< Psalm 45 >

1 [Kusen On lun Tulik natul Korah su Onkakin Lungse] Kas wolana oan in nunak luk Ke nga kinala on soko inge nu sin tokosra. Louk akola tari nu ke on soko inge, Oana pen in sim nutin sie mwet etu sim.
Kwa mtsogoleri wamayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe a “Maluwa a Kakombo.” Salimo la ana a Kora. Nyimbo ya pa ukwati. Mtima wanga watakasika ndi nkhani yokoma pamene ndikulakatula mawu anga kwa mfumu; lilime langa ndi cholembera cha wolemba waluso.
2 Kom pa oasku emeet inmasrlon mukul uh. Kom mwet na pah in sramsram se. God El akinsewowoye kom pacl e nukewa.
Inu ndinu abwino kwambiri kuposa anthu onse ndipo milomo yanu inadzozedwa ndi chikondi cha Mulungu chosasinthika, popeza Mulungu wakudalitsani kwamuyaya.
3 Tokosra kulana, losya cutlass nutum pupom; Kom wolana ac fulatlana.
Mangirirani lupanga lanu mʼchiwuno mwanu, inu munthu wamphamvu; mudziveke nokha ndi ulemerero ndi ukulu wanu.
4 Kasrusr nu meet in wal fulat lom, nu ke kutangla, Tuh kom in karinganang ma pwaye ac suwoswos! Ku lom ac fah asot kutangla lulap!
Mu ukulu wanu mupite mutakwera mwachigonjetso mʼmalo mwa choonadi, kudzichepetsa ndi chilungamo; dzanja lanu lamanja lionetsere ntchito zanu zoopsa.
5 Mwe pisr nutum an kosroh, Elos fakisya insien mwet lokoalok lom; Mutunfacl elos putatla nu ye niom.
Mivi yanu yakuthwa ilase mitima ya adani a mfumu, mitundu ya anthu igwe pansi pa mapazi anu.
6 Tokosrai su God El sot nu sum Ac fah oan nwe tok ma pahtpat. Kom leum fin mwet lom ke suwoswos;
Mpando wanu waufumu, Inu Mulungu, udzakhala ku nthawi za nthawi; ndodo yaufumu yachilungamo idzakhala ndodo yaufumu ya ufumu wanu.
7 Kom lungse ma suwohs ac srunga ma koluk. Ke sripa se inge God, su God lom, El sulekomla Ac okoaot mwe engan nu fom Yohk liki kutena tokosra saya.
Inu mumakonda chilungamo ndi kudana ndi zoyipa; choncho Mulungu, Mulungu wanu, wakukhazikani pamwamba pa anzanu pokudzozani ndi mafuta a chimwemwe.
8 Nuknuk lom keng ke foulin myrrh ac aloes; Mwet srital ke mwe on elos akpwarye kom in lohm su yunla ke ivory.
Mikanjo yanu yonse ndi yonunkhira ndi mure ndi aloe ndi kasiya; kuchokera ku nyumba zaufumu zokongoletsedwa ndi mnyanga wanjovu nyimbo za zoyimbira zazingwe zimakusangalatsani.
9 Inmasrlon mutan fusr su muta inkul sum, oasr acn nutin tokosra, Ac kasra el tu layen layot ke tron lom Ac naweyukla ke mwe yun gold.
Ana aakazi a mafumu ali pakati pa akazi anu olemekezeka; ku dzanja lanu lamanja kuli mkwatibwi waufumu ali mu golide wa ku Ofiri.
10 O kom, mutan pisrla kien tokosra, porongo ma nga fahk uh. Mulkunla mwet lom ac sou lom.
Tamvera, iwe mwana wa mkazi ganizira ndipo tchera khutu; iwala anthu ako ndi nyumba ya abambo ako.
11 Oasku lom ac fah oru tuh tokosra elan lungse kom; El leum lom, ke ma inge kom enenu in aksol.
Mfumu yathedwa nzeru chifukwa cha kukongola kwako; mulemekeze pakuti iyeyo ndiye mbuye wako.
12 Mwet in acn Tyre elos ac fah use mwe lung nu sum; Mwet kasrup elos ac fah suk ohi ye motom.
Mwana wa mkazi wa ku Turo adzabwera ndi mphatso, amuna a chuma adzafunafuna kukoma mtima kwako.
13 Fisrak mutan el muta in lohm sin tokosra — el arulana oasku! Nuknuk lal orekla ke turet gold.
Wokongola kwambiri ndi mwana wa mfumu ali mʼchipinda mwake, chovala chake ndi cholukidwa ndi thonje ndi golide.
14 El nuknukyang ke sie nuknuk na kato, ac kokola el nu yurin tokosra. Mutan kulansap lal su welul Elos oayapa utukyak nu yurin tokosra.
Atavala zovala zamaluwamaluwa akupita naye kwa mfumu; anamwali okhala naye akumutsatira ndipo abweretsedwa kwa inu.
15 Ke engan ac insewowo elos tuku Ac utyak nu in lohm sin tokosra.
Iwo akuwaperekeza ndi chimwemwe ndi chisangalalo; akulowa mʼnyumba yaufumu.
16 Ac kom, O Tokosra, ac fah pus wen nutum Tuh elos in aol mwet matu lom in tokosra, Ac kom ac fah oru tuh elos in mwet kol fin faclu nufon.
Ana ako aamuna adzatenga malo a makolo ako; udzachititsa kuti akhale ana a mfumu mʼdziko lonse.
17 On soko inge ac fah oru tuh inem in esamyuk nwe tok, Ac mwet nukewa ac fah kaksakin kom ma pahtpat.
Ndidzabukitsa mbiri yako mʼmibado yonse; choncho mitundu yonse idzakutamanda ku nthawi za nthawi.

< Psalm 45 >