< Job 26 >

1 Na Job el fahk,
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 “Ku pwaye kutu kasru uh — Nga sukasrup ac munas, a kom fahk ma ingan!
“Wamuthandizadi munthu wopanda mphamvu! Walimbitsadi dzanja la munthu wofowoka!
3 Saok kas in kasru na wowo Ac luti lalmwetmet lom an nu sin mwet lalfon se nga uh!
Wapereka malangizo kwa munthu amene alibe nzeru! Ndipotu waonetsadi nzeru zochuluka!
4 Kom nunku mu su ac lohng kas lom ingan? Su pirikkomyak kom in kaskas ouingan uh?”
Kodi wakuthandiza ndani kuti uyankhule mawu awa? Ndipo ndi mzimu wa yani umene unayankhula pakamwa pako?
5 “Ngunin mwet misa uh Rarrar in kof ye faclu.
“Mizimu ya anthu akufa ikunjenjemera pansi pa madzi, ndi zonse zokhala mʼmadzimo.
6 Facl sin mwet misa uh ikakelik oan ye mutun God; Ac wangin mwe afyuf kosrala ma inge liki ye mutal. (Sheol h7585)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
7 God El asroelik acn engyeng in epang, Ac srupusrak faclu yen wangin ma oan we.
Mulungu anayala thambo la kumpoto pa phompho; Iye anakoloweka dziko lapansi mʼmalo mwake pamene panali popanda nʼkanthu komwe.
8 God pa nwakla pukunyeng uh ke kof, Ac liyaung in tia fokelik ke toasriya uh.
Amasunga madzi ambiri mʼmitambo yake, koma mitamboyo siphulika chifukwa cha kulemera kwa madziwo.
9 El sang sie pukunyeng kosrala malem uh ke fong in Mwesr.
Iye amaphimba mwezi wowala, amawuphimba ndi mitambo yake.
10 El filiya pekusra uh raunela faclu In sraclik kalem liki lohsr uh.
Mulungu anawalembera madzi malire wonga uta, kukhala malire pakati pa kuwunika ndi mdima.
11 Ke el kai sru ma loango acn lucng, Sru uh ac kusrusryak ac rarrar ke sangeng.
Mizati yochirikiza mitambo yakumwamba imanjenjemera, ndi kudabwa pa kudzudzula kwake.
12 Ku lal uh pa kutangla meoa uh; Ac ke usrnguk lal El kunausla Rahab — ma sulallal soko ma muta inkof uh.
Ndi mphamvu zake anatontholetsa nyanja; ndi nzeru zake anakantha chirombo cha mʼmadzi chija chotchedwa Rahabe.
13 Momong lal uh pa oru acn engyeng uh in kalem, Ac paol pa uniya kosro sulallal su srike in kaingla uh.
Ndi mpweya wake anayeretsa zamumlengalenga, dzanja lake linapha chinjoka chothawa chija.
14 Tusruktu ma inge akkalemye kutu srisrik na kuiyal, Mahma na lal uh pa kut lohng inge. Su ku in etu lupan fulat ac ku lun God uh?”
Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake; tingomva pangʼono za Iye ngati kunongʼona! Kodi ndani angathe kudziwa kukula kwa mphamvu zake?”

< Job 26 >