< Maluko 6 >

1 Yesu na vawuliwa vaki, vakawuka penapo vakahamba kuchijiji chaki cha ku Nazaleti.
Yesu anachoka kumeneko napita ku mudzi kwawo, pamodzi ndi ophunzira ake.
2 Ligono la Kupumulila, atumbwili kuwula munyumba ya kukonganekela Vayawudi. Vamahele vevamuyuwini vakangisi, vakajova, “Wu, agapatili koki mambu aga geijova? Apatili koki luhala ulu? Kavili ikita wuli gachinamtiti?
Tsiku la Sabata litafika, anayamba kuphunzitsa mʼsunagoge, ndipo ambiri amene anamumva anadabwa. Iwo anafunsa kuti, “Kodi munthu uyu anazitenga kuti zimenezi? Kodi ndi nzeru yotani imene munthu ameneyu wapatsidwa, kuti Iye akuchitanso zodabwitsa!
3 Wu, mwenuyu lepi selemala, mwana wa Maliya na mlongo wavi Yakobo na Yose na Yuda na Simoni? Wu, valumbu vaki titama nawu lepi bahapa?” Ndi vakabela kumsadika.
Kodi uyu si mpalamatabwa uja? Kodi uyu si mwana wa Mariya ndi mʼbale wa Yakobo, Yose, Yudasi ndi Simoni? Kodi alongo ake si ali ndi ife?” Ndipo anakhumudwa naye.
4 Yesu akavajovela, “Mlota wa Chapanga itopeswa kila pandi, lepi kunyumba yaki, kwa valongo vaki na pamulima waki.”
Yesu anawawuza kuti, “Mneneri amalemekezedwa kulikonse kupatula kwawo, ndi pakati pa abale ake ndi a mʼbanja mwake.”
5 Ndava yeniyo Yesu akitili lepi mambu gachinamtiti pala, ndi avavikili mawoko vatamu vadebedebe akavalamisa.
Sanachite zodabwitsa kumeneko, koma anangosanjika manja pa odwala ochepa ndi kuwachiritsa.
6 Akangisi neju ndava ya vandu vangasadika. Kangi Yesu avigendalili muhijiji ya papipi na kuvawula vandu.
Ndipo Iye anadabwa chifukwa chakusowa chikhulupiriro kwawo. Pamenepo Yesu anayenda mudzi ndi mudzi kuphunzitsa.
7 Akavakemela vawuliwa kumi na vavili, akatumbula akavatuma vandu vavili vavili, akavapela uhotola wa kuvinga mizuka.
Atayitana khumi ndi awiriwo, Iye anawatuma awiriawiri ndipo anawapatsa ulamuliro pa mizimu yoyipa.
8 Akavalagiza akajova, “Kwemwihamba uko, mukotoka kugega chindu chochoha chila ndonga ndu, lepi chakulya, lihaku, amala mashonga pachilolo.
Zomwe anawalangiza ndi izi: “Musatenge kanthu ka paulendo koma ndodo yokha; osatenga buledi, thumba, kapena ndalama.
9 Muwala champali nambu mkotoka kugega ligwanda lingi.”
Muvale nsapato koma osatenga malaya apadera.
10 Akavajovela, “Nyumba yeyoha yevakuvapokela mutama bahapo mbaka pa ligono lemuwuka.
Pamene mulowa mʼnyumba mukakhale momwemo kufikira mutachoka mʼmudzimo.
11 Kwa vandu vevibela kuvapokela amala kuvayuwanila, penapo ndi muwuka na muvakung'undila lububu lwavi, kulangisa kuvya vene vaubeli ujumbi wa Chapanga!”
Ndipo ngati pa malo ena sakakulandirani kapena kukumverani, sasani fumbi la kumapazi anu pamene mukuchoka, kuti ukhale umboni wowatsutsa.”
12 Hinu, vakawuka penapo vakahamba kuvakokosela vandu vamuwuyila Chapanga.
Anatuluka kupita kukalalikira kuti anthu atembenuke mtima.
13 Vakayivinga mizuka vamahele. Na kuvanyala mahuta ga zeituni vatamu vamahele, vakavalamiswa.
Anatulutsa ziwanda zambiri ndi kudzoza mafuta odwala ambiri ndi kuwachiritsa.
14 Nkosi Helodi agayuwini goha, muni malovi ga Yesu gayenili pandi zoha. Vandu vangi vajovayi mwenuyu, “Ndi Yohani Mbatizaji ayukili! Ndava muni ihenga gachinamtiti.”
Mfumu Herode anamva zimenezi, pakuti dzina la Yesu linali litadziwika kwambiri. Ena amati, “Yohane Mʼbatizi waukitsidwa kwa akufa, ndipo nʼchifukwa chake mphamvu zochita zodabwitsa zinkagwira ntchito mwa Iye.”
15 Vangi vakajova, “Mwenuyu ndi Eliya.” Vangi vakajova, “Mwenuyu ndi mmonga wa valota va Chapanga va kadeni.”
Ena anati, “Iye ndi Eliya.” Enanso anati, “Ndi mneneri, ofanana ndi mmodzi wa aneneri akale.”
16 Nambu Helodi peayuwini malovi gala akajova, “Yohani namdumwili mutu, hinu ayukili!”
Koma Herode atamva zimenezi anati, “Yohane, munthu amene ndinamudula mutu, waukitsidwa kuchokera kwa akufa.”
17 Aholalili genago ndava mu magono ga mumbele, Helodi alagazili Yohani akamuliwa na kukungiwa muchifungu. Genago gahumalili ndava Helodi amgegili Helodiya mdala wa Filipi mweavi mlongo waki.
Pakuti Herode iye mwini analamula kuti amumange Yohane ndi kumuyika mʼndende. Anachita izi chifukwa cha Herodia, mkazi wa mʼbale wake Filipo, amene iye anamukwatira.
18 Yohani amjovelayi Helodi, “Chabwina lepi veve kumtola mdala wa mlongo waku.”
Pakuti Yohane ankanena kwa Herode kuti, “Sikololedwa kwa inu kuti mukwatire mkazi wa mʼbale wanu.”
19 Hinu Helodiya, mweavi mdala wa nkosi, amuhakalili neju Yohani, akagana kumkoma, nambu ahotwili lepi.
Ndipo Herodia anamusungira Yohane chidani ndipo anafuna kumupha, koma sanathe kutero,
20 Helodi amuyogwipi Yohani muni amanyili kuvya Yohani ndi mundu wa msopi na mbwina. Ndava yeniyo amyangalili. Helodi aganayi kumuyuwanila Yohani, pamonga amyuwanili mtima wamvinili.
chifukwa Herode anaopa Yohane ndipo anamuteteza, podziwa kuti iye anali munthu wolungama ndi woyera mtima. Herode akamamva Yohane, ankathedwa nzeru; komabe amakonda kumumvetsera.
21 Ligono limonga mdala wa nkosi apatili fwasi pa ligono la kukumbukwa kwa kuvelekewa Helodi. Hinu akavakemela vagogo va libanji na vachilongosi va Galilaya pamonga na vakulu va manjolinjoli.
Pomaliza mpata unapezeka. Pa tsiku lokumbukira kubadwa kwake, Herode anakonzera phwando akuluakulu ake, akulu a ankhondo ndi anthu odziwika a mu Galileya.
22 Hinu msikana waki Helodiya, akayingila na kutumbula kukina ngo'ma. Hinu akavahekesa neju Helodi na vayehe vaki. Nkosi akamjovela msikana yula, “Uniyupa chindu chochoha chila na nene yati nikupela.”
Mwana wamkazi wa Herodia atabwera ndi kudzavina, anakondweretsa Herode ndi alendo ake a pa mphwandopo. Mfumu inati kwa mtsikanayo, “Undipemphe chilichonse chimene ukuchifuna, ndipo ndidzakupatsa.”
23 Kavili akamlapakisa, akamjovela, “Chochoha cheukuniyupa, yati nikupela, hati ngati kugavana upinga wa unkosi wangu.”
Ndipo analonjeza ndi lumbiriro kuti, “Chilichonse chimene upempha ndidzakupatsa, ngakhale theka la ufumu wanga.”
24 Penapo msikana yula akawuka mugati mu libanji, akahamba kumkota nyina waki. “Wigana niyupa kyani?” Namwene akamyangula, “Mutu wa Yohani Mbatizaji.”
Iye anatuluka nati kwa amayi ake, “Kodi ndikapemphe chiyani?” Iye anamuyankha kuti, “Mutu wa Yohane Mʼbatizi.”
25 Msikana yula akawuya kanyata kavili kwa nkosi, akamjovela, “Nigana unipela hinu naha mulupalu mutu wa Yohani Mbatizaji.”
Nthawi yomweyo mtsikana uja anafulumira kupita komwe kunali mfumu ndi pempho lake: “Ndikufuna kuti mundipatse pomwe pano mutu wa Yohane Mʼbatizi mʼmbale.”
26 Nkosi peayuwini genago, akavya ngolongondi, nambu muni ajilapakisi mwene, na ndava ya vayehe vaki, ahotwili lepi kumbelelela msikana yula ndi akamyidikila.
Mfumu inamva chisoni chachikulu, koma chifukwa cha lumbiro lake ndi alendo ake a pa mphwandolo, sanafune kumukaniza.
27 Hinu, akamlagiza linjolinjoli akaleta mutu wa Yohani. Linjolinjoli akahamba kuudumula mutu wa Yohani muchifungu mula,
Nthawi yomweyo iye anatumiza yemwe anali ndi ulamuliro wonyonga anthu kuti abweretse mutu wa Yohane. Munthuyo anapita, nakadula mutu wa Yohane mʼndende,
28 kangi amletili mutu wula mulupalu akampela msikana, namwene akampelekela nyina waki.
nabweretsa mutuwo mʼmbale. Anawupereka kwa mtsikanayo, ndipo iye anakapereka kwa amayi ake.
29 Vawuliwa va Yohani pevayuwini vakahamba kutola higa yaki vakahamba kuzika.
Atamva izi, ophunzira a Yohane anabwera nadzatenga mtembo ndi kukawuyika mʼmanda.
30 Vamitumi vakawuya mulugendu lwavi vakamjovela Yesu, mambu goha gavakitili na chavawulili vandu.
Atumwi anasonkhana mozungulira Yesu namufotokozera zonse zomwe anachita ndi kuphunzitsa.
31 Vandu vamahele neju vabwelayi na kuwuka kwa Yesu, ndi mbaka fwasi ya kulya yavi lepi. Hinu Yesu akavajovela vawuliwa, “Tihamba kuchiyepela mukapumulila padebe.”
Popeza kuti panali anthu ambiri amene amabwera ndi kumapita, analibe mpata wakuti adye, ndipo Iye anawawuza kuti, “Tiyeni kuno kumalo achete kuti tikapume.”
32 Hinu, vakawuka ngavene muwatu vakahamba kuchiyepela.
Ndipo anachoka okha pa bwato napita kumalo a okhaokha.
33 Nambu vandu vamahele vavaweni pavawukayi, vakavamanya. Ndi vakalongolela kuhika kula kwa magendelu kweahambayi Yesu na vawuliwa vaki.
Koma ambiri amene anawaona akuchoka anawazindikira ndipo anathamanga wapansi kuchokera mʼmidzi yonse nakayambirira kufika.
34 Yesu na vawuliwa vaki pevahulwiki muwatu kumbwani, ndi auweni msambi uvaha wa vandu, akaviniswa mtima, muni vavi ngati limbelele langali mdimaji. Akatumbula kuvawula mambu gamahele.
Yesu atafika ku mtunda ndi kuona gulu lalikulu la anthu, anamva nawo chisoni chifukwa anali ngati nkhosa zopanda mʼbusa. Ndipo anayamba kuwaphunzitsa zinthu zambiri.
35 Lilanga palatipimi, ndi vawuliwa vaki vakahamba kumjovela Yesu, “Penapa palugangatu, lilanga litipama.
Pa nthawi iyi nʼkuti dzuwa litapendeka, ndipo ophunzira ake anabwera kwa Iye nati, “Kuno ndi kuthengo, ndipo ano ndi madzulo.
36 Mbanga uvalaga vandu vahamba mumigunda na muhijiji ya papipi, vakagula vyakulya.”
Awuzeni anthuwa azipita ku midzi ndi madera ozungulira, kuti akadzigulire kanthu kakuti adye.”
37 Yesu akavajovela, “Muvapela nyenye chakulya.” Nambu vene vakamkota, “Tivapela kyani? Yati yikutigana tihenga lihengu kwa miyehi yamahele ndi tipatayi mashonga ga kuvagulila chakulya vandu voha ava?”
Koma Iye anayankha kuti, “Apatseni kanthu koti adye.” Iwo anati kwa Iye, “Apa pafunika ndalama za miyezi isanu ndi itatu zomwe munthu amalandira! Kodi tipite kukagwiritsa ntchito ndalama zotere kugulira buledi kuti tiwapatse adye?”
38 Yesu akavakota, “Mabumunda gavi galinga? Muhamba mukalola.” Pevamali kulola vakawuya kumjovela, “Yivii mhanu na somba zivili.”
Iye anawafunsa kuti, “Muli ndi malofu a buledi angati? Pitani mukaone.” Ataona anati kwa Iye, “Asanu ndi nsomba ziwiri.”
39 Yesu akavalagiza vawuliwa vaki vavatamika vandu voha chikundi chikundi pahi pamanyai.
Pamenepo Yesu anawalamulira kuti awakhazike anthu pansi mʼmagulu pa msipu obiriwira.
40 Hinu vene vakatama chikundi chikundi, vingi vandu hamsini, na vingi vandu miya.
Ndipo anakhala pansi mʼmagulu a anthu 100 ndi gulu la anthu makumi asanu.
41 Kangi Yesu akagatola mabumunda mhanu na somba zila, akalola kunani kwa Chapanga, akamsengusa Chapanga. Ndi akagametula mabumunda gala pamonga na somba zila. Akavapela vawuliwa vaki muni vavagavanisila vandu.
Atatenga malofu a buledi asanu ndi nsomba ziwiri, nayangʼana kumwamba, Iye anayamika nagawa malofu a bulediwo. Kenaka anawapatsa ophunzira ake kuti awapatse anthu. Ndipo anagawanso nsomba ziwirizo kwa onse.
42 Vandu voha vevavi penapo valili vakayukuta.
Onse anadya ndipo anakhuta,
43 Hinu, vakanonga masigalilu ga mabumunda na somba vakamemesa madengu kumi na gavili.
ndipo ophunzira ake anatola buledi ndi nsomba zotsalira zokwanira madengu khumi ndi awiri.
44 Vevalili chakulya chila, vavi vagosi elufu mhanu.
Chiwerengero cha amuna amene anadya chinali 5,000.
45 Bahapo Yesu akavalagiza vawuliwa vaki vayingila muwatu valongolela kuhamba kumwambu ya nyanja, kumuji wa Betisaida. Muni mwene avi akona ilagana na msambi wa vandu.
Nthawi yomweyo Yesu anawuza ophunzira ake kuti alowe mʼbwato ndi kuti atsogole kupita ku Betisaida, pamene Iye ankawuza anthu kuti azipita.
46 Hati peamali kulagana na vandu, akahamba kuchitumbi kumuyupa Chapanga.
Atawasiya, Iye anakwera ku phiri kukapemphera.
47 Lilanga palatipimi, Yesu avi mwene kundumba na watu wamali kuhika pagati ya nyanja.
Pofika madzulo, bwato linali pakati pa nyanja, ndipo Iye anali yekha pa mtunda.
48 Mwene avaweni vawuliwa chaving'ahika muwatu mula na mipundi muni mpungu wavi uvaha ukuvawuyisa mumbele. Hinu hambakucha, Yesu avahegalili kuni igenda mumanji akagana kuvapita.
Iye anaona ophunzira ake akuvutika popalasa bwato, chifukwa mphepo imawomba mokumana nawo. Pa nthawi ya mʼbandakucha Iye anafika kwa iwo akuyenda pa nyanja. Anali pafupi kuwapitirira,
49 Nambu pavamuweni igenda panani ya manji vayogwipi, vaholali kuvya lihoka, “Vakaywanga mulete.”
koma atamuona Iye akuyenda pa nyanja, anaganiza kuti anali mzukwa. Iwo anafuwula,
50 Voha pavamuweni vayogwipi neju. Bahapo Yesu akajova nawu, “Mjipolesa mtima. Ndi nene. Mkoto kuyogopa!”
pakuti onse anamuona ndipo anachita mantha. Nthawi yomweyo Iye anawayankhula nati, “Limbani mtima! Ndine. Musachite mantha.”
51 Ndi, akayingila muwatu wevavili vawuliwa na mpungu wa luyuga lukaguna lukumbi lulalula. Vawuliwa vakakangasa neju,
Ndipo Iye anakwera mʼbwato pamodzi nawo, ndipo mphepo inaleka. Iwo anadabwa kwambiri,
52 ndava muni vamanyili lepi mana chinamtiti cha kuyonjokeseka chakulya chila ndava ya kunonopa kwa mitima yavi.
popeza sanazindikire zimene zinachitika pa malofu a buledi; pakuti mitima yawo inali yowuma.
53 Vakakupuka nyanja, vakahika kumuji wa ku Genezaleti vakahuyimika watu.
Atawoloka, anafika ku Genesareti nayima pa dooko.
54 Pevahumili muwatu mula, kanyata vandu vakammanya Yesu.
Atangotuluka mʼbwato, anthu anamuzindikira Yesu.
55 Hinu, kanyata vakahamba kila chijiji pandu pala, vakatumbula kuvatola vatamu vevagonili mumipasa, vakavapeleka kila pevayuwini Yesu avili.
Anathamanga uku ndi uko mʼdera lonse nakanyamula odwala pa machira kupita nawo kulikonse kumene anamva kuti kuli Iye.
56 Pandu poha peahambili Yesu, muhijiji na mumiji na mumigunda, vandu vavavikili vatamu pandu pakugulisila vindu, vandu vakamuyupa neju avayidakila vatamu vala, vapamisayi lugunyilu lwa nyula yaki. Ndi voha vevampamisi valamili.
Ndipo kulikonse kumene anapita, ku midzi, mʼmizinda ndi madera a ku midzi, iwo anayika odwala mʼmalo a mʼmisika. Iwo anamupempha kuti awalole kuti akhudze ngakhale mphonje za mkanjo wake, ndipo onse amene anamukhudza anachira.

< Maluko 6 >