< Masalimo 60 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Kakombo wa Pangano.” Mikitamu ya Davide yophunzitsira. Pamene anamenyana ndi Mesopotamiya ndi Aramu-Zoba, ndi pamene Yowabu anabwerera ndi kukantha Aedomu 12,000 mʼChigwa cha Mchere. Inu Mulungu mwatikanatu ife, ndipo mwatiwonongera otiteteza. Inu mwatikwiyira, tsopano tibwezeretseni mwakale!
Kuom jatend wer. E dwol mar “Ondanyo mar singruok.” Miktam mar Daudi. Mar puonjo. Kane okedo gi Aram-Naharaim kod Aram Zoba, kendo kane Joab odwogo mi onego jo-Edom alufu apar gariyo e Holo mar Chumbi. Yaye Nyasaye, isedagiwa mi imuomori kuomwa; isebedo ka ikecho kodwa, to koro loswa!
2 Inu mwagwedeza dziko ndipo mwalingʼamba, konzani mingʼalu yake pakuti ikugwedezeka kwambiri.
Iseyiengo piny mi ibare diere ariyo, Los kuondene mosebarore, nikech oyiengni.
3 Inu mwaonetsa anthu anu nthawi za mavuto; inu mwatipatsa vinyo amene watichititsa kudzandira.
Isenyiso jogi kinde mag chandruok mapek; isemiyowa kongʼo mamiyo wakwangʼ.
4 Koma kwa iwo amene amaopa Inu, Inu mwakweza mbendera kuti tisonkhanireko pothawa uta.
To isechungo bandech loch ni joma oluori mondo oumgi ka oywanegi atungʼ. (Sela)
5 Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja, kuti iwo amene mumawakonda apulumutsidwe.
Reswa kendo konywa gi lweti ma korachwich mondo joma ihero ogol e chandruok.
6 Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika: “Mwakupambana ndidzagawa Sekemu ndipo ndidzayeza malire a chigwa cha Sukoti.
Nyasaye osewuoyo gie kare maler kowacho niya, “Abiro pogo Shekem ne ji, kendo abiro pimo ne ji Holo mar Sukoth.
7 Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso; Efereimu ndi chipewa changa chodzitetezera, Yuda ndi ndodo yanga yaufumu
Gilead en mara, Manase bende mara; Efraim en oguta mar lweny, to Juda en osimbona mar loch.
8 Mowabu ndi mbale yanga yosambira, pa Edomu ndidzaponyapo nsapato yanga, pa Filisitiya ndidzafuwula mwakupambana.”
Moab en besen mara mar luok, to Edom e kama amoe wuochena; Filistia ema akoke ka aseloyo lweny.”
9 Adzandifikitse ndani ku mzinda wotetezedwa? Ndani adzanditsogolera ku Edomu?
En ngʼa mabiro kela e dala maduongʼ mochiel motegno? Ngʼa mabiro telona nyaka Edom?
10 Kodi si Inu Mulungu, Inu amene mwatikana ife ndipo simutuluka pamodzi ndi magulu athu ankhondo.
Donge in ema isedagiwa, yaye Nyasaye, kendo tinde ok idhi gi jolwenjwa e lweny?
11 Tipatseni chithandizo kuti tilimbane ndi mdani wathu, pakuti thandizo lochokera kwa munthu ndi lopanda phindu.
Miwa kony mondo walo wasikwa, nikech kony mar dhano onge tich.
12 Chifukwa cha Mulungu, ife tidzapeza chipambano ndipo tidzapondaponda adani athu.
Wabiro loyo lweny ka Nyasaye nikodwa, kendo obiro nyono wasikwa piny.

< Masalimo 60 >