< Masalimo 23 >

1 Salimo la Davide. Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
(En salme af David.) HERREN er min Hyrde, mig skal intet fattes,
2 Amandigoneka pa msipu wobiriwira, amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
han lader mig ligge på grønne Vange. Til Hvilens Vande leder han mig, han kvæger min Sjæl,
3 amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo chifukwa cha dzina lake.
han fører mig ad rette Veje for sit Navns Skyld.
4 Ngakhale ndiyende mʼchigwa cha mdima wakuda bii, sindidzaopa choyipa, pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu zimanditonthoza.
Skal jeg end vandre i Dødsskyggens Dal, jeg frygter ej ondt; thi du er med mig, din Kæp og din Stav er min Trøst.
5 Mumandikonzera chakudya adani anga akuona. Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta; chikho changa chimasefukira.
I mine Fjenders Påsyn dækker du Bord for mig, du salver mit Hoved med Olie, mit Bæger flyder over.
6 Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova kwamuyaya.
Kun Godhed og Miskundhed følger mig alle mine Dage, og i HERRENs Hus skal jeg bo gennem lange Tider.

< Masalimo 23 >