjika. Nʼkutheka kuti mtendere wanu udzapitirira.”
28 Wszystko to przyszło na króla Nabuchodonozora;
Zonsezi zinamuchitikira mfumu Nebukadinezara.
29 Bo po wyjściu dwunastu miesięcy, przechodząc się w Babilonie na pałacu królewskim,
Itapita miyezi khumi ndi iwiri, pamene mfumu inkayenda pa denga la nyumba ya ufumu ya ku Babuloni,
30 Mówił król i rzekł: Izali nie to jest on Babilon wielki, którym ja w sile mocy mojej zbudował, aby był stolicą królestwa i ku ozdobie sławy mojej?
iye anati, “Kodi Babuloni si mzinda wamphamvu ndi wokongola umene ndinamanga ndi mphamvu zanga ngati nyumba yanga yaufumu, kuonetsera ulemerero wa ufumu wanga?”
31 A gdy jeszcze ta mowa była w ustach królewskich, oto głos z nieba przyszedł mówiąc: Tobie się mówi, królu Nabuchodonozorze! że królestwo twoje odeszło od ciebie;
Akuyankhulabe izi mawu anamveka kuchokera kumwamba kuti, “Imvani izi, mfumu Nebukadinezara: Ufumu wako wachotsedwa.
32 I od ludzi wyrzucą cię, a z zwierzem polnym będzie mieszkanie twoje; trawą jako wół paść się będziesz, ażby się wypełniło siedm lat nad tobą, dokądbyś nie poznał, że Najwyższy panuje nad królestwem ludzkiem, a że je daje, komu chce.
Udzachotsedwa pakati pa anthu ndipo udzakhala ndi zirombo zakuthengo; udzadya udzu monga ngʼombe. Zaka zisanu ndi ziwiri zidzadutsa mpaka iwe utavomereza kuti Wammwambamwamba ndiye mwini ulamuliro pa maufumu a anthu ndipo amawupereka kwa aliyense amene iye afuna.”
33 Tejże godziny wypełniło się ono słowo nad Nabuchodonozorem; bo go wyrzucono od ludzi, a trawę jadał jako wół, a rosą niebieską ciało jego skrapiane było, aż na nim włosy urosły jako pierze orle, a paznogcie jego jako pazury u ptaków.
Nthawi yomweyo zonse zimene zinanenedwa zokhudza Nebukadinezara zinakwaniritsidwa. Iye anachotsedwa pakati pa anthu ndipo ankadya udzu ngati ngʼombe. Thupi lake linanyowa ndi mame akumwamba mpaka tsitsi lake linakula ngati nthenga za chiwombankhanga ndi zikhadabo ngati zikhadabo za mbalame.
34 A po skończeniu onych dni podniosłem ja Nabuchodonozor w niebo oczy moje, a rozum mój do mnie się zaś wrócił, i błogosławiłem Najwyższego, a Żyjącego na wieki chwaliłem i wysławiałem; bo władza jego władza wieczna, a królestwo jego od narodu do narodu.
Pomaliza pa zaka zimenezo ine, Nebukadinezara ndinakweza maso anga kumwamba, ndipo nzeru zanga zinabwereramo. Kenaka ndinatamanda Wammwambamwamba; ndinamupatsa ulemu ndi kumulemekeza Iye amene akhala nthawi zonse.
35 A wszyscy obywatele ziemi jako za nic poczytani są. Według woli swojej postępuje, z wojskiem niebieskiem i z obywatelami ziemi, a niemasz, ktoby wstręt uczynił ręce jego i rzekł mu: Cóż to czynisz?
Anthu onse a dziko lapansi
36 Tegoż czasu rozum mój wrócił się do mnie, a do sławy królestwa mego ozdoba moja, i dostojność moja wróciła się do mnie; nadto hetmani moi i książęta moi szukali mię, a na królestwie mojem zmocniłem się, i wielmożność większa mi jest przydana.
Pa nthawi yomweyo nzeru zanga zinabwereramo. Ndinalandiranso ulemu wanga ndi ufumu wanga. Nduna ndi akalonga anga anandilandiranso. Ndipo anandibwezera ufumu wanga ndi kukhalanso wamphamvu kuposa kale.
37 A tak teraz ja Nabuchodonozor chwalę, i wywyższam i wysławiam króla niebieskiego, którego wszystkie sprawy są prawdą, a ścieszki jego sądem, a który chodzących w hardości poniżyć może.
Tsopano ine Nebukadinezara, ndikutamanda, kukweza ndi kulemekeza Mfumu yakumwamba chifukwa zonse zimene amachita ndi zoyenera ndipo njira zake zonse ndi zachilungamo. Ndipo onse amene amayenda modzikuza adzawatsitsa.

< Daniela 4 >