< Masalimo 60 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Kakombo wa Pangano.” Mikitamu ya Davide yophunzitsira. Pamene anamenyana ndi Mesopotamiya ndi Aramu-Zoba, ndi pamene Yowabu anabwerera ndi kukantha Aedomu 12,000 mʼChigwa cha Mchere. Inu Mulungu mwatikanatu ife, ndipo mwatiwonongera otiteteza. Inu mwatikwiyira, tsopano tibwezeretseni mwakale!
Davidin kultainen kappale, edelläveisaajalle, kultaisesta seppeleen kukkaisesta opettamaan, Kuin hän oli sotinut Syrialaisten kanssa Mesopotamiasta, ja Zoban Syrialaisten kanssa; kuin Joab palasi, ja löi Suolalaaksossa kaksitoistakymmentä tuhatta Edomilaista. Jumala, sinä joka olet meitä lykännyt pois, hajoittanut meitä ja ollut vihainen, palaja taas meidän tykömme.
2 Inu mwagwedeza dziko ndipo mwalingʼamba, konzani mingʼalu yake pakuti ikugwedezeka kwambiri.
Sinä joka maan liikuttanut ja halaissut olet, paranna hänen rakonsa, joka niin haljennut on.
3 Inu mwaonetsa anthu anu nthawi za mavuto; inu mwatipatsa vinyo amene watichititsa kudzandira.
Sinä olet kansalles kovuutta osoittanut, ja meitä kompastuksen viinalla juottanut.
4 Koma kwa iwo amene amaopa Inu, Inu mwakweza mbendera kuti tisonkhanireko pothawa uta.
Sinä annoit lipun niille, jotka sinua pelkäävät, jolla he itsensä ojensivat ylös, totuuden tähden, (Sela)
5 Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja, kuti iwo amene mumawakonda apulumutsidwe.
Että sinun ystäväs vapahdetuksi tulisivat: niin auta nyt oikialla kädelläs, ja kuule meidän rukouksemme.
6 Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika: “Mwakupambana ndidzagawa Sekemu ndipo ndidzayeza malire a chigwa cha Sukoti.
Jumala on puhunut pyhässänsä, siitä minä iloitsen: minä tahdon jakaa Sikemin ja mitata Sukkotin laakson.
7 Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso; Efereimu ndi chipewa changa chodzitetezera, Yuda ndi ndodo yanga yaufumu
Gilead on minun, minun on Manasse, Ephrain on minun pääni voima: Juuda on minulle lainopettaja.
8 Mowabu ndi mbale yanga yosambira, pa Edomu ndidzaponyapo nsapato yanga, pa Filisitiya ndidzafuwula mwakupambana.”
Moab on minun pesinpatani, Edomin ylitse heitän minä kenkäni: sinä Philistea, iloitse minusta.
9 Adzandifikitse ndani ku mzinda wotetezedwa? Ndani adzanditsogolera ku Edomu?
Kuka vie minun vahvaan kaupunkiin? kuka johdattaa minun Edomiin?
10 Kodi si Inu Mulungu, Inu amene mwatikana ife ndipo simutuluka pamodzi ndi magulu athu ankhondo.
Etkös sinä, Jumala, joka meitä lykkäsit pois? ja etkö sinä, Jumala, lähde ulos meidän sotaväkemme kanssa?
11 Tipatseni chithandizo kuti tilimbane ndi mdani wathu, pakuti thandizo lochokera kwa munthu ndi lopanda phindu.
Saata meille apu tuskasta; sillä ihmisten apu on turha.
12 Chifukwa cha Mulungu, ife tidzapeza chipambano ndipo tidzapondaponda adani athu.
Jumalassa tahdomme me voimalliset työt tehdä: ja hän tallaa alas meidän vihollisemme.

< Masalimo 60 >