< Masalimo 56 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Njiwa pa Mtengo wa Thundu wa Kutali.” Mikitamu ya Davide, pamene Afilisti anamugwira ku Gati. Mundichitire chifundo Inu Mulungu, pakuti anthu akundithamangitsa kwambiri; tsiku lonse akundithira nkhondo.
Til Sangmesteren; til „den stumme Due i det fjerne” af David; „et gyldent Smykke”, der Filisterne havde grebet ham i Gath.
2 Ondinyoza akundithamangitsa tsiku lonse, ambiri akumenyana nane monyada.
Gud! vær mig naadig; thi et Menneske søger at opsluge mig, Stridsmanden trænger mig den ganske Dag.
3 Ndikachita mantha ndimadalira Inu.
Mine Fjender søge den ganske Dag at opsluge mig; thi de ere mange, som i Hovmod stride imod mig.
4 Mwa Mulungu, amene mawu ake ine ndimatamanda, mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha. Kodi munthu amene amafa angandichite chiyani?
Paa den Dag, jeg frygter, forlader jeg mig paa dig.
5 Tsiku lonse amatembenuza mawu anga; nthawi zonse amakonza zondivulaza.
I Gud vil jeg prise hans Ord; jeg forlader mig paa Gud, jeg vil ikke frygte; hvad kan Kød gøre mig?
6 Iwo amakambirana, amandibisalira, amayangʼanitsitsa mayendedwe anga ndipo amakhala ndi chidwi chofuna kuchotsa moyo wanga.
Den ganske Dag fordreje de mine Ord; alle deres Tanker ere imod mig til det onde.
7 Musalole konse kuti athawe; mu mkwiyo wanu Mulungu mugwetse mitundu ya anthu.
De holde sig sammen, de skjule sig, de tage Vare paa mine Fodspor, ligesom de have tragtet efter mit Liv.
8 Mulembe za kulira kwanga, mulembe chiwerengero cha misozi yanga mʼbuku lanu. Kodi zimenezi sizinalembedwe mʼbuku lanulo?
Skulde de undkomme ved deres Uretfærdighed? Gud! nedstød disse Folk i Vrede!
9 Adani anga adzabwerera mʼmbuyo pamene ndidzalirira kwa Inu. Pamenepo ndidzadziwa kuti Mulungu ali ku mbali yanga.
Du har talt mine Landflygtighedsdage; gem mine Taarer i din Flaske; staa de ikke i din Bog?
10 Mwa Mulungu amene mawu ake ndimawatamanda, mwa Yehova amene mawu ake ndimawatamanda,
Da skulle mine Fjender vende tilbage paa den Dag, jeg raaber; dette ved jeg, at du er min Gud.
11 mwa Mulungu ine ndimadalira ndipo sindidzachita mantha. Kodi munthu angandichite chiyani?
I Gud vil jeg prise Ordet; i Herren vil jeg prise Ordet.
12 Ndiyenera kuchita zomwe ndinalumbira kwa Mulungu; ndidzapereka nsembe zanga zachiyamiko kwa inu.
Jeg forlader mig paa Gud, jeg vil ikke frygte; hvad skulde et Menneske gøre mig?
13 Pakuti mwawombola moyo wanga ku imfa ndi mapazi anga kuti ndingagwe, kuti ndiyende pamaso pa Mulungu mʼkuwala kwa moyo.
Gud! Løfter til dig hvile paa mig, med Taksigelse vil jeg betale dig. Thi du friede min Sjæl fra Døden, ja, mine Fødder fra Fald, at jeg skal vandre for Guds Ansigt i de levendes Lys.