< Yobu 35 >

1 Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,
Hahoi Elihu ni a pathung e teh,
2 “Kodi mukuganiza kuti mukukhoza? Mukunena kuti, ‘Ndine wolungama pamaso pa Mulungu.’
Heteheh, a lan telah na pouk maw, Cathut lannae hlak ka lan telah na dei maw.
3 Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani, ndipo ndimapeza chiyani ndikapanda kuchimwa?’
Bangkongtetpawiteh, ka yonnae hah pap boipawiteh, hot teh, nang hanelah bangmaw a hawinae, meknae hoe ka hmu telah na ti.
4 “Ine ndikufuna ndikuyankheni inu pamodzi ndi abwenzi anu omwe.
Nama koe kaawm e naw hoi na pathung han.
5 Yangʼanani kumwamba ndipo muone mitambo imene ili kutali ndi inuyo.
Kalvan lah moung nateh khenhaw! khenhaw! nang hlak hoe ka rasang e tâmainaw hah,
6 Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani? Ngati machimo anu ndi ochuluka, zimenezo zimachita chiyani kwa Iye?
Yonnae na sak pawiteh, ama taranlahoi bangmaw hoe na kuepcing sak, nahoeh pawiteh kâtapoenae hah pap pawiteh, ama hanelah bangmaw na sak,
7 Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani? Kapena Iye amalandira chiyani chochokera mʼdzanja lanu?
Tamikalan lah na awm pawiteh, ama hah bangmaw na poe, Nahoeh pawiteh, ama ni na kut dawk hoi bangmaw a hmu.
8 Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo, ndipo chilungamo chanu chimakhudza anthu anzanu.
Na hawihoehnae ni nang patetlah kaawm e tami hah a ratet, na lannae ni tami capa buet touh a ratet.
9 “Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa; akufuna chithandizo kuti achoke pansi pa ulamuliro wa anthu amphamvu.
Hnephnap e a pap kecu dawkvah a hramki awh, athakaawme taminaw e rektapnae kecu dawkvah, kabawpnae a panki hoi a hram awh.
10 Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga, amene amatisangalatsa nthawi ya usiku,
Hateiteh, apinihai nâmaw kasakkung Cathut, karum lah la sak han ka poe e hah ao telah dei awh hoeh.
11 amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi ndipo amatipatsa nzeru kupambana mbalame zowuluka?’
Talai e sarang hlak hai apinimaw na cangkhai awh. Kalvan e tava hlak lung na ang sak awh.
12 Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye chifukwa cha kudzikuza kwa anthu oyipa.
Tamikathoutnaw a kâoup kecu dawk, hawvah a hram awh ei, pathung awh hoeh.
13 Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake; Wamphamvuzonse sasamalira zimenezi.
Banghai bang hoeh e lawk hah Cathut ni khoeroe thai mahoeh, Athakasaipounge, ni hai banglahai noutna mahoeh.
14 Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti Iye saona zimene zikuchitika. Iye adzaweruza molungama ngati inu mutamudikira
Ama teh na hmawt hoeh telah na dei nakunghai, amae hmalah lannae ao teh, ama teh na ring raw na ring han.
15 ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango, zoyipa zambiri zimene anthu amachita,
Bangkongtetpawiteh, atuvah a lungkhueknae dawk hoi na rek hoeh niteh, pathunae hnonaw pueng hah pâkuem hoeh.
16 abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake, mukungochulukitsa mawu opanda nzeru.”
Hatdawkvah, Job ni a khuekhaw awm laipalah, a pahni a ang teh, panuenae laipalah lawk a pap sak.

< Yobu 35 >