Aionian Verses

Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol h7585)
Vsi njegovi sinovi in vse njegove hčere so vstali, da ga potolažijo, toda odklonil je, da bi bil potolažen in rekel je: »Kajti žalujoč bom šel v grob k svojemu sinu.« Tako je njegov oče jokal za njim. (Sheol h7585)
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol h7585)
Rekel je: »Moj sin ne bo šel dol s teboj, kajti njegov brat je mrtev, on pa je ostal sam. Če ga po poti, na katero greste, zadene nesreča, potem boste moje sive lase z bridkostjo privedli do groba.« (Sheol h7585)
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol h7585)
Če tudi tega vzamete od mene in ga zadene nesreča, boste moje sive lase z bridkostjo privedli do groba.‹ (Sheol h7585)
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol h7585)
se bo zgodilo, ko bo videl, da dečka ni z nami, da bo umrl. Tvoji služabniki bodo sive lase tvojega služabnika, našega očeta, z bridkostjo privedli do groba. (Sheol h7585)
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol h7585)
Toda če Gospod naredi novo stvar in zemlja odpre svoja usta in jih požre, z vsem, kar jim pripada in gredo hitro dol v jamo, potem boste razumeli, da so ti ljudje izzivali Gospoda.« (Sheol h7585)
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol h7585)
Oni in vsi, ki so pripadali k njim, so živi odšli dol v jamo, in zemlja se je zaprla nad njimi in izginili so iz skupnosti. (Sheol h7585)
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol h7585)
Kajti v moji jezi je vžgan ogenj in gorel bo do najnižjega pekla in použil bo zemljo z njenim narastom in vžgal bo temelje gora. (Sheol h7585)
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol h7585)
Gospod ubija in oživlja. Privede dol do groba in privede gor. (Sheol h7585)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
bridkosti pekla so me obkrožile, zanke smrti so me ovirale; (Sheol h7585)
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
Stori torej glede na svojo modrost in ne dopusti, da bi njegova osivela glava šla v miru dol v podzemlje. (Sheol h7585)
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol h7585)
Zdaj ga torej ne imej brez krivde, kajti moder človek si in veš, kaj mu moraš storiti, temveč njegovo osivelo glavo s krvjo privedi dol k podzemlju.« (Sheol h7585)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol h7585)
Kakor je oblak použit in izginil proč, tako kdor gre dol h grobu, ne bo več prišel gor. (Sheol h7585)
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol h7585)
To je tako visoko kakor nebo. Kaj lahko storiš? Globlje kakor pekel. Kaj lahko spoznaš? (Sheol h7585)
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol h7585)
Oh, da bi me hotel skriti v grob, da bi me varoval na skrivnem, dokler tvoj bes ne mine, da bi mi določil določeni čas in me spomnil! (Sheol h7585)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
Če čakam, je moja hiša grob; svojo posteljo sem postlal v temi. (Sheol h7585)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)
Šli bodo dol k zapahom jame, ko je naš skupni počitek v prahu.« (Sheol h7585)
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol h7585)
Svoje dni preživijo v obilju in v trenutku gredo dol v grob. (Sheol h7585)
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol h7585)
Suša in vročina použijeta snežne vode; tako grob tiste, ki so grešili. (Sheol h7585)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
Pekel je nag pred njim in uničenje nima pokrivala. (Sheol h7585)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol h7585)
Kajti v smrti ni spomina nate. Kdo se ti bo zahvaljeval v grobu? (Sheol h7585)
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol h7585)
Zlobni bodo napoteni v pekel in vsi narodi, ki pozabljajo Boga. (Sheol h7585)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
Kajti moje duše ne boš pustil v peklu niti ne boš trpel, da bi tvoj Sveti videl trohnobo. (Sheol h7585)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
Obkrožile so me bridkosti pekla. Zanke smrti so me ovirale. (Sheol h7585)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol h7585)
Oh Gospod, mojo dušo si privedel iz groba. Ohranil si me živega, da ne bi šel dol v jamo. (Sheol h7585)
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol h7585)
Naj ne bom osramočen, oh Gospod, kajti klical sem k tebi. Naj bodo zlobni osramočeni in naj bodo molče v grobu. (Sheol h7585)
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol h7585)
Kakor ovce so položeni v grob; z njimi se bo hranila smrt in iskreni bodo zjutraj imeli nad njimi oblast in njihova lepota bo požrta v grobu, proč od njihovega bivanja. (Sheol h7585)
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol h7585)
Toda Bog bo mojo dušo odkupil iz oblasti groba, kajti sprejel me bo. (Sela) (Sheol h7585)
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol h7585)
Naj se jih polasti smrt in naj hitro gredo dol v pekel, kajti zlobnost je v njihovih bivališčih in med njimi. (Sheol h7585)
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol h7585)
Kajti veliko je tvoje usmiljenje do mene in mojo dušo si osvobodil pred najglobljim peklom. (Sheol h7585)
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol h7585)
kajti moja duša je polna stisk in moje življenje se bliža grobu. (Sheol h7585)
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol h7585)
Kateri človek je, kdor živi in ne bo videl smrti? Ali bo svojo dušo osvobodil pred roko groba? (Sela) (Sheol h7585)
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol h7585)
Obdale so me bridkosti smrti in bolečine pekla so me prijele; spoznal sem stisko in bridkost. (Sheol h7585)
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol h7585)
Če se povzpnem v nebesa, si tam; če si svojo posteljo pripravim v peklu, glej, si tam. (Sheol h7585)
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol h7585)
Naše kosti so razkropljene ob ustih groba, kakor kadar nekdo seka in cepi les na zemlji. (Sheol h7585)
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol h7585)
požrimo jih žive kakor grob in cele, kakor tiste, ki gredo dol v jamo. (Sheol h7585)
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol h7585)
Njena stopala gredo dol k smrti, njeni koraki se prijemljejo pekla. (Sheol h7585)
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol h7585)
Njena hiša je pot v pekel, spuščajoča se k celicam smrti.… (Sheol h7585)
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol h7585)
Toda ta ne spozna, da so tam mrtvi in da so njeni gostje v globinah pekla. (Sheol h7585)
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol h7585)
Pekel in uničenje sta pred Gospodom, koliko bolj potem srca človeških otrok? (Sheol h7585)
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol h7585)
Pot življenja je modremu zgoraj, da lahko odide od pekla spodaj. (Sheol h7585)
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol h7585)
Udaril ga boš s šibo, njegovo dušo pa boš rešil pred peklom. (Sheol h7585)
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol h7585)
Pekel in uničenje nikdar nista polna, tako človekove oči nikoli niso nasičene. (Sheol h7585)
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol h7585)
grob in jalova maternica; zemlja, ki ni nasičena z vodo; in ogenj, ki ne govori: »Dovolj je.« (Sheol h7585)
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol h7585)
Karkoli tvoja roka najde, da stori, to stôri z vso svojo močjo, kajti v grobu, kamor greš, ni dela, niti naklepa, niti spoznanja, niti modrosti. (Sheol h7585)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol h7585)
Postavi me kakor pečat na svoje srce, kakor pečat na svoj laket, kajti ljubezen je močna kakor smrt, ljubosumje je kruto kakor grob. Njegovi ogorki so ognjeno oglje, ki ima najbolj silovit plamen. (Sheol h7585)
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol h7585)
Zato se bo pekel povečal in svoja usta odprl brez mere. Njihova slava, njihova množica, njihov pomp in kdor se razveseljuje, se bo pogreznil vanj. (Sheol h7585)
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol h7585)
»Izprosi si znamenje od Gospoda, svojega Boga, prosi ga ali v globini ali na višini zgoraj.« (Sheol h7585)
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol h7585)
Pekel od spodaj vztrepetava zaradi tebe, da te sreča ob tvojem prihodu. Zaradi tebe razvnema mrtve, celó vse zemeljske vodje, iz njihovih prestolov je dvignil vse kralje narodov. (Sheol h7585)
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol h7585)
Tvoj pomp je priveden dol h grobu in zvok tvojih lir. Ličinka se razteguje pod teboj in ličinke te pokrivajo. (Sheol h7585)
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol h7585)
Vendar boš priveden dol v pekel, na obronke jame. (Sheol h7585)
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol h7585)
Ker ste rekli: »Sklenili smo zavezo s smrtjo in s peklom smo v dogovoru. Ko bo šel skozi poplavljajoč bič, ta ne bo prišel k nam, kajti laži smo naredili za svoje zatočišče in pod neresnico smo se skrili.« (Sheol h7585)
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol h7585)
Vaša zaveza s smrtjo bo razveljavljena in vaš dogovor s peklom ne bo obstal; ko bo skozi šel preplavljajoč bič, potem boste z njim pomendrani. (Sheol h7585)
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol h7585)
»Rekel sem o preostanku svojih dni: ›Šel bom do velikih vrat groba. Prikrajšan sem preostanka svojih let.‹ (Sheol h7585)
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol h7585)
Kajti grob te ne more hvaliti, smrt te ne more proslavljati. Tisti, ki gredo dol v jamo, ne morejo upati na tvojo resnico. (Sheol h7585)
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol h7585)
Odhajaš h kralju z mazilom, množila si svoje dišave, svoje poslance si poslala daleč in sebe si ponižala celo do pekla. (Sheol h7585)
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol h7585)
Tako govori Gospod Bog: ›Na dan, ko je šel dol do groba, sem povzročil žalovanje. Zanj sem pokril globino in omejil njegove tokove in velike vode so bile ustavljene. Libanonu sem storil, da je žaloval za njim in vsa poljska drevesa so medlela zaradi njega. (Sheol h7585)
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol h7585)
Narodom sem storil, da se tresejo ob zvoku njegovega padca, ko sem ga vrgel dol do pekla, s tistimi, ki se spuščajo v jamo in vsa edenska drevesa, izbrana in najboljša iz Libanona, vsa, ki pijejo vodo, bodo potolažena v spodnjih delih zemlje. (Sheol h7585)
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol h7585)
Tudi oni so z njim odšli dol v pekel, k tistim, ki so umorjeni z mečem; in tisti, ki so bili njegov laket, ki so prebivali pod njegovo senco v sredi narodov. (Sheol h7585)
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol h7585)
Močni izmed mogočnih mu bodo govorili iz srede pekla s tistimi, ki mu pomagajo. Odšli so dol, ležijo neobrezani, umorjeni z mečem. (Sheol h7585)
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol h7585)
Ne bodo ležali z mogočnimi, ki so padli od neobrezancev, ki so odšli dol k peklu z njihovimi bojnimi orožji. Njihove meče so položili pod njihove glave, toda njihove krivičnosti bodo na njihovih kosteh, čeprav so bili strahota mogočnih v deželi živih. (Sheol h7585)
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol h7585)
Odkupil jih bom pred oblastjo groba; odkupil jih bom pred smrtjo. ›Oh smrt, jaz bom tvoje kuge; ‹ ›Oh grob, jaz bom tvoje uničenje.‹ Kesanje bo skrito mojim očem. (Sheol h7585)
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol h7585)
Čeprav kopljejo v pekel, jih bo moja roka vzela od tam. Čeprav plezajo gor do nebes, jih bom od tam privedel dol. (Sheol h7585)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol h7585)
in rekel: »Zaradi razloga svoje stiske sem klical h Gospodu in me je slišal. Ven iz trebuha pekla sem klical in ti si slišal moj glas. (Sheol h7585)
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol h7585)
Da, prav tako, ker greši z vinom, je ponosen človek niti se ne drži doma, ki svojo željo povečuje kakor pekel in je kakor smrt in ne more biti nasičen, temveč k sebi zbira vse narode in k sebi kopiči vsa ljudstva. (Sheol h7585)
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna g1067)
Toda povem vam: ›Da kdorkoli je brez razloga jezen na svojega brata, bo v nevarnosti sodbe, ‹ in kdorkoli bo svojemu bratu rekel: ›Raka, ‹ bo v nevarnosti pred vélikim zborom. Toda kdorkoli bo rekel: ›Ti bedak, ‹ bo v nevarnosti peklenskega ognja. (Geenna g1067)
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
In če te tvoje desno oko pohujšuje, ga iztakni in ga vrzi od sebe; kajti zate je koristno, da bi eden izmed tvojih udov propadel in ne, da bi tvoje celó telo moralo biti vrženo v pekel. (Geenna g1067)
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna g1067)
In če te tvoja desnica pohujšuje, jo odsekaj in jo vrzi od sebe; kajti zate je koristno, da bi eden izmed tvojih udov propadel, ne pa da bi tvoje celó telo moralo biti vrženo v pekel. (Geenna g1067)
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna g1067)
In ne bojte se tistih, ki ubijejo telo, toda niso zmožni ubiti duše, temveč se raje bojte njega, ki je zmožen uničiti tako dušo kakor telo v peklu. (Geenna g1067)
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs g86)
In ti, Kafarnáum, ki si bil vzvišen do neba, boš priveden navzdol do pekla; kajti če bi se mogočna dela, ki so bila storjena v tebi, zgodila v Sódomi, bi preostala do današnjega dne.‹ (Hadēs g86)
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn g165)
In kdorkoli govori besedo zoper Sina človekovega, mu bo to odpuščeno; toda kdorkoli govori zoper Svetega Duha, mu ne bo odpuščeno ne na tem svetu ne v svetu, ki pride.‹ (aiōn g165)
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn g165)
Tudi tisti, ki je seme sprejel med trnje, je tisti, ki sliši besedo. Skrb tega sveta in zapeljivost bogastev pa zadušita besedo in on postaja brez sadu. (aiōn g165)
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn g165)
Sovražnik, ki jih je posejal, je hudič. Žetev je konec sveta, žanjci pa so angeli. (aiōn g165)
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn g165)
Kakor je torej plevel pobran in v ognju sežgan, tako bo ob koncu tega sveta. (aiōn g165)
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn g165)
Tako bo torej ob koncu sveta. Prišli bodo angeli in zlobne bodo oddvojili od pravičnih, (aiōn g165)
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs g86)
In jaz ti prav tako pravim: ›Da si ti Peter in na tej skali bom zgradil svojo cerkev in velika vrata pekla ne bodo prevladala proti njej. (Hadēs g86)
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios g166)
Zatorej, če te tvoja roka ali tvoje stopalo pohujšuje, ju odsekaj proč in ju vrzi od sebe. Bolje je zate, da v življenje vstopiš šepav ali pohabljen, raje kakor imeti dve roki ali dve stopali in biti vržen v večni ogenj. (aiōnios g166)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna g1067)
In če te tvoje oko pohujšuje, ga iztakni in ga vrzi od sebe. Bolje je zate, da vstopiš v življenje z enim očesom, raje kakor imeti dve očesi in biti vržen v peklenski ogenj. (Geenna g1067)
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios g166)
In glej, nekdo je prišel ter mu rekel: »Dobri Učitelj, katero dobro stvar naj storim, da bom lahko imel večno življenje?« (aiōnios g166)
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios g166)
In vsak, kdor je zaradi mojega imena zapustil hiše ali brate ali sestre ali očeta ali mater ali ženo ali otroke ali zemljišča, bo prejel stokratno in bo podedoval večno življenje. (aiōnios g166)
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn g165)
In ko je na poti zagledal figovo drevo, je prišel k njemu, pa na njem ni našel nič, razen listja samega in mu rekel: »Naj odslej na tebi nikoli več ne zraste noben sad.« In figovo drevo je takoj ovenelo. (aiōn g165)
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna g1067)
Gorje vam, pisarji in farizeji, hinavci! Kajti obidete morje in zemljo, da naredite enega spreobrnjenca in ko je narejen, ga naredite dvakrat bolj otroka pekla, kakor ste sami. (Geenna g1067)
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna g1067)
Vi kače, vi gadji rod, kako lahko pobegnete obsodbi na pekel? (Geenna g1067)
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn g165)
In ko je sedèl na Oljski gori, so k njemu zaupno prišli učenci, rekoč: »Povej nam, kdaj bodo te stvari? In kakšno bo znamenje tvojega prihoda in konca sveta?« (aiōn g165)
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios g166)
Tedaj bo prav tako rekel tem na levici: ›Odidite od mene, vi prekleti, v večni ogenj, pripravljen za hudiča in njegove angele; (aiōnios g166)
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios g166)
In ti bodo šli proč v večno kazen, toda pravični v večno življenje.« (aiōnios g166)
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn g165)
učeč jih obeleževati vse besede, katerekoli sem vam zapovedal. In glejte, jaz sem z vami vedno, celó do konca sveta. Amen.« (aiōn g165)
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
toda kdor bo preklinjal zoper Svetega Duha, nima nikoli odpuščanja, temveč je v nevarnosti večnega prekletstva, ‹« (aiōn g165, aiōnios g166)
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn g165)
in skrbi tega sveta, zapeljivost bogastev in poželenja po drugih stvareh vstopijo, zadušijo besedo in ta postane brezplodna. (aiōn g165)
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna g1067)
In če te tvoja roka pohujšuje, jo odsekaj proč; bolje je zate, da vstopiš v življenje pohabljen, kakor imeti dve roki in iti v pekel, v ogenj, ki ne bo nikoli pogašen, (Geenna g1067)
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna g1067)
In če te tvoje stopalo pohujšuje, ga odsekaj proč; bolje je zate, da vstopiš v življenje šepav, kakor imeti dve stopali in biti vržen v pekel, v ogenj, ki ne bo nikoli pogašen, (Geenna g1067)
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna g1067)
In če te tvoje oko pohujšuje, ga iztakni ven; bolje je zate, da vstopiš v Božje kraljestvo z enim očesom, kakor biti z dvema očesoma vržen v peklenski ogenj, (Geenna g1067)
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
In ko je odšel naprej po poti, je nekdo pritekel in pokleknil k njemu ter ga prosil: »Dobri Učitelj, kaj naj storim, da bom lahko podedoval večno življenje?« (aiōnios g166)
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn g165, aiōnios g166)
toda prejel bo stokratno, sedaj, v tem času, hiš in bratov in sester in mater in otrok in zemljišč s preganjanji; in večno življenje v svetu, ki pride. (aiōn g165, aiōnios g166)
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn g165)
In Jezus je odgovoril ter mu rekel: »Nihče naj od tebe odslej nikoli več ne jé sadu.« In njegovi učenci so to slišali. (aiōn g165)
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn g165)
in nad Jakobovo hišo bo vladal večno in njegovemu kraljestvu ne bo konca.« (aiōn g165)
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn g165)
kakor je govoril našim očetom, Abrahamu in njegovemu semenu na veke.« (aiōn g165)
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn g165)
kakor je govoril po ustih svojih svetih prerokov, ki so bili, odkar je svet nastal, (aiōn g165)
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos g12)
In rotili so ga, da jim ne bi ukazal oditi ven, v brezno. (Abyssos g12)
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs g86)
In ti Kafarnáum, ki si vzvišen do neba, boš pahnjen navzdol do pekla. (Hadēs g86)
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios g166)
In glej, nek izvedenec v postavi je vstal ter ga skušal, rekoč: »Učitelj, kaj naj storim, da podedujem večno življenje?« (aiōnios g166)
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna g1067)
Toda posvaril vas bom, koga se bojte: ›Bojte se njega, ki ima, potem ko je ubil, oblast, da vrže v pekel.‹ Da, pravim vam: ›Bojte se ga.‹ (Geenna g1067)
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn g165)
In gospodar je pohvalil nepravičnega oskrbnika, ker je modro ravnal, kajti otroci tega sveta so v svojem rodu modrejši od otrok svetlobe. (aiōn g165)
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios g166)
In pravim vam: ›Prijatelje si pridobivajte s krivičnim mamonom, da vas, ko padete, lahko sprejmejo v večna prebivališča.‹ (aiōnios g166)
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs g86)
in v peklu je povzdignil svoje oči, medtem ko je bil mučen in daleč stran zagledal Abrahama in Lazarja v njegovem naročju. (Hadēs g86)
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios g166)
In nek vladar ga je vprašal, rekoč: »Dobri Učitelj, kaj naj storim, da bom podedoval večno življenje?« (aiōnios g166)
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
ki ne bo prejel mnogokrat več v tem sedanjem času in večno življenje v svetu, ki pride.‹« (aiōn g165, aiōnios g166)
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn g165)
Jezus jim odgovori in reče: »Otroci tega sveta se poročajo in so dane v zakon, (aiōn g165)
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn g165)
toda tisti, ki bodo šteti za vredne, da dosežejo oni svet in vstajenje od mrtvih, se ne bodo niti poročali, niti ne bodo dane v zakon, (aiōn g165)
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
da se, kdorkoli veruje vanj, ne bo pogubil, temveč bo imel večno življenje. (aiōnios g166)
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Kajti Bog je tako ljubil svet, da je dal svojega edinorojenega Sina, da kdorkoli veruje vanj, se ne bo pogubil, temveč bo imel večno življenje. (aiōnios g166)
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios g166)
Kdor veruje v Sina, ima večno življenje; kdor pa ne veruje Sinu, ne bo videl življenja, temveč na njem ostaja Božji bes.« (aiōnios g166)
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
toda kdorkoli pije od vode, ki mu jo bom jaz dal, ne bo nikoli žejen, temveč bo voda, ki mu jo bom jaz dal, postala v njem izvir vode, ki izvira v večno življenje.« (aiōn g165, aiōnios g166)
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios g166)
In kdor žanje, prejema plače in zbira sad za večno življenje, da se lahko skupaj veselita oba, kdor seje in kdor žanje. (aiōnios g166)
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios g166)
Resnično, resnično, povem vam: ›Kdor sliši mojo besedo in veruje vanj, ki me je poslal, ima večno življenje in ne bo prišel v obsodbo, temveč je iz smrti prešel v življenje.‹ (aiōnios g166)
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios g166)
Preiskujete pisma, kajti v njih mislite, [da] imate večno življenje. To pa so ta, ki pričujejo o meni. (aiōnios g166)
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios g166)
Ne trudite se za jed, ki propada, temveč za jed, ki vzdrži v večno življenje, ki vam jo bo dal Sin človekov, kajti njega je potrdil Oče Bog.« (aiōnios g166)
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios g166)
In to je volja tistega, ki me je poslal, da bo vsakdo, ki vidi Sina in veruje vanj, lahko imel večno življenje in jaz ga bom dvignil na poslednji dan.« (aiōnios g166)
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios g166)
Resnično, resnično, povem vam: ›Kdor veruje vame, ima večno življenje.‹ (aiōnios g166)
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn g165)
Jaz sem živi kruh, ki je prišel dol iz nebes. Če katerikoli človek od tega kruha jé, bo živel večno, in kruh, ki ga bom jaz dal, je moje meso, ki ga bom dal za življenje sveta.« (aiōn g165)
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios g166)
Kdorkoli jé moje meso in pije mojo kri, ima večno življenje in jaz ga bom dvignil na poslednji dan.‹ (aiōnios g166)
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn g165)
To je ta kruh, ki je prišel dol iz nebes. Ne kakor vaši očetje, ki so jedli mano in so mrtvi. Kdor jé od tega kruha, bo živel večno.« (aiōn g165)
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios g166)
Potem mu je Simon Peter odgovoril: »Gospod, h komu naj gremo? Ti imaš besede večnega življenja. (aiōnios g166)
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn g165)
In služabnik v hiši ne ostaja za vedno, toda Sin ostaja večno. (aiōn g165)
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn g165)
Resnično, resnično, povem vam: ›Če se človek drži moje besede, nikoli ne bo videl smrti.‹« (aiōn g165)
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn g165)
Tedaj so mu Judje rekli: »Torej, mi vemo, da imaš hudiča. Abraham je mrtev in preroki; ti pa praviš: ›Če se človek drži moje besede, nikoli ne bo okusil smrti.‹ (aiōn g165)
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn g165)
Odkar je svet nastal, se ni slišalo, da bi katerikoli človek odprl oči nekoga, ki je bil rojen slep. (aiōn g165)
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn g165, aiōnios g166)
in dam jim večno življenje in nikoli ne bodo propadle niti jih noben človek ne bo iztrgal iz moje roke. (aiōn g165, aiōnios g166)
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn g165)
In kdorkoli živi in veruje vame, ne bo nikoli umrl. Veruješ to?« (aiōn g165)
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios g166)
Kdor ima rad svoje življenje, ga bo izgubil; kdor pa svoje življenje na tem svetu sovraži, ga bo ohranil za večno življenje. (aiōnios g166)
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn g165)
Množica mu je odgovorila: »Iz postave smo slišali, da Kristus ostaja večno; in kako praviš ti: ›Sin človekov mora biti dvignjen?‹ Kdo je ta Sin človekov?« (aiōn g165)
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios g166)
In jaz vem, da je njegova zapoved večno življenje. Karkoli torej govorim, govorim tako, celó kakor mi je rekel Oče.« (aiōnios g166)
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn g165)
Peter mu reče: »Nikoli ne boš umival mojih stopal.« Jezus mu je odgovoril: »Če te ne umijem, nimaš deleža z menoj.« (aiōn g165)
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn g165)
In prosil bom Očeta in dal vam bo drugega Tolažnika, da bo lahko večno ostal z vami, (aiōn g165)
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios g166)
kakor si mu izročil oblast nad vsem mesom, da bi on lahko dal večno življenje tolikim, kolikor si mu jih dal. (aiōnios g166)
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios g166)
In to je večno življenje, da bi oni lahko spoznali tebe, edinega resničnega Boga in Jezusa Kristusa, ki si ga poslal. (aiōnios g166)
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs g86)
ker moje duše nočeš pustiti v peklu niti nočeš trpeti, da bi tvoj Sveti videl trohnenje. (Hadēs g86)
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs g86)
in ker je to videl vnaprej, je govoril o Kristusovem vstajenju, da njegova duša ni ostala v peklu niti njegovo meso ni videlo trohnenja. (Hadēs g86)
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn g165)
ki ga morajo sprejeti nebesa do časov obnovitve vseh stvari, ki jih je Bog govoril po ustih vseh svojih svetih prerokov, odkar je svet nastal. (aiōn g165)
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios g166)
Tedaj sta Pavel in Barnaba postala pogumna in rekla: »Potrebno je bilo, da bi se Božja beseda najprej spregovorila vam, toda ker ste jo postavili proč od sebe in sebe sodite nevredne večnega življenja, glejte, se obračava k poganom. (aiōnios g166)
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios g166)
In ko so pogani to slišali, so bili veseli in slavili Gospodovo besedo; in kolikor jih je bilo odrejenih za večno življenje, je verovalo. (aiōnios g166)
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn g165)
Bogu so vsa njegova dela znana od začetka sveta. (aiōn g165)
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios g126)
Kajti od stvarjenja sveta so nevidne stvari o njem jasno vidne, ker so razumljene po stvareh, ki so narejene; celó njegova večna moč in Božanstvo, tako da so brez opravičila. (aïdios g126)
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Ki so Božjo resnico zamenjali v laž in so bolj oboževali in služili stvarstvu kakor Stvarniku, ki je blagoslovljen na veke. Amen. (aiōn g165)
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios g166)
Večno življenje tem, ki si s potrpežljivim vztrajanjem v dobrem ravnanju prizadevajo za slavo in čast in nesmrtnost; (aiōnios g166)
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios g166)
da kakor je greh kraljeval za smrt, točno tako lahko milost kraljuje po pravičnosti za večno življenje po Jezusu Kristusu, našem Gospodu. (aiōnios g166)
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Toda sedaj, ko ste osvobojeni greha in ste postali služabniki Bogu, imate svoj sad v svetost in konec večno življenje. (aiōnios g166)
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios g166)
Kajti plačila za greh so smrt; toda Božji dar je večno življenje po Jezusu Kristusu, našem Gospodu. (aiōnios g166)
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
katerih so očetje in iz katerih je, glede na meso, prišel Kristus, ki je čez vse, Bog, blagoslovljen na veke. Amen. (aiōn g165)
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos g12)
ali: ›Kdo se bo spustil v brezno?‹ (to je, da Kristusa ponovno privede gor od mrtvih).« (Abyssos g12)
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē g1653)
Kajti Bog jih je vse zaprl v nevero, da bi se lahko vseh usmilil. (eleēsē g1653)
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn g165)
Kajti iz njega in preko njega in njemu so vse stvari; ki mu bodi slava na veke. Amen. (aiōn g165)
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn g165)
In ne bodite prilagojeni temu svetu, temveč bodite preobraženi s prenavljanjem svojega mišljenja, da boste lahko razločili, kaj je tista dobra, sprejemljiva in popolna Božja volja. (aiōn g165)
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios g166)
Torej njemu, ki je sposoben, da vas utrdi v skladu z mojim evangelijem in oznanjevanjem Jezusa Kristusa, glede na razodetje skrivnosti, ki je bila tajno čuvana od nastanka sveta, (aiōnios g166)
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios g166)
toda sedaj je razodeta in po pismih prerokov, glede na zapoved večnega Boga, razglašena vsem narodom zaradi poslušnosti veri; (aiōnios g166)
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn g165)
Bogu, edinemu modremu, bodi slava po Jezusu Kristusu na veke. Amen. [Napisano Rimljanom iz Korinta in poslano po služabnici Fojbi iz kenhrejske cerkve.] (aiōn g165)
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn g165)
Kje je modri? Kje je pisar? Kje je razpravljavec tega sveta? Mar ni modrosti tega sveta Bog naredil za nespametnost? (aiōn g165)
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn g165)
Vendar govorimo modrost med temi, ki so popolni; vendar ne modrosti tega sveta niti princev tega sveta, ki se izjalovi; (aiōn g165)
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn g165)
temveč govorimo Božjo modrost v skrivnosti, celó prikrito modrost, ki jo je Bog pred svetom odredil v našo slavo; (aiōn g165)
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn g165)
ki je nobeden izmed princev tega sveta ni spoznal. Kajti če bi jo spoznali, ne bi križali Gospoda slave. (aiōn g165)
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn g165)
Naj se noben človek ne vara. Če se komurkoli med vami zdi, da je v tem svetu moder, naj postane bedak, da bo lahko moder. (aiōn g165)
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn g165)
Zatorej, če jed stori, da se moj brat pohujša, dokler stoji svet ne bom jedel mesa, da ne bi svojega brata primoral grešiti. (aiōn g165)
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn g165)
Torej vse te stvari so se jim zgodile za zglede. Napisane pa so v svarilo nam, nad katere so prišli konci sveta. (aiōn g165)
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs g86)
Oh smrt, kje je tvoje želo? Oh grob, kje je tvoja zmaga?‹ (Hadēs g86)
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn g165)
v katerih je bog tega sveta zaslepil misli tistih, ki ne verujejo, da jim ne bi zasijala svetloba veličastnega Kristusovega evangelija, ki je podoba Boga. (aiōn g165)
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios g166)
Kajti naša lahka stiska, ki je samo za trenutek, opravlja za nas veliko večjo, presegajočo in večno težo slave; (aiōnios g166)
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios g166)
medtem ko ne gledamo na stvari, ki so vidne, temveč na stvari, ki so nevidne. Kajti stvari, ki so vidne, so začasne, toda stvari, ki so nevidne, so večne. (aiōnios g166)
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios g166)
Kajti vemo, da če bi naša zemeljska hiša tega šotorskega svetišča razpadla, imamo v nebesih večno Božjo stavbo, hišo ne narejeno z rokami. (aiōnios g166)
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn g165)
(kakor je pisano: ›Razdelil je povsod, dal je revnim. Njegova pravičnost ostaja na veke.‹ (aiōn g165)
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn g165)
Bog in Oče našega Gospoda Jezusa Kristusa, ki je blagoslovljen na vékomaj, ve, da ne lažem. (aiōn g165)
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn g165)
ki je samega sebe dal za naše grehe, da nas lahko osvobodi iz tega sedanjega hudobnega sveta, glede na voljo Boga in našega Očeta, (aiōn g165)
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
ki mu bodi slava na veke vekov. Amen.‹ (aiōn g165)
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios g166)
Kajti kdor seje v svoje meso, bo od mesa požel trohljivost; toda kdor seje v Duha, bo od Duha požel večno življenje. (aiōnios g166)
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn g165)
daleč nad vsako kneževino in oblast in moč in gospostvo ter [nad] vsako ime, ki je poimenovano ne samo na tem svetu, temveč tudi na tem, ki prihaja. (aiōn g165)
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn g165)
v katerih ste v preteklem času živeli glede na način tega sveta, glede na princa oblasti zraka, duha, ki sedaj deluje v otrocih neposlušnosti; (aiōn g165)
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn g165)
da bi v prihajajočih časih lahko pokazal izjemna bogastva svoje milosti v svoji prijaznosti do nas po Kristusu Jezusu. (aiōn g165)
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn g165)
in storil, da vsi ljudje vidijo, kakšna je družba skrivnosti, ki je bila od začetka sveta skrita v Bogu, ki je po Jezusu Kristusu ustvaril vse stvari; (aiōn g165)
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn g165)
glede na večen namen, ki ga je nameraval v Kristusu Jezusu, našem Gospodu, (aiōn g165)
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
njemu bodi slava v cerkvi po Kristusu Jezusu skozi vsa obdobja, od veka do veka. Amen. (aiōn g165)
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn g165)
Kajti ne borimo se proti mesu in krvi, temveč proti kneževinam, proti oblastem, proti vladarjem teme tega sveta, proti duhovni zlobnosti na visokih položajih. (aiōn g165)
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Torej Bogu in našemu Očetu bodi slava na veke vekov. Amen. (aiōn g165)
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn g165)
celó skrivnost, ki je bila skrita pred veki in pred rodovi, toda sedaj je razodeta njegovim svetim, (aiōn g165)
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios g166)
ki bodo kaznovani z večnim uničenjem proč od Gospodove prisotnosti in proč od slave njegove moči; (aiōnios g166)
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios g166)
Torej sam naš Gospod Jezus Kristus in Bog, celó naš Oče, ki nas je ljubil in nam je po milosti dal večno tolažbo ter dobro upanje, (aiōnios g166)
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios g166)
Vendar sem zaradi tega razloga dosegel usmiljenje, da bi Jezus Kristus lahko vnaprej na meni pokazal vso potrpežljivost za vzor tem, ki naj bi odslej verovali vanj za večno življenje. (aiōnios g166)
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Torej Kralju, večnemu, nesmrtnemu, nevidnemu, edinemu modremu Bogu, bodi čast in slava na veke vekov. Amen. (aiōn g165)
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios g166)
Bojuj dober boj vere, oprimi se večnega življenja, kamor si tudi poklican in si pred mnogimi pričami izpovedal dobro izpoved. (aiōnios g166)
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios g166)
ki ima edini nesmrtnost in prebiva v svetlobi, ki sem mu noben človek ne more približati; katerega noben človek ni videl niti ne more videti; njemu bodi čast in večna oblast. Amen. (aiōnios g166)
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn g165)
Naročajte tem, ki so na tem svetu bogati, da naj ne bodo vzvišeni niti naj ne zaupajo v negotova bogastva, temveč v živega Boga, ki nam bogato daje v uživanje vse stvari; (aiōn g165)
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
ki nas je rešil in nas poklical s sveto poklicanostjo, ne glede na naša dela, temveč glede na svoj lastni namen in milost, ki nam je bila dana v Kristusu Jezusu pred začetkom sveta, (aiōnios g166)
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios g166)
Zato zaradi izvoljenih prenašam vse stvari, da bi lahko tudi oni dosegli rešitev duš, ki je v Kristusu Jezusu z večno slavo. (aiōnios g166)
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn g165)
kajti Demá me je zapustil, ker je vzljubil ta sedanji svet in je odpotoval v Tesaloníko; Kreskens v Galatijo, Tit v Dalmacijo. (aiōn g165)
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn g165)
In Gospod me bo osvobodil iz vsakega zlega dela in me ohranil za svoje nebeško kraljestvo. Njemu bodi slava na veke vekov. Amen. (aiōn g165)
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
v upanju večnega življenja, ki ga je Bog, ki ne more lagati, obljubil, preden je svet nastal; (aiōnios g166)
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn g165)
in nas uči, da naj bi v tem sedanjem svetu zanikali brezbožnost in posvetna poželenja, živeli trezno, pravično in bogaboječe (aiōn g165)
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios g166)
da naj bi, opravičeni po njegovi milosti, postali dediči glede na upanje večnega življenja. (aiōnios g166)
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios g166)
Kajti zato je mogoče za nekaj časa odpotoval, da bi ga sprejel za zmeraj; (aiōnios g166)
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn g165)
nam je v teh poslednjih dneh spregovoril po svojem Sinu, ki ga je določil [za] dediča vseh stvari, po katerem je tudi naredil svetove; (aiōn g165)
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn g165)
Toda sinu pravi: »Tvoj prestol, oh Bog, je na veke vekov; žezlo pravičnosti je žezlo tvojega kraljestva.« (aiōn g165)
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
Kakor pravi tudi na drugem mestu: »Ti si duhovnik na veke po Melkízedekovem redu.« (aiōn g165)
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios g166)
in ker je postal popoln, je postal avtor večne rešitve duš vsem tistim, ki ga ubogajo; (aiōnios g166)
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios g166)
nauka o krščevanjih in o polaganju rok in o vstajenju mrtvih ter o večni sodbi. (aiōnios g166)
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn g165)
in so okusili dobro Božjo besedo in moči sveta, ki pride, (aiōn g165)
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn g165)
kamor je za nas vstopil predhodnik, celó Jezus, postavljen [za] vélikega duhovnika na veke po Melkízedekovem redu. (aiōn g165)
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn g165)
Kajti on pričuje: »Ti si duhovnik na veke po Melkízedekovem redu.« (aiōn g165)
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn g165)
(kajti ti duhovniki so postali brez prisege; toda ta s prisego po tistem, ki mu je rekel: »Gospod je prisegel in se ne bo kesal: ›Ti si duhovnik na veke po Melkízedekovem redu‹«). (aiōn g165)
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn g165)
toda ta človek, ker ostaja večno, ima nespremenljivo duhovništvo. (aiōn g165)
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn g165)
Kajti postava dela ljudi [za] vélike duhovnike, ki imajo šibkost; toda beseda prisege, ki je bila, odkar [je] postava, postavlja Sina, ki je posvečen na vékomaj. (aiōn g165)
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios g166)
niti ne s krvjo koz in telet, temveč je s svojo lastno krvjo enkrat vstopil v sveti prostor in za nas dosegel večno odkupitev. (aiōnios g166)
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios g166)
koliko bolj bo Kristusova kri, ki je po večnem Duhu samega sebe brez madeža daroval Bogu, očistila vašo vest pred mrtvimi deli, da služite živemu Bogu? (aiōnios g166)
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios g166)
In zaradi tega razloga je on posrednik nove zaveze, da bi s pomočjo smrti, za odkupitev od prestopkov, ki so bili pod prvo zavezo, tisti, ki so poklicani, lahko prejeli obljubo večne dediščine. (aiōnios g166)
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn g165)
kajti potem bi moral od ustanovitve sveta pogosto trpeti. Toda sedaj se je prikazal enkrat ob koncu sveta, da z žrtvovanjem samega sebe odstrani greh. (aiōn g165)
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn g165)
Po veri razumemo, da so bili svetovi zasnovani po Božji besedi, tako da stvari, ki so vidne, niso bile narejene iz stvari, ki se kažejo. (aiōn g165)
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn g165)
Jezus Kristus, isti včeraj in danes in na veke. (aiōn g165)
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios g166)
Torej Bog miru, ki je od mrtvih ponovno privedel našega Gospoda Jezusa, ta véliki pastir ovc, naj vas po krvi večne zaveze, (aiōnios g166)
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn g165)
naredi popolne v vsakem dobrem delu, da izpolnite njegovo voljo, ki povzroča v vas to, kar je prijetno v njegovem pogledu, po Jezusu Kristusu, ki mu bodi slava na veke vekov. Amen. (aiōn g165)
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna g1067)
In jezik je ogenj, svet krivičnosti. Tako je jezik med našimi udi, da omadežuje celotno telo in razvnema zakon narave; in ta je vžgan iz pekla. (Geenna g1067)
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn g165)
ker ste ponovno rojeni, ne iz trohljivega semena, temveč iz netrohljivega, po Božji besedi, ki živi in ostaja na veke. (aiōn g165)
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn g165)
toda Gospodova beseda vztraja za vedno. In to je beseda, ki vam je oznanjena po evangeliju. (aiōn g165)
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
Če katerikoli človek govori, naj govori kakor Božje izreke; če katerikoli človek služi, naj to opravlja kakor iz zmožnosti, ki jo daje Bog; da bo v vseh stvareh Bog lahko proslavljen po Jezusu Kristusu, ki mu bodi hvala in gospostvo na veke vekov. Amen. (aiōn g165)
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios g166)
Toda Bog vse milosti, ki nas je poklical v svojo večno slavo po Kristusu Jezusu, potem ko ste nekaj časa trpeli, vas stori popolne, utrjene, okrepljene, vas ustali. (aiōnios g166)
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn g165)
Njemu bodi slava in gospostvo na veke vekov. Amen. (aiōn g165)
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios g166)
kajti tako vam bo razkošno odprt vstop v večno kraljestvo našega Gospoda in Odrešenika Jezusa Kristusa. (aiōnios g166)
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō g5020)
Kajti če Bog ni prizanesel angelom, ki so grešili, temveč jih je vrgel navzdol v pekel in jih izročil verigam teme, da bodo pridržani do sodbe, (Tartaroō g5020)
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Temveč rastite v milosti in v spoznanju našega Gospoda in Odrešenika Jezusa Kristusa. Njemu bodi slava tako sedaj in na veke. Amen. (aiōn g165)
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios g166)
(kajti življenje je bilo jasno pokazano in videli smo ga in pričujemo in vam kažemo to večno življenje, ki je bilo z Očetom in je bilo jasno pokazano nam), (aiōnios g166)
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn g165)
In svet mineva in njegovo poželenje; kdor pa izpolnjuje Božjo voljo, ostaja na veke. (aiōn g165)
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios g166)
In to je obljuba, ki nam jo je obljubil, celó večno življenje. (aiōnios g166)
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios g166)
Kdorkoli sovraži svojega brata, je morilec; in veste, da noben morilec nima večnega življenja, ki [bi] ostajalo v njem. (aiōnios g166)
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios g166)
In to je zapis, da nam je Bog dal večno življenje in to življenje je v njegovem Sinu. (aiōnios g166)
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
Te besede sem napisal vam, ki verujete v ime Božjega Sina; da boste lahko vedeli, da imate večno življenje in da lahko verujete v ime Božjega Sina. (aiōnios g166)
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios g166)
In mi vemo, da je Božji Sin prišel ter nam dal razumevanje, da bi lahko spoznali tistega, ki je resničen in mi smo v njem, ki je resničen, celó v njegovem Sinu Jezusu Kristusu. Ta je resničen Bog in večno življenje. (aiōnios g166)
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn g165)
zaradi resnice, ki prebiva v nas in bo za vedno z nami. (aiōn g165)
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios g126)
In angele, ki niso obdržali svojega prvega stanja, temveč so zapustili svoje prebivališče, je ohranil v večnih verigah pod temo, do sodbe vélikega dne. (aïdios g126)
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios g166)
Celó kakor so Sódoma in Gomóra in na podoben način mesta okoli njiju, ki so same sebe predajala v prešuštvo in hodila za tujim mesom, postavljena kot zgled, trpeč maščevanje večnega ognja. (aiōnios g166)
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn g165)
besneči morski valovi, ki se penijo od svoje lastne sramote; blodeče zvezde, ki jim je za vedno prihranjena črna temà. (aiōn g165)
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios g166)
ohranite se v Božji ljubezni, pričakujte usmiljenje našega Gospoda Jezusa Kristusa, za večno življenje. (aiōnios g166)
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
edinemu modremu Bogu, našemu Odrešeniku, bodi slava in veličanstvo, gospostvo in oblast, tako sedaj kot na veke. Amen. (aiōn g165)
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn g165)
in nas naredil kralje in duhovnike Bogu ter svojemu Očetu; njemu bodi slava in gospostvo na veke vekov. Amen. (aiōn g165)
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn g165, Hadēs g86)
Jaz sem ta, ki živi in je bil mrtev; in glej, živ sem na vékomaj, Amen; in ključe imam od pekla in od smrti. (aiōn g165, Hadēs g86)
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn g165)
In ko so te živali dale slavo in čast in zahvalo njemu, ki je sedel na prestolu, ki živi na veke vekov, (aiōn g165)
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn g165)
je štiriindvajset starešin padlo dol pred njim, ki je sedel na prestolu in oboževalo njega, ki živi na veke vekov in svoje krone vrglo pred prestol, rekoč: (aiōn g165)
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn g165)
In vsako ustvarjeno bitje, ki je na nebu in na zemlji in pod zemljo in takšna, kot so v morju in vse, ki so v njem, sem slišal govoriti: »Blagoslov in čast in slava in oblast naj bo njemu, ki sedi na prestolu in Jagnjetu na veke vekov.« (aiōn g165)
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs g86)
In pogledal sem in zagledal konja mrtvaško blede barve; in tistemu, ki je sedel na konju, je bilo ime Smrt in Pekel je sledil za njim. In izročena jima je bila oblast nad četrtino zemlje, da ubijata z mečem in z lakoto in s smrtjo in z zemeljskimi živalmi. (Hadēs g86)
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn g165)
rekoč: »Amen: ›Blagoslov, slava, modrost, zahvaljevanje, čast, oblast in moč bodi našemu Bogu na veke vekov. Amen.‹« (aiōn g165)
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos g12)
In zatrobil je peti angel in videl sem zvezdo pasti z neba na zemljo in dan mu je bil ključ od jame brez dna. (Abyssos g12)
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos g12)
In odprl je jamo brez dna in iz jame se je dvignil dim kakor dim velike talilne peči; in zaradi dima iz jame sta potemnela sonce in zrak. (Abyssos g12)
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos g12)
In nad seboj so imele kralja, ki je angel iz jame brez dna, katerega ime je v hebrejskem jeziku Ábadon, toda v grškem jeziku ima svoje ime Apolíon. (Abyssos g12)
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn g165)
in prisegel pri njem, ki živi na veke vekov, ki je ustvaril nebo in stvari, ki so na njem in zemljo in stvari, ki so na njej in morje in stvari, ki so v njem, da naj ne bi bilo več časa, (aiōn g165)
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos g12)
In ko bosta končala svoje pričevanje, se bo iz jame brez dna povzpel zvernik, ki bo povzročil vojno proti njima in ju premagal ter ju ubil. (Abyssos g12)
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn g165)
In zatrobil je sedmi angel in na nebu so bili močni glasovi, govoreč: »Kraljestva tega sveta so postala kraljestva našega Gospoda in njegovega Kristusa in vladal bo na veke vekov.« (aiōn g165)
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios g166)
In videl sem drugega angela leteti po sredi neba, ki je imel večen evangelij, da ga oznani tem, ki prebivajo na zemlji in vsakemu narodu, sorodstvu, jeziku in ljudem, (aiōnios g166)
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn g165)
in dim njihovega mučenja se vzpenja na veke vekov in ne podnevi ne ponoči nima počitka, kdor obožuje zvernika ter njegovo podobo in kdorkoli sprejme znamenje njegovega imena. (aiōn g165)
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn g165)
In ena izmed štirih živali je dala sedmim angelom sedem zlatih stekleničk, polnih besa Boga, ki živi na veke vekov. (aiōn g165)
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos g12)
Zvernik, ki si ga videl, je bil in ga ni in vzpel se bo iz jame brez dna in šel v pogubo in tisti, ki prebivajo na zemlji, katerih imena od ustanovitve sveta niso bila zapisana v knjigi življenja, se bodo čudili, ko bodo gledali zvernika, ki je bil in ga ni, pa vendar je. (Abyssos g12)
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn g165)
In ponovno so rekli: »Aleluja. In njen dim se je vzdigoval na veke vekov.« (aiōn g165)
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr g3041 g4442)
In zvernik je bil ujet in z njim lažni prerok, ki je delal čudeže pred njim, s katerimi je zavajal te, ki so sprejeli znamenje zvernika in te, ki so oboževali njegovo podobo. Oba sta bila živa vržena v ognjeno jezero, goreče z žveplom. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos g12)
In videl sem angela priti dol z neba, ki je imel v svoji roki ključ od jame brez dna ter veliko verigo. (Abyssos g12)
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos g12)
in ga vrgel v jamo brez dna in ga zaprl ter zapečatil nad njim, da naj ne bi več zavajal narodov, dokler se ne bi dopolnilo tisoč let, potem pa mora biti malo časa odvezan. (Abyssos g12)
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
Hudič, ki jih je zavedel, pa je bil vržen v ognjeno in žvepleno jezero, kjer sta zvernik in lažni prerok in mučeni bodo dan in noč, na veke vekov. (aiōn g165, Limnē Pyr g3041 g4442)
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs g86)
In morje se je odreklo mrtvim, ki so bili v njem; in smrt in pekel sta izročila mrtve, ki so bili v njiju in bili so sojeni, vsak glede na svoja dela. (Hadēs g86)
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
In smrt in pekel sta bila vržena v ognjeno jezero. To je druga smrt. (Hadēs g86, Limnē Pyr g3041 g4442)
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr g3041 g4442)
In kdorkoli ni bil najden zapisan v knjigi življenja, je bil vržen v ognjeno jezero. (Limnē Pyr g3041 g4442)
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr g3041 g4442)
Toda strahopetci, neverniki, gnusneži, morilci, vlačugarji, čarodeji, malikovalci in vsi lažnivci bodo imeli svoj delež v jezeru, ki gori z ognjem in žveplom, kar je druga smrt.« (Limnē Pyr g3041 g4442)
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn g165)
In tam ne bo noči in ne potrebujejo nobene sveče niti sončne svetlobe, kajti Gospod Bog jim daje svetlobo in kraljevali bodo na veke vekov. (aiōn g165)

CHW > Aionian Verses: 264
SLV > Aionian Verses: 264