< Job 42 >

1 Kalpasanna, simmungbat ni Job kenni Yahweh ket kinunana,
Pamenepo Yobu anayankha Yehova kuti,
2 “Ammok a maaramidmo amin a banbanag, nga awan ti panggepmo a mabalin a malapdan.
“Ndikudziwa kuti Inu mungathe kuchita zinthu zonse; chimene mufuna kuchita wina sangaletse konse.
3 Sinaludsodmo kaniak, 'Siasino daytoy nga awanan pannakaammo a nangyeg iti kinasipnget kadagiti panggepko?' Ngarud, nakaibagaak kadagiti banbanag a saanko a maawatan, banbanag a narigatko unay a maawatan, a saanko nga ammo ti kaipapananna.
Munandifunsa kuti, ‘Kodi ndiwe yani amene ukufuna kusokoneza uphungu wanga ndi mawu opanda nzeru? Zoonadi ndinayankhula zimene sindinazimvetse, zinthu zodabwitsa kwambiri kwa ine zimene sindinazidziwe.
4 Kinunam kaniak, 'Ita, dumngegka, ket agsaoak; adda banbanag a damagek kenka, ket ibagam kaniak dagitoy.'
“Inu munandiwuza kuti, ‘Mvetsetsa tsopano ndipo ndidzayankhula; ndidzakufunsa ndipo iwe udzandiyankhe.’
5 Nangngegak ti maipapan kenka babaen kadagiti lapayagko, ngem ita makitkitanakan dagiti matak.
Ndinkangomva za Inu ndi makutu anga, koma tsopanonso ndakuonani ndi maso anga.
6 Isu a kagurak ti bagik; agbabawiak babaen kadagiti tapok ken dapdapo.”
Nʼchifukwa chake ndi kuchita manyazi, ndikulapa podzithira fumbi ndi phulusa.”
7 Ket napasamak a kalpasan nga imbagana dagitoy a sasao kenni Job, kinuna ni Yahweh kenni Elifaz a taga-Teman, “Napasgedan ti pungtotko kenka ken iti dua a gagayyemmo ta saanyo nga imbaga ti umno a banag maipanggep kaniak, a kas iti inaramid ni Job nga adipenko.
Yehova atayankhula ndi Yobu mawu amenewa anawuza Elifazi wa ku Temani kuti, “Ine ndakukwiyira pamodzi ndi abwenzi ako awiri, chifukwa simunayankhule zabwino za Ine, monga mmene wayankhulira mtumiki wanga Yobu.
8 Ita ngarud, mangalakayo iti pito a kalakian a baka ken pito a kalakian a karnero, mapankayo kenni Job nga adipenko ket mangidatagkayo para iti bagiyo iti daton a mapuoran. Ikararagannakayonto ni Job nga adipenko ket denggekto ti kararagna, tapno saankayo a dusaen iti kinamaagyo. Saanyo nga imbaga ti umno a maipanggep kaniak, a kas iti inaramid ni Job nga adipenko.”
Kotero tsopano mutenge ngʼombe zazimuna zisanu ndi ziwiri ndi nkhosa zazimuna zisanu ndi ziwiri ndi kupita nazo kwa mtumiki wanga Yobu kuti mukapereke nsembe zopsereza. Mtumiki wanga Yobu adzakupemphererani, ndipo Ine ndidzalandira pemphero lake. Sindidzakuchitirani kanthu molingana ndi uchitsiru wanu. Inu simunayankhule zabwino za Ine, monga anayankhulira Yobu mtumiki wanga.”
9 Isu a napan da Elifaz a taga-Teman, ni Bildad a taga-Shuhit, ken ni Zofar a taga-Naamat ket inaramidda ti imbilin ni Yahweh kadakuada, ket inawat ni Yahweh ni Job.
Motero Elifazi wa ku Temani, Bilidadi wa ku Suki ndi Zofari wa ku Naama anachita zimene Yehova anawawuza ndipo Yehova anamvera pemphero la Yobu.
10 Idi nagkararag ni Job para kadagiti gagayyemna, insubli ni Yahweh dagiti kinabaknangna. Inikkan ni Yahweh isuna iti mamindua a daras a kaadu dagiti sanikua nga adda kenkuana idi.
Yobu atawapempherera abwenzi ake aja, Yehova anamubwezera chuma chake ndipo anamupatsa mowirikiza kuposa zomwe anali nazo kale.
11 Ket amin dagiti kakabsat ni Job a lallaki, ken amin a kakabsatna a babbai, ken amin a gagayyemna idi — napanda kenkuana ket nakipanganda iti balayna. Nakipagladingitda kenkuana ken liniwliwada isuna maipanggep kadagiti amin a didigra nga impalak-am ni Yahweh kenkuana. Amin a tattao ket nangted kenni Job iti maysa a pidaso ti pirak ken maysa a balitok a singsing.
Abale ake ndi alongo ake onse, kuphatikizapo onse amene ankamudziwa kale, amabwera kwa iye nʼkudzadya naye chakudya mʼnyumba mwake. Iwo anamutonthoza ndi kumupepesa chifukwa cha mavuto onse amene Yehova analola kuti amugwere. Aliyense wa iwowa anamupatsa ndalama ndi mphete yagolide.
12 Ad-adda pay a binendisionan ni Yahweh ti maudi a paset ti biag ni Job ngem ti immuna; addaan isuna iti sangapulo ket uppat a ribu a karnero, innem a ribu a kamelio, sangaribu a pares a baka, ken sangaribu a kabaian nga asno.
Yehova anadalitsa Yobu pa masiku ake otsirizawa kupambana poyamba paja. Iye anali ndi nkhosa 14,000, ngamira 6,000, ngʼombe zantchito 2,000 ndi abulu aakazi 1,000.
13 Naaddaan met isuna iti pito nga annak a lallaki ken tallo a babbai.
Anaberekanso ana aamuna asanu ndi awiri ndi ana aakazi atatu.
14 Pinanagananna ti inauna nga anakna a babai iti Jemimah, Keziah ti maikadua, ken Kerenhapuch ti maikatlo.
Mwana wake wamkazi woyamba anamutcha Yemima, wachiwiri anamutcha Keziya, wachitatu anamutcha Kereni Hapuki.
15 Iti entero a daga, awanen ti masarakan a babbai a napinpintas ngem kadagiti annak ni Job a babbai. Inikkan ida ti amada iti tawid kasta met kadagiti annakna a lallaki.
Mʼdziko monsemo munalibe akazi okongola ngati ana a Yobu, ndipo abambo awo anawapatsa cholowa pamodzi ndi alongo awo.
16 Kalpasan daytoy, nagbiag pay ni Job iti sangagasut ket uppat a pulo a tawen; nakadennana pay dagiti annakna a lallaki ken dagiti appokona agingga iti maikapat a henerasion.
Zitachitika zimenezi, Yobu anakhala ndi moyo zaka 140. Iye anaona zidzukulu zake mpaka mʼbado wachinayi.
17 Kalpasanna, natay ni Job gapu iti kinalakayna unay a ginanasna ti nagbiag.
Potsiriza, Yobu anamwalira ali nkhalamba ya zaka zochuluka kwambiri.

< Job 42 >