< 시편 114 >

1 이스라엘이 애굽에서 나오며 야곱의 집이 방언 다른 민족에게서 나올 때에
Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
2 유다는 여호와의 성소가 되고 이스라엘은 그의 영토가 되었도다
Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
3 바다는 이를 보고 도망하며 요단은 물러갔으며
Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
4 산들은 수양 같이 뛰놀며 작은 산들은 어린 양 같이 뛰었도다
mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
5 바다야, 네가 도망함은 어찜이며 요단아 네가 물러감은 어찜인고
Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
6 너희 산들아, 수양 같이 뛰놀며 작은 산들아 어린 양 같이 뛰놂은 어찜인고
inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
7 땅이여, 너는 주 앞 곧 야곱의 하나님 앞에서 떨지어다
Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
8 저가 반석을 변하여 못이 되게 하시며 차돌로 샘물이 되게 하셨도다
amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.

< 시편 114 >