< Masalimo 1 >

1 Wodala munthu amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa, kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa, kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
Kasakkung: Panuekhoeh Tamikathoutnaw e khokhangnae koe ka cet hoeh e tami, tamikayonnaw e lamthung dawk kangdout hoeh e tami, kadudamnaw e kamkhuengnae koe hai ka tahung hoeh e tami,
2 Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
BAWIPA e lawk ka ngâi niteh, a kâlawknaw hah karum khodai luepluep ka pouk e tami teh a yawhawi.
3 Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi, umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake ndipo masamba ake safota. Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
Ahni teh tui teng vah ung e, a tue a pha torei ka paw niteh, a hna hai kamyai hoeh e thingkung hoi a kâvan. A tawksak e naw dawk hawinae a hmu han.
4 Sizitero ndi anthu oyipa! Iwo ali ngati mungu umene umawuluzidwa ndi mphepo.
Tamikathoutnaw teh, hottelah laipalah, kahlî ni a palek e cahik hoi a kâvan awh.
5 Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo, kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
Hatdawkvah, tamikathoutnaw teh, lawkcengnae hnin navah kangdout thai awh mahoeh. Tamikayonnaw hai tami kalannaw e kamkhuengnae dawk bawk thai mahoeh.
6 Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama, koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.
Bangkongtetpawiteh, BAWIPA ni tami kalannaw e lamthung teh a panue. Tamikathoutnaw e lamthung teh rawknae koe a pha han.

< Masalimo 1 >