< Masalimo 60 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Kakombo wa Pangano.” Mikitamu ya Davide yophunzitsira. Pamene anamenyana ndi Mesopotamiya ndi Aramu-Zoba, ndi pamene Yowabu anabwerera ndi kukantha Aedomu 12,000 mʼChigwa cha Mchere. Inu Mulungu mwatikanatu ife, ndipo mwatiwonongera otiteteza. Inu mwatikwiyira, tsopano tibwezeretseni mwakale!
Gode! Di da nini higale, nini hasali. Di da ninima ougi galu. Be wali ninima bu beba: ma!
2 Inu mwagwedeza dziko ndipo mwalingʼamba, konzani mingʼalu yake pakuti ikugwedezeka kwambiri.
Di da soge fogoma: ne hamoi amola Di da soge damuni, a:lesi. Soge da agele sa: imu gadeneiba: le, ea fa: ginisi amo uhinisima.
3 Inu mwaonetsa anthu anu nthawi za mavuto; inu mwatipatsa vinyo amene watichititsa kudzandira.
Dia hamobeba: le, Dia fi da se bagade naba. Ninia da adini ba: i dunu defele, amane gigiawasa ahoa.
4 Koma kwa iwo amene amaopa Inu, Inu mwakweza mbendera kuti tisonkhanireko pothawa uta.
Di da dunu Dima beda: be, ilima diwaneya udidibi amo mae ba: ma: ne sisai dagoi.
5 Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja, kuti iwo amene mumawakonda apulumutsidwe.
Dia gasa bagade amoga nini gaga: ma! Dunu amo da Dia dogolegei, ilia da gaga: su ba: ma: ne, ninia sia: ne gadosu amoma dabe adole ima.
6 Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika: “Mwakupambana ndidzagawa Sekemu ndipo ndidzayeza malire a chigwa cha Sukoti.
Ea hadigi sogebi amogainini, Gode da amane sia: i “Na da hasalasili, Siegeme moilai bai bagade amola Sagode Fago amo alalo hahamone, huluane momogili Na fi dunuma imunu.
7 Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso; Efereimu ndi chipewa changa chodzitetezera, Yuda ndi ndodo yanga yaufumu
Gilia: de da Na: Ma: na: sa amola da Na: Ifala: ime da Na dialuma figisu amola Yuda da Na Hina Bagade Dagulu.
8 Mowabu ndi mbale yanga yosambira, pa Edomu ndidzaponyapo nsapato yanga, pa Filisitiya ndidzafuwula mwakupambana.”
Be Na da Moua: be amo na lobo dodofesu ofodo hamomu. Amola Na da Idome amo Ni lai dagoi, amo enoga dawa: digima: ne, Na da emo salasu gisa: le, Idomema galagamu! Filisidini dunu da Nama bagadewane hasalasibiba: le, Nama ha: gi wele sia: su hamomu, ilia da dawa: bela: ? Amane hame!”
9 Adzandifikitse ndani ku mzinda wotetezedwa? Ndani adzanditsogolera ku Edomu?
Gode! Nowa da na oule, gasa bagade gagili sali moilai fi amoga heda: ma: bela: ? Nowa da na sigi aligili, Idome amoga masa: bela: ?
10 Kodi si Inu Mulungu, Inu amene mwatikana ife ndipo simutuluka pamodzi ndi magulu athu ankhondo.
Di da dafawane nini higale fisiagabela: ? Di da ninia dadi gagui dunu ilima gilisili mogodigili gadili masa: bela: ?
11 Tipatseni chithandizo kuti tilimbane ndi mdani wathu, pakuti thandizo lochokera kwa munthu ndi lopanda phindu.
Ninima ha lai dunu da nini hasalasa: besa: le, Dia nini fidima. Bai osobo bagade dunu ilia fidisu da hamedeidafa gala.
12 Chifukwa cha Mulungu, ife tidzapeza chipambano ndipo tidzapondaponda adani athu.
Gode da ninimagasea, ninia da ili hasalasimu. E da ninima ha lai dunu ili hasalimu.