< 詩篇 136 >
1 請眾感謝上主,因他寬仁,因為他的仁慈永遠常存。
Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
Yamikani Mulungu wa milungu.
Yamikani Ambuye wa ambuye,
Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
10 祂擊殺了埃及國的首生,因為祂的仁慈永遠常存。
Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
11 祂領以色列走出埃及境,因為祂的仁慈永遠常存。
Natulutsa Israeli pakati pawo,
12 祂伸出手臂施展了大能,因為祂的仁慈永遠常存。
Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
13 祂把紅海的水從中分開,因為祂的仁慈永遠常存。
Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
14 祂領以色列人海中步行,因為祂的仁慈永遠常存。
Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
15 祂淹沒法郎軍隊於海心,因為祂的仁慈永遠常存。
Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
16 祂率領百姓在曠野繞行,因為祂的仁慈永遠常存。
Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
17 祂嚴懲了最強悍的國君,因為祂的仁慈永遠常存。
Amene anakantha mafumu akuluakulu,
18 祂擊殺了極強盛的國王,因為祂的仁慈永遠常存。
Napha mafumu amphamvu,
19 祂殺死了阿摩黎王息紅,因為祂的仁慈永遠常存。
Siloni mfumu ya Aamori,
20 祂殺死敖格,巴商之君,因為祂的仁慈永遠常存。
Ogi mfumu ya Basani,
21 祂將異民地使選民佔領,因為祂的仁慈永遠常存。
Napereka dziko lawo ngati cholowa,
22 祂使己僕以色列人繼承,因為祂的仁慈永遠常存。
Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
23 祂懷念了我們遭難的人,因為祂的仁慈永遠常存。
Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
24 祂救拔我們脫離了仇人,因為祂的仁慈永遠常存。
Amene anatimasula kwa adani athu,
25 祂給一切生靈提供食品,因為祂的仁慈永遠常存。
Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
26 請眾感謝天主上居天庭,因為他的仁慈永遠常存。
Yamikani Mulungu wakumwamba,