< Zacarias 5 >

1 Kalpasanna, timmaliawak ken timmangadak ket adtoy, nakitak ti maysa nga agtaytayab a nalukot a pagbasaan!
Ndinayangʼananso ndipo taonani ndinaona chikalata chimene chimawuluka.
2 Kinuna ti anghel kaniak, “Ania ti makitkitam?” Insungbatko, “Makitkitak ti maysa a nalukot a pagbasaan a duapulo a kadapan ti kaatiddogna ken sangapulo a kadapan ti kaakabana.”
Mngelo uja anandifunsa kuti, “Kodi ukuona chiyani?” Ndinayankha kuti, “Ndikuona chikalata chikuwuluka, mulitali mwake mamita asanu ndi anayi ndipo mulifupi mwake mamita anayi ndi theka.”
3 Ket kinunana kaniak, “Daytoy ti lunod nga agsaknap iti entero a daga ti Juda, ta manipud ita, mapapanawto ti tunggal agtatakaw segun iti nailanad iti maysa a paset ti pagbasaan, idinto a mapapanaw amin dagiti agsapata iti ulbod, segun iti nailanad iti sabali a paset ti pagbasaan, maitutop kadagiti sasaoda.
Ndipo mngeloyo anandiwuza kuti, “Awa ndi matemberero amene akupita pa dziko lonse lapansi; potsata zimene zalembedwa mʼkati mwa chikalatamo, aliyense wakuba adzachotsedwa, ndipo potsata zomwe zalembedwa kunja kwake, aliyense wolumbira zabodza adzachotsedwanso.
4 'Iyegkonto daytoy a lunod' —daytoy ket pakaammo ni Yahweh a Mannakabalin-amin, 'sumrekto ngarud daytoy iti balay ti agtatakaw ken iti balay ti tao nga agsapata iti ulbod babaen iti naganko. Agtalinaed daytoy iti balayna ket ibusen daytoy dagiti kayo ken batbato iti balay.'”
Yehova Wamphamvuzonse akunena kuti, ‘Temberero limeneli ndidzalitumiza, ndipo lidzalowa mʼnyumba ya munthu wakuba ndi munthu wolumbira zabodza mʼdzina langa. Lidzakhala mʼnyumbamo mpaka kuyiwonongeratu, matabwa ake ndi miyala yake yomwe.’”
5 Kalpasanna, nagparang ti anghel a nakisarsarita kaniak ket kinunana kaniak, “Tumangadka ket kitaem ti sumungsungad!”
Kenaka mngelo amene amayankhula nane uja anabwera patsogolo panga ndipo anandiwuza kuti, “Kweza maso ako tsopano kuti uwone kuti ndi chiyani chikubwerachi.”
6 Kinunak, “Ania daytoy?” Kinunana, “Maysa daytoy a basket a sumungsungad a naglaon iti maysa nga efa. Daytoy dagiti nadagsen a basolda iti entero a daga.”
Ndinafunsa kuti, “Kodi chimenechi nʼchiyani?” Mngeloyo anayankha kuti, “Limeneli ndi dengu loyezera.” Ndipo anawonjezera kunena kuti, “Umenewu ndi uchimo wa anthu mʼdziko lonse.”
7 Ket naingato ti buli a kalub ti basket, ket adda maysa a babai a nakatugaw iti uneg daytoy!
Pamenepo chovundikira chake chamtovu chinatukulidwa, ndipo mʼdengumo munali mutakhala mkazi.
8 Kinuna ti anghel, “Ibagbagi daytoy a babai ti Kinadangkes!” Ket intalmegna ti babai iti uneg ti basket sana inkabil ti buli a kalub ti basket.
Mngeloyo anati, “Chimenechi ndi choyipa,” ndipo anamukankhira mkaziyo mʼdengu muja, nabwezera chovundikira chamtovu chija pamwamba pake.
9 Timmangadak ket nakitak ti dua a babbai nga umas-asideg kaniak, ken adda angin kadagiti payakda—ta addaanda kadagiti payak a kasla kadagiti payak ti kannaway. Intayabda ti basket iti nagbaetan ti daga ken langit.
Kenaka ndinayangʼananso, ndipo ndinaona akazi awiri akuwuluka kubwera kumene kunali ine; akuwuluzika ndi mphepo. Iwo anali ndi mapiko ngati a kakowa, ndipo ananyamula dengu lija, kupita nalo pakati pa mlengalenga ndi dziko lapansi.
10 Isu a kinunak iti anghel a nakisarsarita kaniak, “Sadino ti pangipananda iti basket?”
Ine ndinafunsa mngelo amene amayankhula nane kuti, “Dengulo akupita nalo kuti?”
11 Kinunana kaniak, “Ipanda ti basket idiay daga ti Siniar tapno mangipatakderda iti templo para iti daytoy, tapno inton nakasaganan ti templo, maikabilto ti basket sadiay, iti naisagana a pagbatayanna.”
Iye anayankha kuti, “Ku dziko la Babuloni kuti akalimangire nyumba. Nyumbayo ikadzatha, adzayikamo dengulo.”

< Zacarias 5 >