< Masalimo 13 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale? Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
Докле ћеш ме, Господе, сасвим заборављати? Докле ћеш одвраћати лице своје од мене?
2 Ndidzalimbana ndi maganizo anga ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti? Mpaka liti adani anga adzandipambana?
Докле ћу се домишљати у души својој, мутити се у срцу свом дан и ноћ? Докле ће се непријатељ мој подизати нада мном?
3 Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga. Walitsani maso anga kuti ndingafe;
Погледај, услиши ме, Господе, Боже мој! Просветли очи моје да не заспим на смрт.
4 mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,” ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.
Да не рече непријатељ мој: Надвладао сам га; да се не радују који ме гоне, ако посрнем.
5 Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika; mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
А ја се уздам у милост Твоју; радоваће се срце моје за спасење Твоје.
6 Ine ndidzayimbira Yehova pakuti wandichitira zokoma.
Певаћу Господу, који ми добро чини.

< Masalimo 13 >