< 2 Kawrin 1 >

1 Kai Pawl, Cathut ngainae lahoi Jisuh Khrih e guncei lah kaawm e, hoi ka nawngha Timote ni Kawrin kho kaawm e Cathut e kawhmoun hoi Akhaia ram pueng dawk kaawm e tami kathoungnaw koe ca na patawn awh.
Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu mwachifuniro cha Mulungu, pamodzi ndi mʼbale wathu Timoteyo, Kulembera mpingo wa Mulungu mu Korinto, pamodzi ndi oyera mtima onse mu Akaya monse.
2 Maimae Pa Cathut koehoi Bawipa Jisuh Khrih koe e lungmanae hoi roumnae teh nangmouh koe awm lawiseh.
Mukhale ndi chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu.
3 Maimae Bawipa Jisuh Khrih e Pa Cathut pahrennae hoi ka kawi e maimae na Pa, kabawmkung Bawi lah kaawm e Cathut teh yawhawinae awm lawiseh.
Alemekezeke Mulungu, Atate a Ambuye athu Yesu Khristu, Atate achifundo chonse, Mulungu wachitonthozo chonse.
4 Maimouh ni reithainae a phunphun khang awh navah, lung na pahawi awh. Bangkongtetpawiteh maimouh ni coe awh e lungpahawinae hoiyah reithainae aphunphun kakhangnaw hah lungpahawi thai nahane doeh.
Iye amatitonthoza ife mʼmavuto athu onse, kuti ifenso tithe kutonthoza amene ali pavuto lililonse ndi chitonthozo chimene ife tilandira kwa Mulungu.
5 Hote Khrih ni a khang e reithainae teh moipap dawkvah, Khrih kecu dawk maimouh ni coe e lungpahawinae hai moipap van.
Pakuti monga momwe tili mʼmasautso pamodzi ndi Khristu, momwemonso Khristu amatitonthoza kwambiri.
6 Maimouh ni reithai patang khang awh pawiteh nangmouh lungpahawinae hoi rungngangnae doeh. Kaimouh ni hawinae ka hmu awh e hai nangmouh ni hawinae na hmu awh nahane doeh. Hote hawinae teh kaimouh ni ka hmu e reithainae koe nangmouh ni lungdonae hoi khang thai nahan thaonae lah ao.
Ngati ife tikusautsidwa, nʼchifukwa choti inu mutonthozedwe ndi kupulumutsidwa. Ngati ife tikutonthozedwa nʼchifukwa choti inu mutonthozedwe, ndi chitonthozo chimene chimabweretsa mwa inu kupirira kosawiringula pa zosautsa zomwe timasauka nazo ife.
7 Hatdawkvah nangmouh koe ka ngaihawinae a cak. Bangkongtetpawiteh, nangmouh ni reithai khangnae na phukhai e patetlah ahawinae hai reirei na khangkhai awh, tie ka panue awh.
Ndipo chiyembekezo chathu pa inu nʼcholimba chifukwa tikudziwa kuti monga momwe mumamva zowawa pamodzi nafe, momwemonso mumatonthozedwa nafe pamodzi.
8 Hmaunawnghanaw, Asia ram vah kaimouh koe runae ka phat e hah, nangmouh panuek laipalah o sak han ka ngai hoeh. Kaimouh ni a rucatnae khang thai hoeh totouh ka kâhmo awh dawk hring hane patenghai ngaihawinae awmhoeh.
Abale, sitikufuna kuti mukhale osadziwa za masautso amene tinakumana nawo mʼchigawo cha Asiya. Tinapanikizidwa koopsa kuposa muyeso woti nʼkutha kupirira, mwakuti sitinkadziwa kuti nʼkukhalabe ndi moyo.
9 Kaimouh due han totouh lawk a tâtueng awh toe telah ka panue. Hatei telah bout onae teh kaimouh ni mahoima kâuepnae tho laipalah kadoutnaw kathâw sakkung, Cathut kângue nahane doeh.
Zoonadi, tinamva mʼmitima mwathu chilango cha imfa. Koma izi zimachitika kuti tisangodzidalira mwa ife tokha koma Mulungu yemwe amaukitsa akufa.
10 Cathut ni hettelah e taki kaawm e duenae koehoi kaimouh na hlout sak. Hmalah hai bout na hlout sak han telah Bawipa dawk ka ngaihawi.
Mulungu watilanditsa ku zoopsa zotere za imfa, ndipo adzatilanditsanso. Ife tayika chiyembekezo chathu pa Iyeyo kuti adzapitiriza kutilanditsabe.
11 Nangmouh ni hai ratoumnae hoi kaimouh hah na kabawp teh, taminaw e ratoumnae dawk kaimouh ni ka hmu awh e poehnonaw khet navah, taminaw ni kaimae yueng lah lunghawinae lawk a dei awh han.
Mutithandize potipempherera. Pamenepo ambiri adzathokoza mʼmalo mwathu, chifukwa cha chisomo chake poyankha mapemphero a anthu ambiri.
12 Kaimouh ni kâoup kawi e teh talaivan lungangnae laipalah Cathut e lungmanae dawk Cathut koehoi ka tho e lungthin thoungnae hoi kahring awh e hah lawkpanuesaknae lung ni na panue sak.
Tsono chonyadira chathu nʼchakuti, chikumbumtima chathu chimatitsimikizira kuti timakhala bwino mʼdziko lapansi, makamaka pa ubale wathu ndi inu. Takhala moona mtima ndi oyera mtima. Sitinachite chomwechi mwa nzeru ya dziko lapansi koma monga mwa chisomo cha Mulungu.
13 Kaimouh ni nangmouh koe ca ka thut awh navah, nangmouh ni na touk thai hane hoi na thai thai nahane hloilah alouke ka thut hoeh.
Pakuti sitikukulemberani zoti simungawerenge kapena kumvetsetsa.
14 Atuvah nangmouh ni kaimouh be na panuek awh hoeh ei, maimae Bawipa Jisuh e hnin nah kaimouh teh nangmouh hanlah kâoupnae lah na o awh e patetlah, nangmouh hai kaimouh hanelah, kâoupnae lah na o awh e hah na panue awh han telah ka ngaihawi.
Monga mwamva pangʼono chabe, ndikuyembekeza kuti mudzamvetsa kwenikweni, kuti mutha kutinyadira monga ife tidzakunyadirani, pa tsiku la Ambuye Yesu.
15 Hettelah mangkhak katang dawkvah nangmouh teh hawinae bout na coe awh hanlah nangmouh koe ahmaloe ka tho han telah ka kâcai.
Popeza ndinatsimikiza mtima za ichi, nʼchifukwa chake ndinafuna kuti poyamba, ndidzakuchezereni kuti mupindule pawiri.
16 Nangmouh koe lah ka cei vaiteh Masidonia ram lah ka cei hnukkhu, haw hoi nangmouh koe ka tho vaiteh, Judah ram totouh nangmouh ni na thak a han telah ka pouknae ao.
Ndinafuna kuti ndidzakuchezereni pa ulendo wanga wopita ku Makedoniya ndi kudzakuonaninso pochokera ku Makedoniyako kuti inu mudzandithandize pa ulendo wanga wopita ku Yudeya.
17 Hottelah ka kâcai e heh a vanlong lah ka pouk e maw. Hoe pawiteh talai ngainae dawkvah ka titeh, Oe teh Oe hoi, nahoeh teh nahoeh telah ka tet boi e na maw.
Kodi pamene ndinkakonzekera zimenezi, mukuganiza kuti ndinkachita mwachibwana? Kapena kuti ndinkaganiza ngati mwa dziko lapansi; kuti ndikhoza kumanena kuti, “Inde, Inde,” nthawi yomweyo nʼkumatinso “Ayi, Ayi?”
18 Cathut teh yuemkamcu e patetlah nangmouh koe ka dei awh e lawk teh vai touh dawk, bokheiyah hoi, nahoeh telah nahoehmaw.
Koma zoona monga Mulungu ali wokhulupirika, uthenga wathu kwa inu siwakuti, “Inde” nʼkutinso “Ayi.”
19 Kaimouh hoi Silvanas, Timote tinaw ni nangmouh koe ka dei awh e Cathut Capa Jisuh Khrih dawk vai touh hoi, Oe hoi Oe nahoeh telah awm laipalah Bawipa dawk, Oe telah doeh ao.
Pakuti Yesu Khristu mwana wa Mulungu amene ine, Silivano ndi Timoteyo tinamulalikira pakati panu sali “Inde” yemweyonso “Ayi.” Koma nthawi zonse mwa Iye muli “Inde.”
20 Hote Bawipa dawk Cathut e a lawk kam e naw pueng teh maimouh kecu dawk a bawilennae a kamnue nahanlah, Oe telah ati, Amen telah ati.
Pakuti ngakhale malonjezo a Mulungu atachuluka chotani, onsewo ndi “Inde” mwa Khristu. Kotero kuti mwa Iye, ife timati “Ameni” kuchitira Mulungu ulemu.
21 Nangmouh hoi kaimouh teh Khrih thung na o sak teh satui kaawikung teh Cathut doeh.
Tsono ndi Mulungu amene anachititsa kuti inu ndi ife tiyime molimba mwa Khristu. Anatidzoza ife,
22 Hote Cathut ni maimouh hah tacik na kin teh maimae lungthung vah lawkawm lah Kathoung Muitha na poe toe.
nayikanso Mzimu wake mʼmitima mwathu kutitsimikizira za mʼtsogolo.
23 Cathut teh kai kampangkhai e lah ao. Ama ni ka lungthin teh a panue. Kawrin kho lah cei hoeh nahan kho ka pouk teh nangmouh hane malam ka pouk dawk doeh.
Mulungu ndi mboni yanga kuti sindinabwererenso ku Korinto kuno kuti ndisakumvetseni chisoni.
24 Kaimouh ni nangmae na yuemnae dawk kâ ka tawn awh hoeh. Nangmouh ni lunghawi nahanlah nangmouh hoi cungtalah thaw ka tawk awh e doeh. Nangmouh teh yuemnae hoi na kangdue thai awh toe.
Sikuti ife tikufuna kukhala olamulira chikhulupiriro chanu, koma timagwira nanu ntchito pamodzi kuti mukhale achimwemwe, chifukwa ndinu okhazikika kwambiri mʼchikhulupiriro.

< 2 Kawrin 1 >