< Masalimo 23 >

1 Salimo la Davide. Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
مزمور داود خداوند شبان من است. محتاج به هیچ چیز نخواهم بود.۱
2 Amandigoneka pa msipu wobiriwira, amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
در مرتعهای سبزمرا می‌خواباند. نزد آبهای راحت مرا رهبری می‌کند.۲
3 amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo chifukwa cha dzina lake.
جان مرا برمی گرداند. و به‌خاطر نام خود به راههای عدالت هدایتم می‌نماید.۳
4 Ngakhale ndiyende mʼchigwa cha mdima wakuda bii, sindidzaopa choyipa, pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu zimanditonthoza.
چون در وادی سایه موت نیز راه روم از بدی نخواهم ترسید زیرا تو با من هستی. عصا و چوب دستی تومرا تسلی خواهد داد.۴
5 Mumandikonzera chakudya adani anga akuona. Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta; chikho changa chimasefukira.
سفره‌ای برای من به حضور دشمنانم می‌گسترانی. سر مرا به روغن تدهین کرده‌ای و کاسه‌ام لبریز شده است.۵
6 Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova kwamuyaya.
هرآینه نیکویی و رحمت تمام ایام عمرم در‌پی من خواهد بود. و در خانه خداوند ساکن خواهم بود تا ابدالاباد.۶

< Masalimo 23 >