< Masalimo 113 >

1 Tamandani Yehova. Mutamandeni, inu atumiki a Yehova, tamandani dzina la Yehova.
Halleluja! Pris, I Herrens tjenere, pris Herrens navn!
2 Yehova atamandidwe, kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Herrens navn være lovet fra nu og til evig tid;
3 Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake, dzina la Yehova liyenera kutamandidwa.
fra sol i opgang til sol i bjærge være Herrens navn lovpriset!
4 Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse, ulemerero wake ndi woposa mayiko akumwamba.
Over alle folk er Herren ophøjet, hans herlighed højt over himlene.
5 Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu, Iye amene amakhala mwaufumu mmwamba?
Hvo er som HERREN vor Gud, som rejste sin Trone i det høje
6 amene amawerama pansi kuyangʼana miyamba ndi dziko lapansi?
og skuer ned i det dybe - i Himlene og på Jorden -
7 Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi ndi kutukula munthu wosowa kuchoka pa dzala;
som rejser den ringe af Støvet, løfter den fattige op af Skarnet
8 amawakhazika pamodzi ndi mafumu, pamodzi ndi mafumu a anthu ake.
og sætter ham mellem Fyrster, imellem sit Folks Fyrster,
9 Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake monga mayi wa ana wosangalala. Tamandani Yehova.
han, som lader barnløs Hustru sidde som lykkelig Barnemoder!

< Masalimo 113 >