< Masalimo 131 >

1 Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
Hodočasnička pjesma. Davidova. O Jahve, ne gordi se moje srce niti se oči uznose. Ne idem za stvarima velikim ni za čudima što su iznad mene.
2 Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
Ne, ja sam se smirio i upokojio dušu svoju; kao dojenče na grudima majke, kao dojenče duša je moja u meni.
3 Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.
U Jahvu se, Izraele, uzdaj odsada dovijeka.

< Masalimo 131 >