Preface
Bibles
+
CHW
HBA
X
<
h2403H
>
X
<
^
>
<
>
<
Masalimo
100
>
1
Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
מזמור לתודה הריעו ליהוה כל-הארץ
2
Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
עבדו את-יהוה בשמחה באו לפניו ברננה
3
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
דעו-- כי יהוה הוא אלהים הוא-עשנו ולא (ולו) אנחנו-- עמו וצאן מרעיתו
4
Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
באו שעריו בתודה--חצרתיו בתהלה הודו-לו ברכו שמו
5
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.
כי-טוב יהוה לעולם חסדו ועד-דר ודר אמונתו
<
Masalimo
100
>
Go to
>
Bookmark
/
Concordance
/
Maps
/
Report Issue
The world's first Holy Bible un-translation!