< Yohane 2 >

1 Pa tsiku lachitatu munali ukwati mu Kana wa ku Galileya. Amayi ake a Yesu anali komweko,
Ze yakilaa mahiku a taatu, ai ukoli winga uko ku Kana a Galilaya nu Nyinya wang'wa Yesu ai ukoli kuko.
2 ndipo Yesu ndi ophunzira ake anayitanidwanso ku ukwatiwo.
uYesu ni amanyisigwa akwe ai atulaa anilwe mu winga.
3 Vinyo atatha, amayi a Yesu anati kwa Iye, “Wawathera vinyo.”
Itungo nai auilwa i magai, u nyinya wakwe uYesu akamuila, “Agila i magai.”
4 Yesu anayankha kuti, “Amayi, chifukwa chiyani mukundiwuza Ine? Nthawi yanga sinakwane.”
uYesu akasukiilya, Musungu ni kanso kintuile ntuni unene? Itungo ni lane likili kupikiila,”
5 Amayi ake anati kwa antchito, “Inu muchite chilichonse chimene akuwuzeni.”
uNyinya nuakwe akaaila, “Kihi nuikamuila itumi.”
6 Pamenepo panali mitsuko yamiyala yothiramo madzi isanu ndi umodzi, imene Ayuda amagwiritsa ntchito pa mwambo wodziyeretsa. Uliwonse unali ndi malita 100 kapena kupitirirapo.
U ugwa ai ikoli ni ntunda mutandatu ni a magwe pang'wanso nai iekilwe kunsoko a ku kalala mu mahiku a Ayahudi, kila ing'wi ai ikete wizulyo nua nzio ibiili, itaatu.
7 Yesu anati kwa antchitowo, “Dzazani madzi mʼmitsukoyi,” ndipo iwo anadzaza ndendende.
uYesu aka aila, Izulyi imazi intunda nia magwe, “akizulya ga nu migulya.
8 Ndipo Iye anatinso kwa iwo, “Tsopano tungani ndipo kaperekeni kwa mkulu waphwando.” Iwo anachita momwemo.
Uugwa aka aila awo ianya mulimo, “Holi ngele itungili nu kutwala ku mua aiilya nu mukulu nua meza. “'Akituma anga naza ualagiiye.
9 Mkulu waphwando analawa madziwo amene anasandulika vinyo, ndipo sanazindikire kumene vinyoyo anachokera, ngakhale kuti antchito amene anatunga madziwo amadziwa. Kenaka anayitanira mkwati pambali
Muaiilya nu mukulu ai umaluilye imazi ayo nai atulaa akailikaa nu kutula magai, ila shanga aiulingile kapumile (kuiti ianyamulimo naza atepile imazi ai alingile kai apumile). Uugwa akamitanga umukulu nua winga nu
10 ndipo anati, “Aliyense amatulutsa vinyo wokoma kwambiri poyambirira ndipo kenaka vinyo wosakoma pamene oyitanidwa atamwa kale wambiri; koma iwe wasunga wokoma mpaka tsopano.”
kumuila, kila ung'wi wandya kuagiza i antu imagai ni maziza ni anga agale wiagiza imagai ni shanga maziza. Kuiti uewe umaikile imagai ni maziza kupikiila itungili”
11 Ichi chinali chizindikiro chodabwitsa choyamba chimene Yesu anachita ku Kana wa ku Galileya. Potero Iye anawulula ulemerero wake, ndipo ophunzira ake anamukhulupirira Iye.
U ukuilwa uwo nua ku Kana a kuGalilaya, ai watulaa wuwo ng'wandyo nua mpyani nia ukuilwa nuang'wa Yesu, azekunukula ikulyo nilakwe, itigwa ia manyisigwa akwe akamuhuiila.
12 Zitatha izi Iye anatsikira ku Kaperenawo pamodzi ndi amayi ake, abale ake ndi ophunzira ake. Iwo anakhala kumeneko masiku owerengeka.
Ze yakilaa izi, uYesu, Nyinya nua kwe, aluna akwe ni amanyisigwa akwe ai alongoe mu kisali nika Kapernaumu nu kikie kuko ku mahiku masheenyu.
13 Nthawi ya Paska ya Ayuda itayandikira, Yesu anapita ku Yerusalemu.
Uugwa ipasaka a Ayahudi ai ahumbeela, itigwa uYesu akalongola ku Yerusalemu.
14 Mʼbwalo la Nyumba ya Mulungu Iye anapeza anthu akugulitsa ngʼombe, nkhosa ndi nkhunda ndipo ena akusintha ndalama pa matebulo.
Aka ahanga ia gulya a ng'ombe, nkolo, ni nkunda mukati Itekeelo. Ga nia kaila mpia ai akoli ikie mukati Itekeelo.
15 Chifukwa cha zimenezi Iye anapanga chikwapu cha zingwe ndipo anatulutsa onse mʼbwalo la Nyumbayo, pamodzi ndi nkhosa ndi ngʼombe; Iye anamwaza ndalama zawo ndi kugudubuza matebulo.
Uyesu akanonia umikoha ukete makundo, aka apumya ihi nai amoli mukati Itekeelo, ize ihanguie ng'ombe ni nkolo. Akahunula impia ni ya akaila mpia nu kuipiula i meza niao.
16 Kwa amene amagulitsa nkhunda, Iye anati, “Tulutsani izi muno! Osasandutsa Nyumba ya Atate anga msika!”
Ku agulya kunda aka aila, “Pumyi i intu izi kuli ni kianza iki, leki kulitendi ito ni lang'wa Tata nu ane kutula kianza ki soko”
17 Ophunzira ake anakumbukira kuti zinalembedwa kuti, “Kudzipereka kwanga ku nyumba yanu kudzandiphetsa.”
Amanyisigwa akwe akakimbukiilya kina ai yatulaa ikilisigwe, “Wilu nu ito ni lako likundya.”
18 Kenaka Ayuda anamufunsa Yesu kuti, “Kodi mungationetse chizindikiro chodabwitsa chotani chotsimikizira ulamuliro wanu wochitira izi?”
Akulu ni a Ayahudi akasukiilya, akamuila, Inge kilingasiilyo kii nu kulagiila kunsoko ukituma imakani aya?”
19 Yesu anawayankha kuti, “Gwetsani Nyumba ya Mulunguyi ndipo Ine ndidzayimanganso mʼmasiku atatu.”
uYesu aka asukiilya, Ligumuli Itekeelo ili nu nene kulizenga ze yakilaa mahiku ataatu.”
20 Ayuda anayankha kuti, “Zinatenga zaka makumi anayi kumanga Nyumbayi, kodi Inu mungayimange masiku atatu?”
Uugwa Akulu a Ayahudi akaligitya, “Ai ikuhoile miaka makumi anne na mutaandatu kulizenga Itekeelo ili nu ewe ukuligitya ukulizenga ku mahiku ataatu?”
21 Koma Nyumba ya Mulungu imene amanena linali thupi lake.
Ga ni iti, nuanso ai utambue itekeelo aze usigiie muili nuakwe.
22 Iye ataukitsidwa kwa akufa, ophunzira ake anakumbukira zimene Iye ananena ndipo anakhulupirira Malemba ndi mawu amene Yesu anayankhula.
Iti gwa panyambele ze yakilaa kiuka kung'waakwe kupuma kuashi, ia manyisigwa ni akwe akakimbukiilya kina ai uligitilye nianso, akahuiila uukilisigwa ni ntambu naiza uYesu wakondilyee kumiligitya.
23 Tsopano Iye ali mu Yerusalemu pa phwando la Paska, anthu ambiri anaona zizindikiro zodabwitsa zimene amachita ndipo anakhulupirira dzina lake.
Uugwa nai watulaa ku Yerusalemu matungo a pasaka, itungo nila sikukuu antu idu ai ahuiie i lina ni lakwe. nai ihengile i ilingasiilyo ni a ukuilwa nai witumile.
24 Koma Yesu sanawakhulupirire iwo, pakuti amadziwa anthu onse.
Kuiti uYesu ai mugila u uhuiili ni enso ku nsoko ai ualingile i ana adamu i hi.
25 Iye sanafune umboni wa wina aliyense popeza amadziwa zomwe zinali mʼmitima mwa anthu.
Shanga ai utakile muntu wihi kumuila kutula ni ili i ana adamu kunsoko ai ulingile nai kimoli mukati ao.

< Yohane 2 >