< Miyambo 7 >

1 Mwana wanga, mvera mawu anga; usunge bwino malamulo angawa.
Ndodana yami, gcina amazwi ami, uzibekele imilayo yami.
2 Utsate malamulo anga ndipo udzakhala ndi moyo; samala malangizo angawa monga uchitira ndi maso ako.
Gcina imilayo yami, uphile, lomthetho wami njengenhlamvu yamehlo akho.
3 Uchite ngati wawamangirira pa zala zako, ndiponso ngati kuti wawalemba pa mtima pako.
Ukubophele eminweni yakho, kubhale esibhebheni senhliziyo yakho.
4 Nzeru uyiwuze kuti, “Iwe ndiwe mlongo wanga,” ndipo khalidwe lomvetsa bwino zinthu ulitchule kuti, “Bwenzi langa lapamtima.”
Uthi kunhlakanipho: Ungudadewethu; ubize ukuqedisisa ngokuthi yisihlobo sakho;
5 Zidzakuteteza kwa mkazi wachigololo ndiponso zidzakuthandiza kusamvera mawu oshashalika a mkazi wachilendo.
ukuze kukugcine kumfazi wemzini, kowesifazana wemzini oyengayo ngamazwi akhe.
6 Tsiku lina pa zenera la nyumba yanga ndinasuzumira pa zenera.
Ngoba ewindini lendlu yami, ngeminxibo yewindi ngalunguza phandle,
7 Ndinaona pakati pa anthu opusa, pakati pa anyamata, mnyamata wina wopanda nzeru.
ngasengibona phakathi kwabangelalwazi, ngananzelela phakathi kwabatsha ijaha eliswele ingqondo,
8 Iye ankayenda njira yodutsa pafupi ndi nyumba ya mkaziyo, kuyenda molunjika nyumba ya mkaziyo.
lisedlula esitaladeni eceleni kwengonsi yakhe, linyathela endleleni yendlu yakhe,
9 Inali nthawi yachisisira madzulo, nthawi ya usiku, kuli mdima.
kusihlwa, ngentambama yosuku, ebusuku obumnyama, lomnyama.
10 Ndipo mkaziyo anadzakumana naye, atavala ngati munthu wachiwerewere wa mtima wonyenga.
Khangela-ke, owesifazana walihlangabeza, lesembatho sewule, elobuqili ngenhliziyo.
11 (Mkaziyo ndi wolongolola ndiponso nkhutukumve, iye ndi wosakhazikika pa khomo.
Lo wayelomsindo, eyisiqholo; inyawo zakhe kazihlali endlini yakhe.
12 Mwina umupeza pa msewu, mwina umupeza pa msika, ndipo amadikirira munthu pa mphambano iliyonse).
Khathesi uphandle, abesesiba ezitaladeni, ecathama kuyo yonke ingonsi.
13 Tsono amagwira mnyamatayo ndi kupsompsona ndi nkhope yake yopanda manyazi amamuwuza kuti,
Ngokunjalo walibamba, walanga, waqinisa ubuso bakhe, wathi kulo:
14 “Ndinayenera kupereka nsembe zachiyanjano. Lero ndakwaniritsa malumbiro anga.
Imihlatshelo yeminikelo yokuthula ikimi; lamuhla sengibhadele izifungo zami.
15 Choncho ndinabwera kudzakumana nawe; ndinkakufunafuna ndipo ndakupeza!
Ngakho-ke ngiphumile ukukuhlangabeza, ngidingisise ubuso bakho; ngikutholile.
16 Pa bedi panga ndayalapo nsalu zosalala zokongola zochokera ku Igupto.
Ngendlele umbheda wami ngezendlalo, ngamalembu acolekileyo kakhulu alemibalabala avela eGibhithe.
17 Pa bedi panga ndawazapo zonunkhira za mure, mafuta onunkhira a aloe ndi sinamoni.
Ngifafazile umbheda wami ngemure, izinhlaba, lekinamoni.
18 Bwera, tiye tikhale malo amodzi kukondwerera chikondi mpaka mmawa; tiye tisangalatsane mwachikondi!
Woza, sizidakise ngothando kuze kuse, sizithokozise ngothando olukhulu.
19 Mwamuna wanga kulibe ku nyumbako; wapita ulendo wautali:
Ngoba indoda kayikho endlini yayo, ihambile uhambo khatshana.
20 Anatenga thumba la ndalama ndipo adzabwera ku nyumba mwezi ukakhwima.”
Ithethe isaka lemali esandleni sayo; ngosuku lwenyanga egcweleyo izakuza endlini yayo.
21 Ndi mawu ake onyengerera amamukakamiza mnyamatayo; amukopa ndi mawu ake oshashalika.
Walihuga ngobunengi bemfundiso yakhe, walivumisa ngenkulumo zakhe ezincengayo.
22 Nthawi yomweyo chitsiru chimamutsatira mkaziyo ngati ngʼombe yopita kukaphedwa, monga momwe mbawala ikodwera mu msampha,
Lahle lamlandela njengenkabi isiya ekuhlatshweni, lanjengesiphukuphuku sisiya ekujezisweni esongweni lenqagala;
23 mpaka muvi utalasa chiwindi chake, chimakhala ngati mbalame yothamangira mʼkhwekhwe, osadziwa kuti moyo wake uwonongeka.
uze umtshoko uhlabe isibindi salo, njengenyoni iphangisela esifwini, ingazi ukuthi simelene lempilo yayo.
24 Tsono ana inu, ndimvereni; mvetsetsani zimene ndikunena.
Khathesi-ke, bantwana, ngizweni, lilalele amazwi omlomo wami.
25 Musatengeke mtima ndi njira za mkazi ameneyu; musasochere potsata njira zake.
Inhliziyo yakho kayingaphambukeli endleleni zakhe; ungaduhi emikhondweni yakhe.
26 Paja iye anagwetsa anthu ambiri; wapha gulu lalikulu la anthu.
Ngoba ubawisele phansi abanengi abalimeleyo, labo bonke ababuleweyo bakhe banengi.
27 Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol h7585)
Indlu yakhe izindlela zesihogo, ezehlela emakamelweni okufa. (Sheol h7585)

< Miyambo 7 >