< Masalimo 150 >

1 Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
Alleluia. Laudate Dominum in sanctis eius: laudate eum in firmamento virtutis eius.
2 Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
Laudate eum in virtutibus eius: laudate eum secundum multitudinem magnitudinis eius.
3 Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
Laudate eum in sono tubae: laudate eum in psalterio, et cithara.
4 Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
Laudate eum in tympano, et choro: laudate eum in chordis, et organo.
5 Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.
Laudate eum in cymbalis benesonantibus: laudate eum in cymbalis iubilationis:
6 Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.
omnis spiritus laudet Dominum. Alleluia.

< Masalimo 150 >