< Psalm 138 >

1 [Psalm lal David] Nga sot kulo nu sum, LEUM GOD, ke insiuk nufon, Nga on kaksakin kom ye mutun god uh.
Salimo la Davide. Ndidzakuyamikani Yehova ndi mtima wanga wonse; ndidzayimba nyimbo zokutamandani pamaso pa “milungu.”
2 Nga forla nu ke Tempul mutal sum, Ac pasrla, ac kaksakin Inem Ke sripen lungse kawil ac pwaye lom, Oayapa ke kom akkalemye lah Inem, ac sap lom, fulat liki ma nukewa.
Ndidzagwada kuyangʼana ku Nyumba yanu yoyera ndipo ndidzayamika dzina lanu chifukwa cha chikondi chanu ndi kukhulupirika kwanu, pakuti Inu mwakuza dzina lanu ndi mawu anu kupambana zinthu zonse.
3 Kom topukyu ke nga tuh pang nu sum; Ke ku lom, kom tuh akkeyeyu.
Pamene ndinayitana, munandiyankha; munandisandutsa wamphamvu ndi wolimba mtima.
4 Tokosra nukewa fin faclu elos fah kaksakin kom, LEUM GOD, Mweyen elos lohng wulela lom.
Mafumu onse a dziko lapansi akuyamikeni Yehova, pamene amva mawu a pakamwa panu.
5 Elos ac fah onkakin orekma lom Ac ke wolana yohk lom.
Iwo ayimbe za njira za Yehova, pakuti ulemerero wa Yehova ndi waukulu.
6 Kom finne muta yen fulat, A kom nunku kaclos su pusisel, Ac kom suiya mwet filang yen loesla me.
Ngakhale kuti Yehova ngokwezeka, amasamalira odzichepetsa, koma anthu onyada amawadziwira chapatali.
7 Ke pacl mwe lokoalok rauniyula Kom karingyume. Kom lain kasrkusrak lun mwet lokoalok luk Ac kom moliyula ke po ku lom.
Ngakhale ndiyende pakati pa masautso, mumasunga moyo wanga; mumatambasula dzanja lanu kutsutsana ndi mkwiyo wa adani anga, mumandipulumutsa ndi dzanja lanu lamanja.
8 Kom fah oru ma nukewa ma kom wulela kac; LEUM GOD, lungse lom oan ma pahtpat. Aksafyela orekma su kom mutawauk oru.
Yehova adzakwaniritsa cholinga chake pa ine; chikondi chanu chosasinthika Yehova, ndi chosatha musasiye ntchito ya manja anu.

< Psalm 138 >