< 1 Kawrin 4 >
1 Hatdawkvah ayâ ni maimanaw teh Khrih e san hoi Cathut e hrolawk hno ka kuemkung lah na pouk awh naseh.
Choncho tsono anthu atione ife monga atumiki a Khristu, ndiponso ngati osunga zinsinsi za Mulungu.
2 Hno kuemkung teh yuemkamcu telah ayâ ni panue e tami han.
Chofunika kwambiri nʼchakuti amene apatsidwa udindo oyangʼanira aonetse kukhulupirika.
3 Nangmouh hoi alouknaw ni hai kai hah lawkkam na cak hoeh telah lawk na ceng awh e heh hno kathoenge doeh. Kai teh kamahoima hai lawk ka ceng hoeh.
Ine ndilibe nazo kanthu ngati ndiweruzidwa ndi inu kapena khothi lina lililonse. Ndithu, inenso sindidziweruza ndekha.
4 Ka pouknae a thoung. Hatei, hottelah ka o dawkvah kai teh tamikalan telah khoe e lah kaawm hoeh. Kai lawkcengkung teh Bawipa doeh.
Chikumbumtima changa sichikunditsutsa, koma sikuti ndine wolungama. Wondiweruza ine ndi Ambuye.
5 Hatdawkvah, atueng a pha hoehnahlan, apihai lawkceng awh hanh. Bawipa a tho totouh ring awh. Ahni ni hmonae koe hro e pueng angnae dawk a kamnue sak vaiteh, tami e pouknae puenghai a kamnue sak han. Hattoteh tami pueng ni Cathut koehoi oupnae a coe awh han.
Chomwecho musaweruze nthawi yoweruza isanakwane. Dikirani mpaka Ambuye atabwera. Iye adzaonetsa poyera zimene zabisika mu mdima ndipo adzaonetsa maganizo a mʼmitima ya anthu. Pa nthawi imeneyo aliyense adzalandira kwa Mulungu chiyamiko.
6 Hmaunawnghanaw, Cakathoung dawk thut lah kaawm e tapuet laihoi ayânaw bari kawi nahoeh tie lawk hah kaimouh roi koehoi kamtu thai awh nahan, buet touh ni buet touh e lathueng na kâoup awh hoeh nahan, kai hoi Apollos bangnue lahoi hete hnonaw hah nangmouh hanelah ka pâpho.
Tsono abale, ndapereka chitsanzo cha ine mwini ndi Apolo kuti mupindule. Phunzirani kwa ife tanthauzo la mawu akuti, “Musamapitirire zimene Malemba akunena,” kuti musamanyade pamene wina aposa mnzake.
7 Apini maw nangmouh na talue sak awh. Na kamtu e laipalah ahmaloe hoi na thung kaawm e hno ao maw. Na kamtu e lah awm pawiteh na kamtu hoeh e patetlah bangkongmaw na kâoup vaw.
Pakuti ndani amakusiyanitsani ndi wina aliyense? Nʼchiyani muli nacho chimene simunalandire? Ndipo ngati munalandira, bwanji mumadzitukumula ngati kuti simunalandire?
8 Na kuep awh toe. Na bawi awh toe. Kaimouh laipalah na uk awh toe. Kaimouh hah nangmouh hoi rei uk thai nahanelah na uk awh katang pawiteh ahawi.
Inu muli nazo kale zonse zimene mufuna! Inu mwalemera kale! Inu mwayamba kale kulamulira ife! Ndilakalaka mukanakhaladi mafumu kuti ife tikhale nawo mafumu pamodzi ndi inu.
9 Kai niteh, thei hane naw patetlah Cathut ni kaimouh gunceinaw a hnukteng koe lah na ta awh toe telah ka pouk. Bangkongtetpawiteh, kalvantaminaw hmalah, hoi talai taminaw hmalah, talaivan abuemlah ni khet han kawi lah ka o awh.
Pakuti kwa ine zikuoneka ngati kuti Mulungu watiyika ife atumwi pachionetsero, kumapeto kwa mndandanda, monga anthu oweruzidwa kuti akaphedwe mʼmabwalo. Ife tayikidwa kuti tionekere ku dziko lonse, kwa angelo ndi anthu.
10 Kaimouh teh Khrih hanelah tamipathu lah ka o awh. Hatei nangmouh teh Khrih dawk na lungang awh. Kaimouh teh ka thayoun awh. Hatei nangmanaw teh na thao awh. Nangmouh teh bari kaawm e lah na o awh. Hatei kaimouh teh hnephnap e lah ka o awh.
Ife ndife opusa chifukwa cha Khristu, koma inu ndinu anzeru mwa Khristu! Ife ndife ofowoka koma inu ndinu amphamvu! Inu ndinu olemekezeka koma ife ndife opeputsidwa!
11 Kaimouh teh atu raw vonhlamrinci hoi, caici lah o hoi, rektap e lah ka o awh teh, im laipalah,
Mpaka pano tili ndi njala ndi ludzu, tili ndi sanza, tikuzunzidwa, tilibe nyumba.
12 mae kut hoi thaw ka tawk awh. Na pathoe awh navah yawhawinae lah ka pouk awh. Rektapnae kâhmo navah ka panguep awh.
Timagwira ntchito molimbika ndi manja athu. Akamatitemberera, ife timadalitsa; tikasautsidwa, ife timapirira.
13 Na dudam awh torei teh, lungpatawnae kamnue sak pouh awh. Atu sittouh tami pueng ni na takhoe awh, talaivan e songnawng patetlah na pouk awh.
Pamene atilalatira timayankha mwachifundo. Mpaka pano takhala ngati zinyalala za dziko, monga zakudzala za dziko lapansi.
14 Nangmouh kaya sak nahanlah ka ngai dawk hete ca ka thut e nahoeh. Ka pahren e ka canaw patetlah na kâhruetcuet awh nahanlah hete ca na thut pouh e doeh.
Sindikulemba izi kuti ndikuchititseni manyazi, koma kukuchenjezani monga ana anga okondedwa.
15 Bangkongtetpawiteh nangmouh dawk Khrih kong na ka cangkhai e thong hra touh kaawm nakunghai, na pa moipap hoeh. Khrih Jisuh dawkvah kamthang kahawi lahoi na khe awh.
Ngakhale muli ndi anthu 10,000 okutsogolerani mwa Khristu, mulibe abambo ambiri, popeza mwa Khristu Yesu, ine ndakhala abambo anu kudzera mu Uthenga Wabwino.
16 Hatdawkvah, kaie nuen na out awh nahanlah na hroecoe awh.
Chifukwa chake ndikukupemphani kuti munditsanze ine.
17 Hot kecu dawkvah, Bawipa dawk yuemkamcu e ka pahren e ka capa Timote nangmouh koe ka patoun. Ahni ni kho tangkuem e kawhmoun pueng koe kai ni ka cangkhai e patetlah Khrih Jisuh dawk kai ni ka dawn e lamthung hah nangmouh bout na panue sak awh han doeh.
Chifukwa cha ichi ndikutumiza kwa inu Timoteyo, mwana wanga amene ndimamukonda, amene ndi wokhulupirika mwa Ambuye. Adzakukumbutsani inuyo za moyo wanga mwa Khristu Yesu, umene ukugwirizana ndi zimene ndimaphunzitsa paliponse mu mpingo uliwonse.
18 Kai nangmouh koe tho mahoeh telah tami tangawn ni a pouk awh teh, a kâoup awh.
Ena mwa inu mukudzitukumula, ngati kuti sindingabwere kwanu.
19 Bawipa ni a ngainae awm pawiteh karanglah ka tho han. Hat toteh, ahnimouh kâoupnae dawk laipalah, ahnimae bahu hah ka panue han doeh.
Koma ndibwera kwanuko posachedwapa, ngati Ambuye alola, ndipo ndi pamene ndidzadziwe osati zimene anthu odzitukumulawa akuyankhula, koma kuti mphamvu zawo nʼzotani.
20 Bangkongtetpawiteh, Cathut uknaeram teh lawk dawk kaawm e nahoeh, bahu dawk doeh ao.
Pakuti ufumu wa Mulungu si mawu chabe koma mphamvu.
21 Bangmaw na ngaihnawn awh, bongpai hoi na ou ka tho han, lungpatawnae, lungdolungnemnae hoi na ou ka tho han.
Kodi musankha chiyani? Kodi ndidzabwere ndi chikwapu, kapena mu chikondi ndiponso mwa mzimu wofatsa?