Aionian Verses
Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol )
Vsi njegovi sinovi in vse njegove hčere so vstali, da ga potolažijo, toda odklonil je, da bi bil potolažen in rekel je: »Kajti žalujoč bom šel v grob k svojemu sinu.« Tako je njegov oče jokal za njim. (Sheol )
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol )
Rekel je: »Moj sin ne bo šel dol s teboj, kajti njegov brat je mrtev, on pa je ostal sam. Če ga po poti, na katero greste, zadene nesreča, potem boste moje sive lase z bridkostjo privedli do groba.« (Sheol )
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol )
Če tudi tega vzamete od mene in ga zadene nesreča, boste moje sive lase z bridkostjo privedli do groba.‹ (Sheol )
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol )
se bo zgodilo, ko bo videl, da dečka ni z nami, da bo umrl. Tvoji služabniki bodo sive lase tvojega služabnika, našega očeta, z bridkostjo privedli do groba. (Sheol )
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol )
Toda če Gospod naredi novo stvar in zemlja odpre svoja usta in jih požre, z vsem, kar jim pripada in gredo hitro dol v jamo, potem boste razumeli, da so ti ljudje izzivali Gospoda.« (Sheol )
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol )
Oni in vsi, ki so pripadali k njim, so živi odšli dol v jamo, in zemlja se je zaprla nad njimi in izginili so iz skupnosti. (Sheol )
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol )
Kajti v moji jezi je vžgan ogenj in gorel bo do najnižjega pekla in použil bo zemljo z njenim narastom in vžgal bo temelje gora. (Sheol )
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol )
Gospod ubija in oživlja. Privede dol do groba in privede gor. (Sheol )
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
bridkosti pekla so me obkrožile, zanke smrti so me ovirale; (Sheol )
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol )
Stori torej glede na svojo modrost in ne dopusti, da bi njegova osivela glava šla v miru dol v podzemlje. (Sheol )
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol )
Zdaj ga torej ne imej brez krivde, kajti moder človek si in veš, kaj mu moraš storiti, temveč njegovo osivelo glavo s krvjo privedi dol k podzemlju.« (Sheol )
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol )
Kakor je oblak použit in izginil proč, tako kdor gre dol h grobu, ne bo več prišel gor. (Sheol )
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol )
To je tako visoko kakor nebo. Kaj lahko storiš? Globlje kakor pekel. Kaj lahko spoznaš? (Sheol )
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol )
Oh, da bi me hotel skriti v grob, da bi me varoval na skrivnem, dokler tvoj bes ne mine, da bi mi določil določeni čas in me spomnil! (Sheol )
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol )
Če čakam, je moja hiša grob; svojo posteljo sem postlal v temi. (Sheol )
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol )
Šli bodo dol k zapahom jame, ko je naš skupni počitek v prahu.« (Sheol )
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol )
Svoje dni preživijo v obilju in v trenutku gredo dol v grob. (Sheol )
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol )
Suša in vročina použijeta snežne vode; tako grob tiste, ki so grešili. (Sheol )
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol )
Pekel je nag pred njim in uničenje nima pokrivala. (Sheol )
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol )
Kajti v smrti ni spomina nate. Kdo se ti bo zahvaljeval v grobu? (Sheol )
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol )
Zlobni bodo napoteni v pekel in vsi narodi, ki pozabljajo Boga. (Sheol )
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
Kajti moje duše ne boš pustil v peklu niti ne boš trpel, da bi tvoj Sveti videl trohnobo. (Sheol )
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
Obkrožile so me bridkosti pekla. Zanke smrti so me ovirale. (Sheol )
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol )
Oh Gospod, mojo dušo si privedel iz groba. Ohranil si me živega, da ne bi šel dol v jamo. (Sheol )
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol )
Naj ne bom osramočen, oh Gospod, kajti klical sem k tebi. Naj bodo zlobni osramočeni in naj bodo molče v grobu. (Sheol )
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol )
Kakor ovce so položeni v grob; z njimi se bo hranila smrt in iskreni bodo zjutraj imeli nad njimi oblast in njihova lepota bo požrta v grobu, proč od njihovega bivanja. (Sheol )
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol )
Toda Bog bo mojo dušo odkupil iz oblasti groba, kajti sprejel me bo. (Sela) (Sheol )
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol )
Naj se jih polasti smrt in naj hitro gredo dol v pekel, kajti zlobnost je v njihovih bivališčih in med njimi. (Sheol )
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol )
Kajti veliko je tvoje usmiljenje do mene in mojo dušo si osvobodil pred najglobljim peklom. (Sheol )
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol )
kajti moja duša je polna stisk in moje življenje se bliža grobu. (Sheol )
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol )
Kateri človek je, kdor živi in ne bo videl smrti? Ali bo svojo dušo osvobodil pred roko groba? (Sela) (Sheol )
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol )
Obdale so me bridkosti smrti in bolečine pekla so me prijele; spoznal sem stisko in bridkost. (Sheol )
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol )
Če se povzpnem v nebesa, si tam; če si svojo posteljo pripravim v peklu, glej, si tam. (Sheol )
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol )
Naše kosti so razkropljene ob ustih groba, kakor kadar nekdo seka in cepi les na zemlji. (Sheol )
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol )
požrimo jih žive kakor grob in cele, kakor tiste, ki gredo dol v jamo. (Sheol )
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol )
Njena stopala gredo dol k smrti, njeni koraki se prijemljejo pekla. (Sheol )
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol )
Njena hiša je pot v pekel, spuščajoča se k celicam smrti.… (Sheol )
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol )
Toda ta ne spozna, da so tam mrtvi in da so njeni gostje v globinah pekla. (Sheol )
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol )
Pekel in uničenje sta pred Gospodom, koliko bolj potem srca človeških otrok? (Sheol )
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol )
Pot življenja je modremu zgoraj, da lahko odide od pekla spodaj. (Sheol )
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol )
Udaril ga boš s šibo, njegovo dušo pa boš rešil pred peklom. (Sheol )
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol )
Pekel in uničenje nikdar nista polna, tako človekove oči nikoli niso nasičene. (Sheol )
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol )
grob in jalova maternica; zemlja, ki ni nasičena z vodo; in ogenj, ki ne govori: »Dovolj je.« (Sheol )
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol )
Karkoli tvoja roka najde, da stori, to stôri z vso svojo močjo, kajti v grobu, kamor greš, ni dela, niti naklepa, niti spoznanja, niti modrosti. (Sheol )
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol )
Postavi me kakor pečat na svoje srce, kakor pečat na svoj laket, kajti ljubezen je močna kakor smrt, ljubosumje je kruto kakor grob. Njegovi ogorki so ognjeno oglje, ki ima najbolj silovit plamen. (Sheol )
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol )
Zato se bo pekel povečal in svoja usta odprl brez mere. Njihova slava, njihova množica, njihov pomp in kdor se razveseljuje, se bo pogreznil vanj. (Sheol )
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol )
»Izprosi si znamenje od Gospoda, svojega Boga, prosi ga ali v globini ali na višini zgoraj.« (Sheol )
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol )
Pekel od spodaj vztrepetava zaradi tebe, da te sreča ob tvojem prihodu. Zaradi tebe razvnema mrtve, celó vse zemeljske vodje, iz njihovih prestolov je dvignil vse kralje narodov. (Sheol )
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol )
Tvoj pomp je priveden dol h grobu in zvok tvojih lir. Ličinka se razteguje pod teboj in ličinke te pokrivajo. (Sheol )
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol )
Vendar boš priveden dol v pekel, na obronke jame. (Sheol )
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol )
Ker ste rekli: »Sklenili smo zavezo s smrtjo in s peklom smo v dogovoru. Ko bo šel skozi poplavljajoč bič, ta ne bo prišel k nam, kajti laži smo naredili za svoje zatočišče in pod neresnico smo se skrili.« (Sheol )
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol )
Vaša zaveza s smrtjo bo razveljavljena in vaš dogovor s peklom ne bo obstal; ko bo skozi šel preplavljajoč bič, potem boste z njim pomendrani. (Sheol )
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol )
»Rekel sem o preostanku svojih dni: ›Šel bom do velikih vrat groba. Prikrajšan sem preostanka svojih let.‹ (Sheol )
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol )
Kajti grob te ne more hvaliti, smrt te ne more proslavljati. Tisti, ki gredo dol v jamo, ne morejo upati na tvojo resnico. (Sheol )
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol )
Odhajaš h kralju z mazilom, množila si svoje dišave, svoje poslance si poslala daleč in sebe si ponižala celo do pekla. (Sheol )
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol )
Tako govori Gospod Bog: ›Na dan, ko je šel dol do groba, sem povzročil žalovanje. Zanj sem pokril globino in omejil njegove tokove in velike vode so bile ustavljene. Libanonu sem storil, da je žaloval za njim in vsa poljska drevesa so medlela zaradi njega. (Sheol )
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol )
Narodom sem storil, da se tresejo ob zvoku njegovega padca, ko sem ga vrgel dol do pekla, s tistimi, ki se spuščajo v jamo in vsa edenska drevesa, izbrana in najboljša iz Libanona, vsa, ki pijejo vodo, bodo potolažena v spodnjih delih zemlje. (Sheol )
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol )
Tudi oni so z njim odšli dol v pekel, k tistim, ki so umorjeni z mečem; in tisti, ki so bili njegov laket, ki so prebivali pod njegovo senco v sredi narodov. (Sheol )
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol )
Močni izmed mogočnih mu bodo govorili iz srede pekla s tistimi, ki mu pomagajo. Odšli so dol, ležijo neobrezani, umorjeni z mečem. (Sheol )
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol )
Ne bodo ležali z mogočnimi, ki so padli od neobrezancev, ki so odšli dol k peklu z njihovimi bojnimi orožji. Njihove meče so položili pod njihove glave, toda njihove krivičnosti bodo na njihovih kosteh, čeprav so bili strahota mogočnih v deželi živih. (Sheol )
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol )
Odkupil jih bom pred oblastjo groba; odkupil jih bom pred smrtjo. ›Oh smrt, jaz bom tvoje kuge; ‹ ›Oh grob, jaz bom tvoje uničenje.‹ Kesanje bo skrito mojim očem. (Sheol )
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol )
Čeprav kopljejo v pekel, jih bo moja roka vzela od tam. Čeprav plezajo gor do nebes, jih bom od tam privedel dol. (Sheol )
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol )
in rekel: »Zaradi razloga svoje stiske sem klical h Gospodu in me je slišal. Ven iz trebuha pekla sem klical in ti si slišal moj glas. (Sheol )
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol )
Da, prav tako, ker greši z vinom, je ponosen človek niti se ne drži doma, ki svojo željo povečuje kakor pekel in je kakor smrt in ne more biti nasičen, temveč k sebi zbira vse narode in k sebi kopiči vsa ljudstva. (Sheol )
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna )
Toda povem vam: ›Da kdorkoli je brez razloga jezen na svojega brata, bo v nevarnosti sodbe, ‹ in kdorkoli bo svojemu bratu rekel: ›Raka, ‹ bo v nevarnosti pred vélikim zborom. Toda kdorkoli bo rekel: ›Ti bedak, ‹ bo v nevarnosti peklenskega ognja. (Geenna )
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
In če te tvoje desno oko pohujšuje, ga iztakni in ga vrzi od sebe; kajti zate je koristno, da bi eden izmed tvojih udov propadel in ne, da bi tvoje celó telo moralo biti vrženo v pekel. (Geenna )
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
In če te tvoja desnica pohujšuje, jo odsekaj in jo vrzi od sebe; kajti zate je koristno, da bi eden izmed tvojih udov propadel, ne pa da bi tvoje celó telo moralo biti vrženo v pekel. (Geenna )
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna )
In ne bojte se tistih, ki ubijejo telo, toda niso zmožni ubiti duše, temveč se raje bojte njega, ki je zmožen uničiti tako dušo kakor telo v peklu. (Geenna )
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs )
In ti, Kafarnáum, ki si bil vzvišen do neba, boš priveden navzdol do pekla; kajti če bi se mogočna dela, ki so bila storjena v tebi, zgodila v Sódomi, bi preostala do današnjega dne.‹ (Hadēs )
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn )
In kdorkoli govori besedo zoper Sina človekovega, mu bo to odpuščeno; toda kdorkoli govori zoper Svetega Duha, mu ne bo odpuščeno ne na tem svetu ne v svetu, ki pride.‹ (aiōn )
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn )
Tudi tisti, ki je seme sprejel med trnje, je tisti, ki sliši besedo. Skrb tega sveta in zapeljivost bogastev pa zadušita besedo in on postaja brez sadu. (aiōn )
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn )
Sovražnik, ki jih je posejal, je hudič. Žetev je konec sveta, žanjci pa so angeli. (aiōn )
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn )
Kakor je torej plevel pobran in v ognju sežgan, tako bo ob koncu tega sveta. (aiōn )
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn )
Tako bo torej ob koncu sveta. Prišli bodo angeli in zlobne bodo oddvojili od pravičnih, (aiōn )
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs )
In jaz ti prav tako pravim: ›Da si ti Peter in na tej skali bom zgradil svojo cerkev in velika vrata pekla ne bodo prevladala proti njej. (Hadēs )
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios )
Zatorej, če te tvoja roka ali tvoje stopalo pohujšuje, ju odsekaj proč in ju vrzi od sebe. Bolje je zate, da v življenje vstopiš šepav ali pohabljen, raje kakor imeti dve roki ali dve stopali in biti vržen v večni ogenj. (aiōnios )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna )
In če te tvoje oko pohujšuje, ga iztakni in ga vrzi od sebe. Bolje je zate, da vstopiš v življenje z enim očesom, raje kakor imeti dve očesi in biti vržen v peklenski ogenj. (Geenna )
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios )
In glej, nekdo je prišel ter mu rekel: »Dobri Učitelj, katero dobro stvar naj storim, da bom lahko imel večno življenje?« (aiōnios )
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios )
In vsak, kdor je zaradi mojega imena zapustil hiše ali brate ali sestre ali očeta ali mater ali ženo ali otroke ali zemljišča, bo prejel stokratno in bo podedoval večno življenje. (aiōnios )
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn )
In ko je na poti zagledal figovo drevo, je prišel k njemu, pa na njem ni našel nič, razen listja samega in mu rekel: »Naj odslej na tebi nikoli več ne zraste noben sad.« In figovo drevo je takoj ovenelo. (aiōn )
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna )
Gorje vam, pisarji in farizeji, hinavci! Kajti obidete morje in zemljo, da naredite enega spreobrnjenca in ko je narejen, ga naredite dvakrat bolj otroka pekla, kakor ste sami. (Geenna )
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna )
Vi kače, vi gadji rod, kako lahko pobegnete obsodbi na pekel? (Geenna )
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn )
In ko je sedèl na Oljski gori, so k njemu zaupno prišli učenci, rekoč: »Povej nam, kdaj bodo te stvari? In kakšno bo znamenje tvojega prihoda in konca sveta?« (aiōn )
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios )
Tedaj bo prav tako rekel tem na levici: ›Odidite od mene, vi prekleti, v večni ogenj, pripravljen za hudiča in njegove angele; (aiōnios )
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios )
In ti bodo šli proč v večno kazen, toda pravični v večno življenje.« (aiōnios )
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn )
učeč jih obeleževati vse besede, katerekoli sem vam zapovedal. In glejte, jaz sem z vami vedno, celó do konca sveta. Amen.« (aiōn )
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn , aiōnios )
toda kdor bo preklinjal zoper Svetega Duha, nima nikoli odpuščanja, temveč je v nevarnosti večnega prekletstva, ‹« (aiōn , aiōnios )
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn )
in skrbi tega sveta, zapeljivost bogastev in poželenja po drugih stvareh vstopijo, zadušijo besedo in ta postane brezplodna. (aiōn )
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna )
In če te tvoja roka pohujšuje, jo odsekaj proč; bolje je zate, da vstopiš v življenje pohabljen, kakor imeti dve roki in iti v pekel, v ogenj, ki ne bo nikoli pogašen, (Geenna )
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna )
In če te tvoje stopalo pohujšuje, ga odsekaj proč; bolje je zate, da vstopiš v življenje šepav, kakor imeti dve stopali in biti vržen v pekel, v ogenj, ki ne bo nikoli pogašen, (Geenna )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna )
In če te tvoje oko pohujšuje, ga iztakni ven; bolje je zate, da vstopiš v Božje kraljestvo z enim očesom, kakor biti z dvema očesoma vržen v peklenski ogenj, (Geenna )
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
In ko je odšel naprej po poti, je nekdo pritekel in pokleknil k njemu ter ga prosil: »Dobri Učitelj, kaj naj storim, da bom lahko podedoval večno življenje?« (aiōnios )
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn , aiōnios )
toda prejel bo stokratno, sedaj, v tem času, hiš in bratov in sester in mater in otrok in zemljišč s preganjanji; in večno življenje v svetu, ki pride. (aiōn , aiōnios )
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn )
In Jezus je odgovoril ter mu rekel: »Nihče naj od tebe odslej nikoli več ne jé sadu.« In njegovi učenci so to slišali. (aiōn )
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn )
in nad Jakobovo hišo bo vladal večno in njegovemu kraljestvu ne bo konca.« (aiōn )
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn )
kakor je govoril našim očetom, Abrahamu in njegovemu semenu na veke.« (aiōn )
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn )
kakor je govoril po ustih svojih svetih prerokov, ki so bili, odkar je svet nastal, (aiōn )
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos )
In rotili so ga, da jim ne bi ukazal oditi ven, v brezno. (Abyssos )
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs )
In ti Kafarnáum, ki si vzvišen do neba, boš pahnjen navzdol do pekla. (Hadēs )
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios )
In glej, nek izvedenec v postavi je vstal ter ga skušal, rekoč: »Učitelj, kaj naj storim, da podedujem večno življenje?« (aiōnios )
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna )
Toda posvaril vas bom, koga se bojte: ›Bojte se njega, ki ima, potem ko je ubil, oblast, da vrže v pekel.‹ Da, pravim vam: ›Bojte se ga.‹ (Geenna )
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn )
In gospodar je pohvalil nepravičnega oskrbnika, ker je modro ravnal, kajti otroci tega sveta so v svojem rodu modrejši od otrok svetlobe. (aiōn )
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios )
In pravim vam: ›Prijatelje si pridobivajte s krivičnim mamonom, da vas, ko padete, lahko sprejmejo v večna prebivališča.‹ (aiōnios )
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs )
in v peklu je povzdignil svoje oči, medtem ko je bil mučen in daleč stran zagledal Abrahama in Lazarja v njegovem naročju. (Hadēs )
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
In nek vladar ga je vprašal, rekoč: »Dobri Učitelj, kaj naj storim, da bom podedoval večno življenje?« (aiōnios )
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
ki ne bo prejel mnogokrat več v tem sedanjem času in večno življenje v svetu, ki pride.‹« (aiōn , aiōnios )
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn )
Jezus jim odgovori in reče: »Otroci tega sveta se poročajo in so dane v zakon, (aiōn )
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn )
toda tisti, ki bodo šteti za vredne, da dosežejo oni svet in vstajenje od mrtvih, se ne bodo niti poročali, niti ne bodo dane v zakon, (aiōn )
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
da se, kdorkoli veruje vanj, ne bo pogubil, temveč bo imel večno življenje. (aiōnios )
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Kajti Bog je tako ljubil svet, da je dal svojega edinorojenega Sina, da kdorkoli veruje vanj, se ne bo pogubil, temveč bo imel večno življenje. (aiōnios )
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios )
Kdor veruje v Sina, ima večno življenje; kdor pa ne veruje Sinu, ne bo videl življenja, temveč na njem ostaja Božji bes.« (aiōnios )
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
toda kdorkoli pije od vode, ki mu jo bom jaz dal, ne bo nikoli žejen, temveč bo voda, ki mu jo bom jaz dal, postala v njem izvir vode, ki izvira v večno življenje.« (aiōn , aiōnios )
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios )
In kdor žanje, prejema plače in zbira sad za večno življenje, da se lahko skupaj veselita oba, kdor seje in kdor žanje. (aiōnios )
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios )
Resnično, resnično, povem vam: ›Kdor sliši mojo besedo in veruje vanj, ki me je poslal, ima večno življenje in ne bo prišel v obsodbo, temveč je iz smrti prešel v življenje.‹ (aiōnios )
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios )
Preiskujete pisma, kajti v njih mislite, [da] imate večno življenje. To pa so ta, ki pričujejo o meni. (aiōnios )
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios )
Ne trudite se za jed, ki propada, temveč za jed, ki vzdrži v večno življenje, ki vam jo bo dal Sin človekov, kajti njega je potrdil Oče Bog.« (aiōnios )
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios )
In to je volja tistega, ki me je poslal, da bo vsakdo, ki vidi Sina in veruje vanj, lahko imel večno življenje in jaz ga bom dvignil na poslednji dan.« (aiōnios )
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios )
Resnično, resnično, povem vam: ›Kdor veruje vame, ima večno življenje.‹ (aiōnios )
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn )
Jaz sem živi kruh, ki je prišel dol iz nebes. Če katerikoli človek od tega kruha jé, bo živel večno, in kruh, ki ga bom jaz dal, je moje meso, ki ga bom dal za življenje sveta.« (aiōn )
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios )
Kdorkoli jé moje meso in pije mojo kri, ima večno življenje in jaz ga bom dvignil na poslednji dan.‹ (aiōnios )
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn )
To je ta kruh, ki je prišel dol iz nebes. Ne kakor vaši očetje, ki so jedli mano in so mrtvi. Kdor jé od tega kruha, bo živel večno.« (aiōn )
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios )
Potem mu je Simon Peter odgovoril: »Gospod, h komu naj gremo? Ti imaš besede večnega življenja. (aiōnios )
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn )
In služabnik v hiši ne ostaja za vedno, toda Sin ostaja večno. (aiōn )
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn )
Resnično, resnično, povem vam: ›Če se človek drži moje besede, nikoli ne bo videl smrti.‹« (aiōn )
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn )
Tedaj so mu Judje rekli: »Torej, mi vemo, da imaš hudiča. Abraham je mrtev in preroki; ti pa praviš: ›Če se človek drži moje besede, nikoli ne bo okusil smrti.‹ (aiōn )
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn )
Odkar je svet nastal, se ni slišalo, da bi katerikoli človek odprl oči nekoga, ki je bil rojen slep. (aiōn )
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn , aiōnios )
in dam jim večno življenje in nikoli ne bodo propadle niti jih noben človek ne bo iztrgal iz moje roke. (aiōn , aiōnios )
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn )
In kdorkoli živi in veruje vame, ne bo nikoli umrl. Veruješ to?« (aiōn )
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios )
Kdor ima rad svoje življenje, ga bo izgubil; kdor pa svoje življenje na tem svetu sovraži, ga bo ohranil za večno življenje. (aiōnios )
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn )
Množica mu je odgovorila: »Iz postave smo slišali, da Kristus ostaja večno; in kako praviš ti: ›Sin človekov mora biti dvignjen?‹ Kdo je ta Sin človekov?« (aiōn )
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios )
In jaz vem, da je njegova zapoved večno življenje. Karkoli torej govorim, govorim tako, celó kakor mi je rekel Oče.« (aiōnios )
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn )
Peter mu reče: »Nikoli ne boš umival mojih stopal.« Jezus mu je odgovoril: »Če te ne umijem, nimaš deleža z menoj.« (aiōn )
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn )
In prosil bom Očeta in dal vam bo drugega Tolažnika, da bo lahko večno ostal z vami, (aiōn )
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios )
kakor si mu izročil oblast nad vsem mesom, da bi on lahko dal večno življenje tolikim, kolikor si mu jih dal. (aiōnios )
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios )
In to je večno življenje, da bi oni lahko spoznali tebe, edinega resničnega Boga in Jezusa Kristusa, ki si ga poslal. (aiōnios )
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs )
ker moje duše nočeš pustiti v peklu niti nočeš trpeti, da bi tvoj Sveti videl trohnenje. (Hadēs )
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs )
in ker je to videl vnaprej, je govoril o Kristusovem vstajenju, da njegova duša ni ostala v peklu niti njegovo meso ni videlo trohnenja. (Hadēs )
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn )
ki ga morajo sprejeti nebesa do časov obnovitve vseh stvari, ki jih je Bog govoril po ustih vseh svojih svetih prerokov, odkar je svet nastal. (aiōn )
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios )
Tedaj sta Pavel in Barnaba postala pogumna in rekla: »Potrebno je bilo, da bi se Božja beseda najprej spregovorila vam, toda ker ste jo postavili proč od sebe in sebe sodite nevredne večnega življenja, glejte, se obračava k poganom. (aiōnios )
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios )
In ko so pogani to slišali, so bili veseli in slavili Gospodovo besedo; in kolikor jih je bilo odrejenih za večno življenje, je verovalo. (aiōnios )
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn )
Bogu so vsa njegova dela znana od začetka sveta. (aiōn )
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios )
Kajti od stvarjenja sveta so nevidne stvari o njem jasno vidne, ker so razumljene po stvareh, ki so narejene; celó njegova večna moč in Božanstvo, tako da so brez opravičila. (aïdios )
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Ki so Božjo resnico zamenjali v laž in so bolj oboževali in služili stvarstvu kakor Stvarniku, ki je blagoslovljen na veke. Amen. (aiōn )
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios )
Večno življenje tem, ki si s potrpežljivim vztrajanjem v dobrem ravnanju prizadevajo za slavo in čast in nesmrtnost; (aiōnios )
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios )
da kakor je greh kraljeval za smrt, točno tako lahko milost kraljuje po pravičnosti za večno življenje po Jezusu Kristusu, našem Gospodu. (aiōnios )
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Toda sedaj, ko ste osvobojeni greha in ste postali služabniki Bogu, imate svoj sad v svetost in konec večno življenje. (aiōnios )
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios )
Kajti plačila za greh so smrt; toda Božji dar je večno življenje po Jezusu Kristusu, našem Gospodu. (aiōnios )
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
katerih so očetje in iz katerih je, glede na meso, prišel Kristus, ki je čez vse, Bog, blagoslovljen na veke. Amen. (aiōn )
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos )
ali: ›Kdo se bo spustil v brezno?‹ (to je, da Kristusa ponovno privede gor od mrtvih).« (Abyssos )
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē )
Kajti Bog jih je vse zaprl v nevero, da bi se lahko vseh usmilil. (eleēsē )
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
Kajti iz njega in preko njega in njemu so vse stvari; ki mu bodi slava na veke. Amen. (aiōn )
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn )
In ne bodite prilagojeni temu svetu, temveč bodite preobraženi s prenavljanjem svojega mišljenja, da boste lahko razločili, kaj je tista dobra, sprejemljiva in popolna Božja volja. (aiōn )
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios )
Torej njemu, ki je sposoben, da vas utrdi v skladu z mojim evangelijem in oznanjevanjem Jezusa Kristusa, glede na razodetje skrivnosti, ki je bila tajno čuvana od nastanka sveta, (aiōnios )
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios )
toda sedaj je razodeta in po pismih prerokov, glede na zapoved večnega Boga, razglašena vsem narodom zaradi poslušnosti veri; (aiōnios )
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn )
Bogu, edinemu modremu, bodi slava po Jezusu Kristusu na veke. Amen. [Napisano Rimljanom iz Korinta in poslano po služabnici Fojbi iz kenhrejske cerkve.] (aiōn )
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn )
Kje je modri? Kje je pisar? Kje je razpravljavec tega sveta? Mar ni modrosti tega sveta Bog naredil za nespametnost? (aiōn )
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn )
Vendar govorimo modrost med temi, ki so popolni; vendar ne modrosti tega sveta niti princev tega sveta, ki se izjalovi; (aiōn )
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn )
temveč govorimo Božjo modrost v skrivnosti, celó prikrito modrost, ki jo je Bog pred svetom odredil v našo slavo; (aiōn )
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn )
ki je nobeden izmed princev tega sveta ni spoznal. Kajti če bi jo spoznali, ne bi križali Gospoda slave. (aiōn )
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn )
Naj se noben človek ne vara. Če se komurkoli med vami zdi, da je v tem svetu moder, naj postane bedak, da bo lahko moder. (aiōn )
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn )
Zatorej, če jed stori, da se moj brat pohujša, dokler stoji svet ne bom jedel mesa, da ne bi svojega brata primoral grešiti. (aiōn )
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn )
Torej vse te stvari so se jim zgodile za zglede. Napisane pa so v svarilo nam, nad katere so prišli konci sveta. (aiōn )
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs )
Oh smrt, kje je tvoje želo? Oh grob, kje je tvoja zmaga?‹ (Hadēs )
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn )
v katerih je bog tega sveta zaslepil misli tistih, ki ne verujejo, da jim ne bi zasijala svetloba veličastnega Kristusovega evangelija, ki je podoba Boga. (aiōn )
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios )
Kajti naša lahka stiska, ki je samo za trenutek, opravlja za nas veliko večjo, presegajočo in večno težo slave; (aiōnios )
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios )
medtem ko ne gledamo na stvari, ki so vidne, temveč na stvari, ki so nevidne. Kajti stvari, ki so vidne, so začasne, toda stvari, ki so nevidne, so večne. (aiōnios )
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios )
Kajti vemo, da če bi naša zemeljska hiša tega šotorskega svetišča razpadla, imamo v nebesih večno Božjo stavbo, hišo ne narejeno z rokami. (aiōnios )
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn )
(kakor je pisano: ›Razdelil je povsod, dal je revnim. Njegova pravičnost ostaja na veke.‹ (aiōn )
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn )
Bog in Oče našega Gospoda Jezusa Kristusa, ki je blagoslovljen na vékomaj, ve, da ne lažem. (aiōn )
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn )
ki je samega sebe dal za naše grehe, da nas lahko osvobodi iz tega sedanjega hudobnega sveta, glede na voljo Boga in našega Očeta, (aiōn )
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
ki mu bodi slava na veke vekov. Amen.‹ (aiōn )
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios )
Kajti kdor seje v svoje meso, bo od mesa požel trohljivost; toda kdor seje v Duha, bo od Duha požel večno življenje. (aiōnios )
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn )
daleč nad vsako kneževino in oblast in moč in gospostvo ter [nad] vsako ime, ki je poimenovano ne samo na tem svetu, temveč tudi na tem, ki prihaja. (aiōn )
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn )
v katerih ste v preteklem času živeli glede na način tega sveta, glede na princa oblasti zraka, duha, ki sedaj deluje v otrocih neposlušnosti; (aiōn )
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn )
da bi v prihajajočih časih lahko pokazal izjemna bogastva svoje milosti v svoji prijaznosti do nas po Kristusu Jezusu. (aiōn )
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn )
in storil, da vsi ljudje vidijo, kakšna je družba skrivnosti, ki je bila od začetka sveta skrita v Bogu, ki je po Jezusu Kristusu ustvaril vse stvari; (aiōn )
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn )
glede na večen namen, ki ga je nameraval v Kristusu Jezusu, našem Gospodu, (aiōn )
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
njemu bodi slava v cerkvi po Kristusu Jezusu skozi vsa obdobja, od veka do veka. Amen. (aiōn )
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn )
Kajti ne borimo se proti mesu in krvi, temveč proti kneževinam, proti oblastem, proti vladarjem teme tega sveta, proti duhovni zlobnosti na visokih položajih. (aiōn )
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Torej Bogu in našemu Očetu bodi slava na veke vekov. Amen. (aiōn )
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn )
celó skrivnost, ki je bila skrita pred veki in pred rodovi, toda sedaj je razodeta njegovim svetim, (aiōn )
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios )
ki bodo kaznovani z večnim uničenjem proč od Gospodove prisotnosti in proč od slave njegove moči; (aiōnios )
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios )
Torej sam naš Gospod Jezus Kristus in Bog, celó naš Oče, ki nas je ljubil in nam je po milosti dal večno tolažbo ter dobro upanje, (aiōnios )
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios )
Vendar sem zaradi tega razloga dosegel usmiljenje, da bi Jezus Kristus lahko vnaprej na meni pokazal vso potrpežljivost za vzor tem, ki naj bi odslej verovali vanj za večno življenje. (aiōnios )
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Torej Kralju, večnemu, nesmrtnemu, nevidnemu, edinemu modremu Bogu, bodi čast in slava na veke vekov. Amen. (aiōn )
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios )
Bojuj dober boj vere, oprimi se večnega življenja, kamor si tudi poklican in si pred mnogimi pričami izpovedal dobro izpoved. (aiōnios )
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios )
ki ima edini nesmrtnost in prebiva v svetlobi, ki sem mu noben človek ne more približati; katerega noben človek ni videl niti ne more videti; njemu bodi čast in večna oblast. Amen. (aiōnios )
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn )
Naročajte tem, ki so na tem svetu bogati, da naj ne bodo vzvišeni niti naj ne zaupajo v negotova bogastva, temveč v živega Boga, ki nam bogato daje v uživanje vse stvari; (aiōn )
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios )
ki nas je rešil in nas poklical s sveto poklicanostjo, ne glede na naša dela, temveč glede na svoj lastni namen in milost, ki nam je bila dana v Kristusu Jezusu pred začetkom sveta, (aiōnios )
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios )
Zato zaradi izvoljenih prenašam vse stvari, da bi lahko tudi oni dosegli rešitev duš, ki je v Kristusu Jezusu z večno slavo. (aiōnios )
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn )
kajti Demá me je zapustil, ker je vzljubil ta sedanji svet in je odpotoval v Tesaloníko; Kreskens v Galatijo, Tit v Dalmacijo. (aiōn )
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn )
In Gospod me bo osvobodil iz vsakega zlega dela in me ohranil za svoje nebeško kraljestvo. Njemu bodi slava na veke vekov. Amen. (aiōn )
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios )
v upanju večnega življenja, ki ga je Bog, ki ne more lagati, obljubil, preden je svet nastal; (aiōnios )
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn )
in nas uči, da naj bi v tem sedanjem svetu zanikali brezbožnost in posvetna poželenja, živeli trezno, pravično in bogaboječe (aiōn )
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios )
da naj bi, opravičeni po njegovi milosti, postali dediči glede na upanje večnega življenja. (aiōnios )
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios )
Kajti zato je mogoče za nekaj časa odpotoval, da bi ga sprejel za zmeraj; (aiōnios )
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn )
nam je v teh poslednjih dneh spregovoril po svojem Sinu, ki ga je določil [za] dediča vseh stvari, po katerem je tudi naredil svetove; (aiōn )
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn )
Toda sinu pravi: »Tvoj prestol, oh Bog, je na veke vekov; žezlo pravičnosti je žezlo tvojega kraljestva.« (aiōn )
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
Kakor pravi tudi na drugem mestu: »Ti si duhovnik na veke po Melkízedekovem redu.« (aiōn )
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios )
in ker je postal popoln, je postal avtor večne rešitve duš vsem tistim, ki ga ubogajo; (aiōnios )
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios )
nauka o krščevanjih in o polaganju rok in o vstajenju mrtvih ter o večni sodbi. (aiōnios )
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn )
in so okusili dobro Božjo besedo in moči sveta, ki pride, (aiōn )
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn )
kamor je za nas vstopil predhodnik, celó Jezus, postavljen [za] vélikega duhovnika na veke po Melkízedekovem redu. (aiōn )
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
Kajti on pričuje: »Ti si duhovnik na veke po Melkízedekovem redu.« (aiōn )
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn )
(kajti ti duhovniki so postali brez prisege; toda ta s prisego po tistem, ki mu je rekel: »Gospod je prisegel in se ne bo kesal: ›Ti si duhovnik na veke po Melkízedekovem redu‹«). (aiōn )
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn )
toda ta človek, ker ostaja večno, ima nespremenljivo duhovništvo. (aiōn )
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn )
Kajti postava dela ljudi [za] vélike duhovnike, ki imajo šibkost; toda beseda prisege, ki je bila, odkar [je] postava, postavlja Sina, ki je posvečen na vékomaj. (aiōn )
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios )
niti ne s krvjo koz in telet, temveč je s svojo lastno krvjo enkrat vstopil v sveti prostor in za nas dosegel večno odkupitev. (aiōnios )
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios )
koliko bolj bo Kristusova kri, ki je po večnem Duhu samega sebe brez madeža daroval Bogu, očistila vašo vest pred mrtvimi deli, da služite živemu Bogu? (aiōnios )
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios )
In zaradi tega razloga je on posrednik nove zaveze, da bi s pomočjo smrti, za odkupitev od prestopkov, ki so bili pod prvo zavezo, tisti, ki so poklicani, lahko prejeli obljubo večne dediščine. (aiōnios )
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn )
kajti potem bi moral od ustanovitve sveta pogosto trpeti. Toda sedaj se je prikazal enkrat ob koncu sveta, da z žrtvovanjem samega sebe odstrani greh. (aiōn )
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn )
Po veri razumemo, da so bili svetovi zasnovani po Božji besedi, tako da stvari, ki so vidne, niso bile narejene iz stvari, ki se kažejo. (aiōn )
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn )
Jezus Kristus, isti včeraj in danes in na veke. (aiōn )
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios )
Torej Bog miru, ki je od mrtvih ponovno privedel našega Gospoda Jezusa, ta véliki pastir ovc, naj vas po krvi večne zaveze, (aiōnios )
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn )
naredi popolne v vsakem dobrem delu, da izpolnite njegovo voljo, ki povzroča v vas to, kar je prijetno v njegovem pogledu, po Jezusu Kristusu, ki mu bodi slava na veke vekov. Amen. (aiōn )
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna )
In jezik je ogenj, svet krivičnosti. Tako je jezik med našimi udi, da omadežuje celotno telo in razvnema zakon narave; in ta je vžgan iz pekla. (Geenna )
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn )
ker ste ponovno rojeni, ne iz trohljivega semena, temveč iz netrohljivega, po Božji besedi, ki živi in ostaja na veke. (aiōn )
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn )
toda Gospodova beseda vztraja za vedno. In to je beseda, ki vam je oznanjena po evangeliju. (aiōn )
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
Če katerikoli človek govori, naj govori kakor Božje izreke; če katerikoli človek služi, naj to opravlja kakor iz zmožnosti, ki jo daje Bog; da bo v vseh stvareh Bog lahko proslavljen po Jezusu Kristusu, ki mu bodi hvala in gospostvo na veke vekov. Amen. (aiōn )
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios )
Toda Bog vse milosti, ki nas je poklical v svojo večno slavo po Kristusu Jezusu, potem ko ste nekaj časa trpeli, vas stori popolne, utrjene, okrepljene, vas ustali. (aiōnios )
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
Njemu bodi slava in gospostvo na veke vekov. Amen. (aiōn )
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios )
kajti tako vam bo razkošno odprt vstop v večno kraljestvo našega Gospoda in Odrešenika Jezusa Kristusa. (aiōnios )
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō )
Kajti če Bog ni prizanesel angelom, ki so grešili, temveč jih je vrgel navzdol v pekel in jih izročil verigam teme, da bodo pridržani do sodbe, (Tartaroō )
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Temveč rastite v milosti in v spoznanju našega Gospoda in Odrešenika Jezusa Kristusa. Njemu bodi slava tako sedaj in na veke. Amen. (aiōn )
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios )
(kajti življenje je bilo jasno pokazano in videli smo ga in pričujemo in vam kažemo to večno življenje, ki je bilo z Očetom in je bilo jasno pokazano nam), (aiōnios )
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn )
In svet mineva in njegovo poželenje; kdor pa izpolnjuje Božjo voljo, ostaja na veke. (aiōn )
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios )
In to je obljuba, ki nam jo je obljubil, celó večno življenje. (aiōnios )
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios )
Kdorkoli sovraži svojega brata, je morilec; in veste, da noben morilec nima večnega življenja, ki [bi] ostajalo v njem. (aiōnios )
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios )
In to je zapis, da nam je Bog dal večno življenje in to življenje je v njegovem Sinu. (aiōnios )
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Te besede sem napisal vam, ki verujete v ime Božjega Sina; da boste lahko vedeli, da imate večno življenje in da lahko verujete v ime Božjega Sina. (aiōnios )
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios )
In mi vemo, da je Božji Sin prišel ter nam dal razumevanje, da bi lahko spoznali tistega, ki je resničen in mi smo v njem, ki je resničen, celó v njegovem Sinu Jezusu Kristusu. Ta je resničen Bog in večno življenje. (aiōnios )
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn )
zaradi resnice, ki prebiva v nas in bo za vedno z nami. (aiōn )
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios )
In angele, ki niso obdržali svojega prvega stanja, temveč so zapustili svoje prebivališče, je ohranil v večnih verigah pod temo, do sodbe vélikega dne. (aïdios )
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios )
Celó kakor so Sódoma in Gomóra in na podoben način mesta okoli njiju, ki so same sebe predajala v prešuštvo in hodila za tujim mesom, postavljena kot zgled, trpeč maščevanje večnega ognja. (aiōnios )
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn )
besneči morski valovi, ki se penijo od svoje lastne sramote; blodeče zvezde, ki jim je za vedno prihranjena črna temà. (aiōn )
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios )
ohranite se v Božji ljubezni, pričakujte usmiljenje našega Gospoda Jezusa Kristusa, za večno življenje. (aiōnios )
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
edinemu modremu Bogu, našemu Odrešeniku, bodi slava in veličanstvo, gospostvo in oblast, tako sedaj kot na veke. Amen. (aiōn )
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn )
in nas naredil kralje in duhovnike Bogu ter svojemu Očetu; njemu bodi slava in gospostvo na veke vekov. Amen. (aiōn )
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn , Hadēs )
Jaz sem ta, ki živi in je bil mrtev; in glej, živ sem na vékomaj, Amen; in ključe imam od pekla in od smrti. (aiōn , Hadēs )
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn )
In ko so te živali dale slavo in čast in zahvalo njemu, ki je sedel na prestolu, ki živi na veke vekov, (aiōn )
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn )
je štiriindvajset starešin padlo dol pred njim, ki je sedel na prestolu in oboževalo njega, ki živi na veke vekov in svoje krone vrglo pred prestol, rekoč: (aiōn )
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn )
In vsako ustvarjeno bitje, ki je na nebu in na zemlji in pod zemljo in takšna, kot so v morju in vse, ki so v njem, sem slišal govoriti: »Blagoslov in čast in slava in oblast naj bo njemu, ki sedi na prestolu in Jagnjetu na veke vekov.« (aiōn )
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs )
In pogledal sem in zagledal konja mrtvaško blede barve; in tistemu, ki je sedel na konju, je bilo ime Smrt in Pekel je sledil za njim. In izročena jima je bila oblast nad četrtino zemlje, da ubijata z mečem in z lakoto in s smrtjo in z zemeljskimi živalmi. (Hadēs )
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn )
rekoč: »Amen: ›Blagoslov, slava, modrost, zahvaljevanje, čast, oblast in moč bodi našemu Bogu na veke vekov. Amen.‹« (aiōn )
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos )
In zatrobil je peti angel in videl sem zvezdo pasti z neba na zemljo in dan mu je bil ključ od jame brez dna. (Abyssos )
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos )
In odprl je jamo brez dna in iz jame se je dvignil dim kakor dim velike talilne peči; in zaradi dima iz jame sta potemnela sonce in zrak. (Abyssos )
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos )
In nad seboj so imele kralja, ki je angel iz jame brez dna, katerega ime je v hebrejskem jeziku Ábadon, toda v grškem jeziku ima svoje ime Apolíon. (Abyssos )
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn )
in prisegel pri njem, ki živi na veke vekov, ki je ustvaril nebo in stvari, ki so na njem in zemljo in stvari, ki so na njej in morje in stvari, ki so v njem, da naj ne bi bilo več časa, (aiōn )
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos )
In ko bosta končala svoje pričevanje, se bo iz jame brez dna povzpel zvernik, ki bo povzročil vojno proti njima in ju premagal ter ju ubil. (Abyssos )
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn )
In zatrobil je sedmi angel in na nebu so bili močni glasovi, govoreč: »Kraljestva tega sveta so postala kraljestva našega Gospoda in njegovega Kristusa in vladal bo na veke vekov.« (aiōn )
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios )
In videl sem drugega angela leteti po sredi neba, ki je imel večen evangelij, da ga oznani tem, ki prebivajo na zemlji in vsakemu narodu, sorodstvu, jeziku in ljudem, (aiōnios )
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn )
in dim njihovega mučenja se vzpenja na veke vekov in ne podnevi ne ponoči nima počitka, kdor obožuje zvernika ter njegovo podobo in kdorkoli sprejme znamenje njegovega imena. (aiōn )
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn )
In ena izmed štirih živali je dala sedmim angelom sedem zlatih stekleničk, polnih besa Boga, ki živi na veke vekov. (aiōn )
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos )
Zvernik, ki si ga videl, je bil in ga ni in vzpel se bo iz jame brez dna in šel v pogubo in tisti, ki prebivajo na zemlji, katerih imena od ustanovitve sveta niso bila zapisana v knjigi življenja, se bodo čudili, ko bodo gledali zvernika, ki je bil in ga ni, pa vendar je. (Abyssos )
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn )
In ponovno so rekli: »Aleluja. In njen dim se je vzdigoval na veke vekov.« (aiōn )
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr )
In zvernik je bil ujet in z njim lažni prerok, ki je delal čudeže pred njim, s katerimi je zavajal te, ki so sprejeli znamenje zvernika in te, ki so oboževali njegovo podobo. Oba sta bila živa vržena v ognjeno jezero, goreče z žveplom. (Limnē Pyr )
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos )
In videl sem angela priti dol z neba, ki je imel v svoji roki ključ od jame brez dna ter veliko verigo. (Abyssos )
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos )
in ga vrgel v jamo brez dna in ga zaprl ter zapečatil nad njim, da naj ne bi več zavajal narodov, dokler se ne bi dopolnilo tisoč let, potem pa mora biti malo časa odvezan. (Abyssos )
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn , Limnē Pyr )
Hudič, ki jih je zavedel, pa je bil vržen v ognjeno in žvepleno jezero, kjer sta zvernik in lažni prerok in mučeni bodo dan in noč, na veke vekov. (aiōn , Limnē Pyr )
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs )
In morje se je odreklo mrtvim, ki so bili v njem; in smrt in pekel sta izročila mrtve, ki so bili v njiju in bili so sojeni, vsak glede na svoja dela. (Hadēs )
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs , Limnē Pyr )
In smrt in pekel sta bila vržena v ognjeno jezero. To je druga smrt. (Hadēs , Limnē Pyr )
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr )
In kdorkoli ni bil najden zapisan v knjigi življenja, je bil vržen v ognjeno jezero. (Limnē Pyr )
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr )
Toda strahopetci, neverniki, gnusneži, morilci, vlačugarji, čarodeji, malikovalci in vsi lažnivci bodo imeli svoj delež v jezeru, ki gori z ognjem in žveplom, kar je druga smrt.« (Limnē Pyr )
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn )
In tam ne bo noči in ne potrebujejo nobene sveče niti sončne svetlobe, kajti Gospod Bog jim daje svetlobo in kraljevali bodo na veke vekov. (aiōn )