< Psalms 70 >

1 God, please save me! Yahweh, come quickly to help me!
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
2 Humble those who are happy about my troubles/difficulties, and cause them to be disgraced/ashamed. Chase away those who are trying to kill me.
Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
3 I hope/desire that you will cause them to become dismayed and ashamed [because you have defeated them].
Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
4 [But] I hope/desire that all those who go to [worship] you will be very joyful [DOU]. I want those who love you because you saved them to shout repeatedly [HYP], “God is great!”
Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
5 As for me, I am poor and needy [DOU]; [so] God, come quickly to help me! Yahweh, you are the one who saves and helps me, [so please] come quickly!
Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.

< Psalms 70 >