< Jérémie 41 >

1 Parole du Seigneur qui vint à Jérémie quand Nabuchodonosor, roi de Babylone, et toute son armée et toute la terre qu'il gouvernait, combattirent contre Jérusalem et contre toutes les villes de Juda, disant:
Pa mwezi wachisanu ndi chiwiri Ismaeli mwana wa Netaniya, mdzukulu wa Elisama amene anali wa banja laufumu ndiponso mmodzi wa atsogoleri a ankhondo a mfumu, anabwera ku Mizipa kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ndi anthu khumi. Pamene ankadya naye kumeneko,
2 Voici ce que dit le Seigneur: Va trouver Sédécias, roi de Juda, et dis-lui: Ainsi parle le Seigneur: Cette ville sera livrée au roi de Babylone, et il la prendra, et il la brûlera par le feu.
Ismaeli mwana wa Netaniya pamodzi ndi anthu khumi aja anayimirira ndi kupha ndi lupanga Gedaliya mwana wa Ahikamu, mdzukulu wa Safani. Choncho anapha munthu amene mfumu ya ku Babuloni inamusankha kukhala bwanamkubwa wa dzikolo.
3 Et tu n'échapperas pas de ses mains; mais tu seras pris, tu seras livré entre ses mains, et tes yeux verront ses yeux, et tu iras à Babylone,
Ismaeli anaphanso Ayuda onse amene anali pamodzi ndi Gedaliya ku Mizipa, kuphatikizanso asilikali a Ababuloni amene anali ku Mizipako.
4 Cependant, écoute la parole du Seigneur, Sédécias, roi de Juda; voici ce que dit le Seigneur:
Mmawa mwake, anthu asanadziwe kuti Gedaliya waphedwa,
5 Tu mourras en paix; et, comme on a pleuré tes pères qui ont régné avant toi, on te pleurera aussi, disant: Hélas! Seigneur! et à ta mort on se frappera la poitrine à cause de toi; car telle est la sentence que j'ai prononcée, dit le Seigneur.
kunafika anthu 80 ochekera ku Sekemu, Silo ndi Samariya, amene anali atameta ndevu zawo, atangʼamba zovala zawo ndi kudzichekacheka. Iwowa anatenga chopereka cha ufa ndi lubani kuti adzapereke ku Nyumba ya Yehova.
6 Ainsi Jérémie dit toutes ces paroles au roi Sédécias en Jérusalem.
Ismaeli mwana wa Netaniya anachoka ku Mizipa akulira kupita kukakumana nawo. Atakumana nawo, iye anati, “Bwerani mudzaonane ndi Gedaliya mwana wa Ahikamu.”
7 Et l'armée du roi de Babylone combattait contre Jérusalem et contre les villes de Juda Lachis et Azica; car parmi les villes fortes de Juda celles-là n'étaient pas encore prises.
Atafika pakati pa mzinda, Ismaeli mwana wa Netaniya pamodzi ndi anthu amene anali naye anawapha anthuwo ndi kuwaponya mʼchitsime.
8 Voici la parole du Seigneur qui vint à Jérémie après que le roi Sédécias eut fait alliance avec le peuple pour publier la remise;
Koma anthu khumi a gululo anawuza Ismaeli kuti, “Musatiphe! Tili ndi tirigu ndi barele, mafuta ndi uchi, zimene tabisa mʼmunda.” Choncho anawasiya ndipo sanawaphere pamodzi ndi anzawo aja.
9 Afin que chacun affranchît son serviteur et sa servante, que l'Hébreu des deux sexes fût libre, et qu'il n'y eût plus de servitude en Juda.
Tsono chitsime chimene anaponyamo mitembo ya anthu amene anawaphawo pamodzi ndi mtembo wa Gedaliya chinali chimene mfumu Asa anachikumba poopsedwa ndi Baasa mfumu ya Israeli. Ismaeli mwana wa Netaliya anachidzaza ndi mitembo.
10 Et tous les grands changèrent d'avis, et tout le peuple qui était entré dans l'alliance, pour que chacun affranchît son serviteur et sa servante, et ils affranchirent
Pambuyo pake Ismaeli anatenga ukapolo anthu ena onse amene anali ku Mizipa: ana aakazi a mfumu pamodzi ndi ena onse amene anatsalira kumeneko, amene Nebuzaradani mtsogoleri wa asilikali olonda mfumu anapatsa Gedaliya mwana wa Ahikamu kuti akhale bwanamkubwa wawo. Ismaeli mwana wa Netaliya anatenga ukapolo anthuwa ndi kuwoloka nawo kumapita ku dziko la Aamoni.
11 Leurs serviteurs et leurs servantes.
Pamene Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri onse a ankhondo amene anali naye pamodzi anamva zoyipa zonse zimene Ismaeli mwana wa Netaniya anachita,
12 Et la parole du Seigneur vint à Jérémie, disant:
anatenga ankhondo awo onse kupita kukamenyana ndi Ismaeli mwana wa Netaniya. Anakamupeza kufupi ndi chidziwe chachikulu cha ku Gibiyoni.
13 Ainsi parle le Seigneur: J'ai fait alliance avec vos pères le jour où je les ai ramenés d'Égypte, de la maison de servitude, disant:
Pamene anthu onse amene Ismaeli anawagwira anaona Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi atsogoleri a ankhondo amene anali naye, anasangalala.
14 Lorsque six années seront révolues, tu affranchiras ton frère hébreu qui t'aura été vendu, et qui aura travaillé six ans pour toi; alors tu le renverras libre. Et ils ne m'ont pas écouté, et ils n'ont point prêté l'oreille à mes commandements.
Anthu onse amene Ismaeli anawagwira ukapolo ku Mizipa anabwerera ndi kupita kwa Yohanani mwana wa Kareya.
15 Et aujourd'hui ils se sont convertis, voulant faire ce qui est juste à mes yeux, pour que chacun proclamât la libération de son prochain; et ils ont fait alliance devant moi dans le temple où mon nom est invoqué.
Koma Ismaeli pamodzi ndi anthu ake asanu ndi atatu, anathawa Yohanani ndi kuthawira kwa Aamoni.
16 Puis vous avez changé d'avis et vous avez profané mon nom en promettant que chacun affranchirait son serviteur et sa servante; et vous ne les avez point renvoyés libres, maîtres d'eux-mêmes; vous les avez gardés, serviteurs et servantes.
Kenaka Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi atsogoleri onse a ankhondo amene anali naye anatsogolera anthu onse otsala a ku Mizipa amene anawapulumutsa kwa Ismaeli mwana wa Netaniya atapha Gedaliya mwana wa Ahikamu. Anthu amenewa anali: asilikali, akazi, ana ndi amuna ofulidwa otumikira mfumu amene anawatenga ku Gibiyoni.
17 A cause de cela, voici ce que dit le Seigneur: Vous ne m'avez point écouté pour proclamer la libération de vos frères. Et moi, voilà que je proclame votre expulsion par le glaive, par la peste et par la famine; je vous disperserai dans tous les royaumes de la terre.
Ndipo ananyamuka nayima ku Geruti Kimuhamu pafupi ndi Betelehemu pa ulendo wawo wopita ku Igupto
18 Et je livrerai les hommes qui ont rompu mon alliance, qui n'ont point maintenu l'alliance faite devant moi et confirmée par le veau qu'ils avaient préparé pour le sacrifice;
kuthawa Ababuloni. Iwo anaopa Ababuloniwo chifukwa Ismaeli mwana wa Netaniya anapha Gedaliya mwana wa Ahikamu, amene mfumu ya ku Babuloni inamuyika kukhala bwanamkubwa wa dzikolo.
19 Ainsi que les princes de Juda, et les grands, et les prêtres, et le peuple.
20 Et je les livrerai à leurs ennemis; et leurs cadavres seront en pâture aux oiseaux du ciel et aux bêtes des champs.
21 Et je livrerai aux mains de leurs ennemis Sédécias, roi de Judée, et ses princes; car l'armée du roi de Babylone ramènera ceux qui s'étaient quelque temps éloignés d'eux.
22 Voilà ce que j'ordonne, dit le Seigneur: Je les ramènerai sur cette terre, et ils combattront contre elle, et ils la prendront, et ils la brûleront par le feu; et je ferai des villes de Juda un désert où il n'y aura point d'habitants.

< Jérémie 41 >