< Haggeo 1 >

1 Iti maikadua a tawen a panagturay ni Dario a kas ari, iti umuna nga aldaw ti maika-innem a bulan, immay ti sao ni Yahweh babaen iti ima ni Haggeo a profeta, ti sao ket para iti gobernador ti Juda a ni Zerubbabel a putot a lalaki ni Salatiel ken para kenni Josue a kangatoan a padi a putot a lalaki ni Josadak ket kinunana:
Chaka chachiwiri cha Mfumu Dariyo, tsiku loyamba la mwezi wachisanu ndi chimodzi, Yehova anapatsa mneneri Hagai uthenga wopita kwa Zerubabeli mwana wa Sealatieli, bwanamkubwa wa Yuda, ndiponso kwa mkulu wa ansembe Yoswa mwana wa Yehozadaki:
2 “Kastoy ti kuna ni Yahweh a mannakabalin-amin: 'Kinuna dagitoy a tattao, “saan pay a dimteng ti tiempo nga ipatakdertayo ti balay ni Yahweh.”
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu awa amanena kuti, ‘Nthawi sinafike yoti nʼkumanga Nyumba ya Yehova.’”
3 Isu nga immay ti sao ni Yahweh babaen iti ima ni Haggeo a profeta ket kinunana,
Tsono Yehova anayankhula ndi mneneri Hagai kuti,
4 “Tiempo kadin nga agnaedkayo kadagiti nalpasen a balayyo idinto a nadadael daytoy a balay?
“Kodi ino ndi nthawi yoti inuyo muzikhala mʼnyumba zomanga bwino, pamene Nyumba yangayi ikanali bwinja?”
5 Isu nga ita, kastoy ti ibagbaga ni Yahweh a mannakabalin-amin: 'Panunotenyo dagiti ar-aramidenyo!
Tsono zimene Yehova Wamphamvuzonse akunena ndi izi, “Ganizirani bwino njira zanu.
6 Nagmulakayo iti adu a bukel ngem bassit ti apityo; mangankayo ngem saankayo a mabsog; uminomkayo iti arak ngem saankayo a mabartek. Agkaweskayo ngem saan a maimengan dagiti bagbagiyo, ken agur-urnong iti kuarta ti mangmangged tapno ipisokna laeng iti supot a napnoan ti abot”
Mwadzala zambiri, koma mwakolola zochepa. Mumadya, koma simukhuta. Mumamwa, koma ludzu lanu silitha. Mumavala, koma simumva kutentha. Mumalandira malipiro, koma ndalama zanu zimatha ngati mwaziyika mʼthumba lobowoka.”
7 Kastoy ti ibagbaga ni Yahweh a Mannakabalin-amin: “Panunotenyo dagiti ar-aramidenyo!
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ganizirani bwino njira zanu.
8 Sumang-atkayo iti bantay, mangalakayo iti kayo, ket bangonenyo ti balayko; maragsakanakto iti daytoy ket maidayawakto!'.
Pitani ku mapiri ndipo mukatenge matabwa oti mudzamangire Nyumba yanga, kuti ndikondwere nayo ndi kulandiramo ulemu,” akutero Yehova.
9 'Nagsapulkayo iti adu ngem kitaenyo! Bassit ti naiyawidyo, ta pinatayab ko daytoy! Apay?'—daytoy ti pakaammo ni Yahweh a Mannakabalin-amin! 'Gapu ta nadadael ti balayko, idinto a maragragsakan ti amin a tao iti bukodna a balay.'
“Mumayembekezera zambiri, koma taonani mwapeza pangʼono pokha. Zimene munazibweretsa ku nyumba, Ine ndinazimwaza. Nʼchifukwa chiyani?” Akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Chifukwa Nyumba yanga ikanali bwinja, pamene aliyense wa inu watanganidwa kumanga nyumba yake.
10 Gapu iti daytoy, ipaidam dagiti langit ti linna-aw kadakayo, ket ipaidam ti daga ti bungana.
Choncho, chifukwa cha inu, mitambo yaleka kugwetsa mvula ndipo dziko lapansi laleka kutulutsa zomera.
11 Pinagtikagko dagiti daga ken dagiti bantay, dagiti bukel ken ti baro nga arak, ti lana ken ti apit ti daga, dagiti tattao ken narurungsot nga ayup, ken amin nga aramid dagiti imayo!'''
Ndabweretsa chilala pa minda ndi pa mapiri, chilala chawumitsa tirigu, mphesa, mafuta a olivi ndi chilichonse chimene chimamera pa nthaka, pa anthu ndi pa ngʼombe, ndi pa ntchito zonse za manja anu.”
12 Ket ni Zerubbabel a putot a lalaki ni Salatiel ken ni Josue a kangatoan a padi a putot a lalaki ni Josadak, ken amin a nabatbati kadagiti tattao ket nagtulnogda iti timek ni Yahweh a Diosda, ken kadagiti sasao ni Haggeo a profeta, gapu ta ni Yahweh a Diosda ti nangibaon kenkuana. Ket nagbuteng dagiti tattao iti rupa ni Yahweh.
Pamenepo Zerubabeli mwana wa Sealatieli, mkulu wa ansembe Yoswa mwana wa Yehozadaki, ndi anthu onse otsala anamvera mawu a Yehova Mulungu wawo ndi uthenga wa Hagai, chifukwa anatumidwa ndi Yehova Mulungu wawo. Ndipo anthuwo anaopa Yehova.
13 Ket ni Haggeo, a mensahero, insaona ti mensahe ni Yahweh kadagiti tattao a kinunana, ''“Addaak kadakayo!'—daytoy ti pakaammo ni Yahweh!”
Tsono Hagai, mthenga wa Yehova, anapereka kwa anthuwo uthenga uwu wa Yehova: “Ine ndili nanu,” akutero Yehova.
14 Tinignay ngarud ni Yahweh ti espiritu ti gobernador ti Juda a ni Zerubbabel a putot a lalaki ni Salatiel, ken ti espiritu ti kangatoan a padi a ni Josue a putot a lalaki ni Josadak, ken ti espiritu dagiti amin a nabatbati kadagiti tattao, isu a napanda ket nagtrabahoda iti balay ni Yahweh a Diosda.
Kotero Yehova anakhudza mtima wa Zerubabeli mwana wa Sealatieli, bwanamkubwa wa Yuda, mtima wa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndiponso mitima ya anthu onse otsala. Iwo anabwera ndi kuyamba ntchito yomanga Nyumba ya Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wawo,
15 Iti maika-duapulo ket uppat nga aldaw iti maika-innem a bulan, iti maikadua a tawen a panagturay ni Dario a kas ari.
pa tsiku la 24 la mwezi wachisanu ndi chimodzi, wa chaka chachiwiri cha Mfumu Dariyo.

< Haggeo 1 >