< Yobu 11 >

1 Pamenepo Zofari wa ku Naama anayankha kuti,
A LAILA olelo aku la o Zopara ka Naamata, i aku la,
2 “Kodi mawu ambirimbiriwa nʼkukhala osayankhidwa? Kodi munthu woyankhulayankhulayu nʼkulungamitsidwa?
Aole anei e pono ke pane aku i na huaolelo he nui la? E hoaponoia anei ke kanaka lehelehe wale?
3 Kodi anthu nʼkukhala chete atamva kubwebweta kwakoku? Kodi palibe wina amene adzakudzudzule pamene ukuyankhula zonyoza?
E paa anei ka waha o kanaka i kou kaena wale ana? A hoomaewaewa mai oe, aole anei he mea nana oe e hoohilahila aku?
4 Iwe ukunena kwa Mulungu kuti, ‘Zikhulupiriro zanga ndi zopanda zolakwika ndipo ndine wangwiro pamaso panu.’
A ua olelo mai oe, he maemae kuu olelo, A ua hala ole au i kou mau maka.
5 Aa, nʼkanakonda Mulungu akanayankhula kuti Iye atsekule pakamwa pake kutsutsana nawe
Ina paha e olelo mai ke Akua, A e wehe ae i kona lehelehe ia oe;
6 ndi kukuwululira chinsinsi cha nzeru yake, pakuti nzeru yeniyeni ili ndi mbali ziwiri. Dziwa izi: Mulungu wayiwala machimo ako ena.
A e hoike mai oia ia oe i na mea huna o ka naauao, Ua papalua ka maiau! Alaila e ike auanei oe, E hoopoina mai no ke Akua i na hewa ou.
7 “Kodi iwe ungathe kumvetsa zinsinsi za Mulungu? Kodi ungafufuze malire a nzeru za Wamphamvuzonse?
E loaa anei ia oe ka ke Akua mau mea hohonu? E loaa pololei loa anei ia oe ka Mea mana?
8 Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol h7585)
Ua kiekie ia e like me ka lani; heaha kau e hana ai? Ua oi kona hohonu i ko ka po; heaha kau e ike ai? (Sheol h7585)
9 Muyeso wa nzeru zake ndi wautali kupambana dziko lapansi ndipo ndi wopingasa kupambana nyanja.
Ua oi kona loa mamua o ko ka honua, A o ka laula imua o ko ke kai.
10 “Ngati Iye atabwera ndi kukutsekera mʼndende nakutengera ku bwalo la milandu, ndani angathe kumuletsa?
Ina e hopu mai ia, a hoopaa iho, a hookolokolo, Alaila owai la ka mea e keakea ia ia?
11 Ndithudi, Mulungu amazindikira anthu achinyengo; akaona choyipa, kodi sachizindikira?
No ka mea, ua ike no ia i ka poe hewa, Ua nana mai hoi ia i ka hala; Aole anei ia e ike mai?
12 Munthu wopanda nzeru sizingatheke kukhala wanzeru monganso mwana wa bulu wakuthengo sangasanduke munthu.
E ake ke kanaka naaupo i akamai, O ke kanaka i hanau nae me he keiki la a ka hoki hihiu.
13 “Koma ngati upereka mtima wako kwa Iye ndi kutambasulira manja ako kwa Iyeyo,
Ina e hoomakaukau oe i kou naau, A e kikoo aku i kou mau lima io na la;
14 ngati utaya tchimo limene lili mʼdzanja lako ndi kusalola choyipa kuti chikhale mʼmoyo mwako,
Ina he hewa iloko o kou lima, e hoolei loa aku ia; A mai ae e noho ka hewa ma kou mau halelewa.
15 udzatukula mutu wako wosachita manyazi; udzayima chilili ndipo sudzachita mantha.
Alaila e hoala ae oe i kou maka me ke kina ole; A e ku paa no oe, aole hoi e makau:
16 Udzayiwala ndithu zowawa zako, zidzakhala ngati madzi amene apita kale.
No ka mea, e hoopoina no oe i ka ehaeha, A e hoomanao ia mea, e like me ka wai i kahe aku:
17 Moyo wako udzawala kupambana usana, ndipo mdima udzakhala ngati mmawa.
A e kupaa kou ola loa ana, e like me ke awakea; Ano ua pouli oe, alaila e like no oe me ke kakahiaka.
18 Udzalimba mtima popeza pali chiyembekezo; ndipo udzayangʼana mbali zonse ndi kugona mosatekeseka.
A e maluhia oe, no ka mea, he mea no e laua ai ka manao; Ano ua poho ka manao, aka, alaila, e noho maluhia oe.
19 Udzagona pansi, popanda wina wokuopseza ndipo ambiri adzakupempha kuti uwachitire chifundo.
A e moe iho oe ilalo, aohe mea nana oe e hoomakau mai; A nui na mea e hoalohaloha imua ou.
20 Koma anthu oyipa adzafuna thandizo osalipeza, ndipo adzasowa njira yothawirapo; chiyembekezo chawo chidzakhala imfa basi.”
Aka, e pio na maka o ka poe hewa, A ua nele lakou i ka puuhonua, A o ko lakou manaolana, o ke kuu ana no ia o ka uhane.

< Yobu 11 >