< Yohane 1 >

1 Pachiyambi panali Mawu, ndipo Mawu anali kwa Mulungu, ndipo Mawu ndiye Mulungu.
Ung'wandyo ai lukoli lukani, nu lukani ai latulaa palung'wi ni Itunda, nu lukani ai latulaa Itunda.
2 Mawuwa anali ndi Mulungu pachiyambi.
Uyu, u lukani, Ung'wandyo ai watulaa palung'wi ni Itunda.
3 Zinthu zonse zinalengedwa ndi Iye; ndipo popanda Iye sikukanakhala kanthu kalikonse kolengedwa.
I intu yihi ai itumilwe ku ng'wenso, ni anga ihite kutula ng'wenso kutili ga ni kintu king'wi nai katulaa kitumilwe.
4 Mwa Iye munali moyo, ndipo moyowo unali kuwunika kwa anthu.
Mukati akwe ai ukoli u upanga, nu uwo upanga ai watulaa welu nu a ana adamu ihi.
5 Kuwunika kunawala mu mdima, koma mdimawo sunakuzindikire.
Welu welyaa mu kiti, ang'wi i kiti shanga ukaulimisa.
6 Kunabwera munthu amene anatumizidwa kuchokera kwa Mulungu; Iyeyo dzina lake linali Yohane.
Ai ukoli u muntu nai ulagiigwe kupuma kung'wa Itunda, niiza ilina ni lakwe ai watulaa Yohana.
7 Iye anabwera ngati mboni kudzachitira umboni kuwunikako kuti kudzera mwa iye anthu onse akhulupirire.
Ai wazile anga mukuiili kukiila kutula uwo u welu, iti kina ihi ahume kuhuiila kukiila ng'wenso.
8 Iyeyu sanali kuwunika; koma anabwera ngati mboni ya kuwunika.
U Yohona shanga ai uwo u welu, ila ai uzile iti wakuiile kutula uwo u welu.
9 Kuwunika koona kumene kuwunikira munthu aliyense kunabwera ku dziko lapansi.
Iyo ai ayulaa welu nua tai naza utuile uzile mu ihi ni nyenso wimuikila welu kila u ng'wi.
10 Iye anali mʼdziko lapansi, ndipo ngakhale kuti dziko lapansi linalengedwa ndi Iye, dziko lapansilo silinamuzindikire Iye.
Ai watulaa mihi, ni ihi ai iumbilwe kukiila ng'wenso, ni ihi shanga ai limumanyile.
11 Iye anabwera kwa iwo amene anali akeake, koma akewo sanamulandire Iye.
Ai uzile ku intu ni akwe, ni antu ni akwe shanga ikamusingiilya.
12 Koma kwa onse amene anamulandira Iye, kwa amene anakhulupirira mʼdzina lake, Iye anawapatsa mphamvu yokhala ana a Mulungu;
Ila ku awo ni idu nai amusingiiye, naza alihuiie i lina ni lakwe, ku awo ai uikiiye tai ane ni akutula ana ang'wi Itunda.
13 ana wobadwa osati monga mwachilengedwe, kapena chisankho cha munthu, kapena chifuniro cha mwamuna koma wobadwa mwa Mulungu.
Naza aleilwe shanga ku sakami, ang'wi ku ulowa nua muili, ang'wi ku ulowa nua muntu, ila kung'wi Itunda mukola.
14 Mawu anasandulika thupi ndipo anakhala pakati pathu. Ife tinaona ulemerero wake, ulemerero wa Iye amene ndi Mwana mmodzi yekhayo wa Atate, wodzaza ndi chisomo ndi choonadi.
Nu ng'wenso u lukani ai wizipiilye muili hangi akikie mukati itu, ka wihengilee ikulyo ni lakwe, ikulyo anga ni la muntu nu ing'wene nua kinyena nai uzile kupuma kung'wa Tata, wizue ukende nua tai.
15 Yohane achitira umboni za Iye. Iye akufuwula kuti, “Uyu ndi Iye amene ndinati, ‘Iye amene akubwera pambuyo panga ndi wondiposa ine chifukwa, Iyeyo analipo ine ndisanabadwe.’”
U Yohana ai ukuiie kutula ung'wenso, nu kitunta ku luli azeligitya, “Uyu yuyoo niza niligitya i nkani niakwe nizeligitya, “Uyo nuzile ze yakilaa unene inge Mukulu kukila unene, kunsoko iiza ukoli ze ikili unene”.
16 Kuchokera mʼkuchuluka kwa chisomo chake ife tonse talandira madalitso pamwamba pa madalitso.
Kunsoko kupuma mu ukondaniili nu akwe, usese kihi kusingiiye nankanda u uhumi ze yakilaa nia uhumi.
17 Pakuti lamulo linapatsidwa kudzera mwa Mose; chisomo ndi choonadi zinabwera kudzera mwa Yesu Khristu.
Kunsoko ilagiilyo ai liletilwe kukiila Musa, u ukende ni tai ai izile kukiila Yesu Kristo.
18 Palibe munthu amene anaona Mulungu, koma Mwana mmodzi yekhayo amene ali wa pamtima pa Atate, ndiye anafotokoza za Iye.
Kutili u ng'wana adamu nai umihengile Itunda matungo ihi, muntu wing'wene niiza inge Itunda, nuili mu kikua kang'wa Tata, umizipilye ung'wenso wamanyike.
19 Tsopano uwu ndi umboni wa Yohane pamene Ayuda a ku Yerusalemu anatumiza ansembe ndi Alevi kudzamufunsa kuti iye anali yani.
Nu uwu wuwu ukuiili nuang'wa Yohana matungo i Akuhani ni Alawi nai alagiigwe kitalakwe ni Ayahudi kumukolya “uewe inge nyenyu?”.
20 Iye sanalephere kuvomereza, koma iye anavomereza momasuka kuti, “Ine sindine Khristu.”
Bila kisinsila hangi shanga ai uhitile, ila ai usukiiye, “Unene shanga Kristo”.
21 Iwo anamufunsa kuti, “Nanga iwe ndiwe yani? Kodi ndiwe Eliya?” Iye anati, “Sindine.” “Kodi ndiwe Mneneri?” Iye anayankha kuti, “Ayi.”
Uu gwa akamokolya, “ku lulo uewe inge nyenyu itungili?” Uewe inge Eliya? Akaligitya, “Unene shanga” Akaligitya, uewe inge munyakidagu? Akasukiila “A aa”.
22 Pomaliza iwo anati, “Ndiwe yani? Tipatse yankho kuti tipite nalo kwa amene anatituma. Kodi iwe ukuti chiyani za iwe mwini?”
Uu gwa akamuila, “uewe inge nyenyu iti kina kuinkiilye isusho naza akulaagiye? Ukikuiila uli uewe mukola?”
23 Yohane anayankha ndi mawu a mneneri Yesaya kuti, “Ine ndi mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Wongolani njira ya Ambuye.’”
Akaligitya, “Unene inge luli nu lakwe nui lilaa muwii, “Migooli i nzila a mukulu! anga munyakidagu Isaya nai uligitilye.”
24 Tsopano Afarisi ena amene anatumidwa
Uu gwa ai akoli ni antu alagiigwe kupuma pang'wanso kupuma ku Afalisayo. Akamukolya nu kuligitya,
25 anamufunsa Iye kuti, “Kodi ndi chifukwa chiyani, umabatiza ngati iwe si Khristu, kapena Eliya, kapena Mneneri?”
: ku niki ukoja gwa angize uewe shanga wi Kilisto ang'wi Eliya ang'wi munyakidagu?
26 Yohane anayankha kuti, “Ine ndimabatiza ndi madzi, koma pakati panu payima amene simukumudziwa.
uYohana ai uasukiiye azeligitya: Nukoja ku mazi, Ga ni iti, mukati anyu wimikile muntu ni shanga mumulingile.
27 Iye ndi amene akubwera pambuyo panga, ine siwoyenera kumasula zingwe za nsapato zake.”
Uyu yuyo nupembilye ze yakilaa unene, Unene ni mugila uhumi nuakutolya i mikoha a ilatu niakwe,
28 Zonsezi zinachitika ku Betaniya kutsidya lina la mtsinje wa Yorodani, kumene Yohane ankabatizira.
Makani aya ai atulikile uko ku Bethania, itumbi nila Yordani, kianza naiza uYohani ukoli ukoja.
29 Pa tsiku lotsatira Yohane anaona Yesu akubwera kwa iye ndipo anati, “Taonani, Mwana Wankhosa wa Mulungu, amene achotsa tchimo la dziko lapansi!
Luhiku nai lutyatile uYohana akamihenga uYesu upembilye kung'waakwe akaligitya, Goza ung'waa nkolo wang'wa Itunda nuiuhola umulandu nua unkumbigulu!
30 Uyu ndi amene ndimatanthauza pamene ndinanena kuti, ‘Munthu amene akubwera pambuyo panga ndi wondiposa ine chifukwa analipo ine ndisanabadwe.’
uyu yuyo naindigitilye inkani niakwe nizeligitya, Nuanso nupembilye kituli kane inge mukulu kukila unene, kunsoko ai watuile zeikili unene,
31 Ine mwini sindinamudziwe Iye, koma ndinabwera kubatiza ndi madzi kuti Iye adziwike mu Israeli.”
Shanga ai numulingile ung'wenso, kuiti aiitulikile nanso kina akunukulwe mukati a Israeli, kina ainzile nikazeoja ku mazi,
32 Kenaka Yohane anapereka umboni uwu: “Ine ndinaona Mzimu Woyera ngati nkhunda kuchokera kumwamba nakhala pa Iye.
uYohana ai ukuiie, “Ai nihengile uNg'wau Ng'welu ukusima kupuma kilunde mpyani a nkuni nu kusiga migulya akwe.
33 Ine sindikanamudziwa Iye, koma kuti amene anandituma ine kudzabatiza ndi madzi anati kwa ine, ‘Munthu amene udzaona Mzimu Woyera akutsika nakhazikika pa Iye ndi amene adzabatize ndi Mzimu Woyera.’
Unene shanga ai numulingile, kuiti nuanso nai undagiiye iti noje ku mazi ai untambuie, “uyo nize ukihenga Ug'wau Ng'welu ukusima nu kikie migilya akwe, Nuanso yuyo nuojaa ku Ng'wau Ng'walu,
34 Ine ndaona ndipo ndikuchitira umboni kuti uyu ndi Mwana wa Mulungu.”
Nihengaa nu kukuiila kina uyu ige ng'wana wang'wa Itunda,”
35 Pa tsiku lotsatira Yohane analinso pamenepo pamodzi ndi awiri a ophunzira ake.
Hangi luhiku nai lutyatile uYohana aiukoli wimikile nia manyisigwa akwe abiili,
36 Iye ataona Yesu akudutsa anati, “Taonani Mwana Wankhosa wa Mulungu!”
ai amihengile uYesu ukugenda nu Yohana akaligitya, “Goza, uNng'waa nkolo nuang'wa Itunda”
37 Ophunzira ake awiriwo atamva iye akunena izi, iwo anamutsatira Yesu.
Amanyisigwa abiili ai amigulye uYohana ukuligitya aya akamutyata uYesu.
38 Atatembenuka, Yesu anaona iwo akumutsatira ndipo anawafunsa kuti, “Kodi mukufuna chiyani?” Iwo anati, “Rabi (kutanthauza kuti Aphunzitsi), kodi mukukhala kuti?”
Hangi uYesu ai upilukile nu kuihenga iamanyisigwa awo amutyatile, nu kuaila, “Muloilwe ntuni?” Akamusukiilya, Rabbi, ( ndogoelyo akwe ng'walimu; ) wikiee pii?”
39 Iye anayankha kuti, “Bwerani mudzaone.” Choncho iwo anapita ndi kukaona kumene Iye amakhala, ndipo anakhala naye tsiku limenelo. Linali ngati pafupifupi ora la khumi.
Aka atambuila, “pembyi nu kihenga. “Uugwa ai alongoe nu kihenga i kianza nai wikiee; akikie palung'wi nu ng'wenso u luhiku nulanso, kunsoko aiyatulaa yapikiila saa ikumi iti.
40 Andreya mʼbale wake wa Simoni Petro, anali mmodzi wa awiriwo amene anamva zimene Yohane ananena ndiponso amene anamutsata Yesu.
Ung'wi nua awo ni abiili nai amigulye uYohana ukutambula ni uugwa kumutyata uYesu ai utuile inge Andrea, muluna akwe uSimoni Petro.
41 Choncho chimene Andreya anachita ndi kukapeza mʼbale wake Simoni ndipo anamuwuza kuti, “Ife tamupeza Mesiya,” (kutanthauza kuti Khristu).
Akamihenga muluna akwe uSimioni nu kumutambuila,”Kamulijaa uMasihi” (niiza impyanigwe Kristo).
42 Kenaka iye anabweretsa Simoni kwa Yesu, amene anamuyangʼana ndipo anati, “Iwe ndiwe Simoni, mwana wa Yohane. Udzatchedwa Kefa” (limene litanthauza kuti Petro).
Akamuleta kung'wa Yesu. uYesu akamugoza nu kuligitya, Uewe wi Simioni ng'wana wang'wa Yohana” wikitangwa Kefa” ( ndogoelyo akwe 'Ptro')
43 Pa tsiku lotsatira Yesu anaganiza zopita ku Galileya. Atamupeza Filipo, anati kwa iye, “Nditsate.”
Luhiku nai lutyatile itungo uYesu nai wahia kuhega kulongola kuGalilaya, ai umuligilye uFilipo nu kumuila, “Ntyate unene.”
44 Filipo monga Andreya ndi Petro, anali wochokera ku mzinda mudzi Betisaida.
uFilipo aiwatulaa mukola ihi nua kuBethasaida, kisali kang'wa Adrea nu Petro.
45 Filipo anakapeza Natanieli ndipo anamuwuza kuti, “Ife tapeza amene Mose analemba za Iye mʼmalamulo, ndi zimene aneneri analembanso za Iye, Yesu wa ku Nazareti, mwana wa Yosefe.”
uFilipo ai umuligilye uNathanaeli nu kumuila, Kamulijaa uyo naiza uMusa ukilisilye inkani niakwe mu malagiilyo nu Unyakidagu, Yesu ng'wana awng'wa Yusufu, kupuma kuNazareti.
46 Natanieli anafunsa kuti, “Nazareti! Kodi kanthu kalikonse kabwino kangachokere kumeneko?” Filipo anati, “Bwera udzaone.”
uNathanaeli akamuila, ''Itii kintu ni kiziza kihumile kupembelya kuNazareti?” uFilipo akamuila, “Nzuu nu kihenga.”
47 Yesu atamuona Natanieli akuyandikira, anati kwa iye, “Uyu ndi Mwisraeli weniweni, mwa iye mulibe chinyengo.”
uYesu akaamihenga uNathanaeli upembilye kung'waakwe nu kuligitya, “Goza uMuisraeli tai taai ni mugila u ukongelwa mukati akwe”
48 Natanieli anafunsa kuti, “Kodi mwandidziwa bwanji?” Yesu anayankha kuti, “Ine ndinakuona iwe utakhala pansi pamtengo wamkuyu Filipo asanakuyitane.”
uNathanaeli akamuila, “Uningile kinyauli unene?” uYesu akamusukiilya nu kumuila, Aza ikili uFilipo kuitanga naza ukoli pihi pi ikota, aza nakihengaa.”
49 Kenaka Natanieli ananena kuti, “Rabi, Inu ndinu Mwana wa Mulungu; Inu ndinu Mfumu ya Israeli.”
uNahanaeli akasukiilya, “Rabi uewe wi Ng'wana wang'wa Itunda Uewe wi Mutemi nua Israeli”
50 Yesu anati, “Ukukhulupirira chifukwa chakuti ndakuwuza kuti Ine ndinakuona iwe uli pansi pamtengo wamkuyu? Iwe udzaona zinthu zazikulu kuposa izo.”
uYesu akasukiilya akamuila, Kunsoko nukuiie aza 'nukihengile pihi i kota' itii wahuiila? ukihenga ntendo nkulu kukila izi.”
51 Ndipo Iye anapitirira kuti, “Zoonadi, Ine ndikuwuza kuti iwe udzaona kumwamba, kutatsekuka ndi angelo a Mulungu akukwera ndi kutsika pa Mwana wa Munthu.”
uYesu akaligitya, “Huiili huiili kumuili mikihenga ilunde likuluguka, nu kuihenga iamalaika akunankila nu kusima migulya a Ng'wana wang'wa Adamu.”

< Yohane 1 >