< 約伯記 35 >
Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,
2 你說過:「我在天主前是正義的。」你想這話合理嗎﹖
“Kodi mukuganiza kuti mukukhoza? Mukunena kuti, ‘Ndine wolungama pamaso pa Mulungu.’
3 你還說過:「這與你何干﹖我若犯罪,我對你做了什麼﹖」
Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani, ndipo ndimapeza chiyani ndikapanda kuchimwa?’
“Ine ndikufuna ndikuyankheni inu pamodzi ndi abwenzi anu omwe.
Yangʼanani kumwamba ndipo muone mitambo imene ili kutali ndi inuyo.
6 你若犯罪,為他有什麼害處﹖你若作惡多端,又能加害他什麼﹖
Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani? Ngati machimo anu ndi ochuluka, zimenezo zimachita chiyani kwa Iye?
7 如果你為人正義,為他又有何益﹖或者他由你手中獲得什麼﹖
Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani? Kapena Iye amalandira chiyani chochokera mʼdzanja lanu?
8 你的惡行只能加害與你類似的人,你的正義也只能有益於世人。
Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo, ndipo chilungamo chanu chimakhudza anthu anzanu.
9 人因受暴虐過甚,必要哀號;因受強權的壓迫,必要呼籲。
“Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa; akufuna chithandizo kuti achoke pansi pa ulamuliro wa anthu amphamvu.
Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga, amene amatisangalatsa nthawi ya usiku,
11 使我們比地上的走獸更聰明,使我們比天上的飛鳥更有智慧的天主在那裏﹖」
amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi ndipo amatipatsa nzeru kupambana mbalame zowuluka?’
12 他們雖呼喊,天主卻不答應,這是因為惡人傲慢的原故。
Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye chifukwa cha kudzikuza kwa anthu oyipa.
13 他們空喊亂叫,天主決不俯聽,全能者決不垂視。
Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake; Wamphamvuzonse sasamalira zimenezi.
14 何況你說過:「你看不見他;但你的案件已放在他面前,你應等待他!」
Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti Iye saona zimene zikuchitika. Iye adzaweruza molungama ngati inu mutamudikira
15 你還說過:「他沒有發怒施罰,似乎不很理會罪過。」
ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango, zoyipa zambiri zimene anthu amachita,
16 的確,約伯開口盡說空話;由於無知,說了許多妄言。
abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake, mukungochulukitsa mawu opanda nzeru.”