< Yeremiya 47 >

1 Uthenga umene Yehova anamupatsa mneneri Yeremiya wonena za Afilisti, Farao asanathire nkhondo Gaza ndi uwu:
The word of the Lord, that was maad to Jeremye, the profete, ayens Palestyns, bifor that Farao smoot Gaza.
2 Yehova akuti, “Taonani mmene madzi akubwerera kuchokera kumpoto; adzasanduka mtsinje wosefukira ndi a mkokomo. Adzasefukira mʼdziko monse ndi kumiza chilichonse mʼmenemo, mizinda ndi onse okhala mʼmenemo. Anthu adzafuwula; anthu onse okhala mʼdzikomo adzalira
The Lord seith these thingis, Lo! watris schulen stie fro the north, and tho schulen be as a stronde flowynge, and tho schulen hile the lond, and the fulnesse therof, the citee, and the dwelleris therof. Men schulen crie, and alle the dwelleris of the lond schulen yelle,
3 akadzamva mgugu wa ngʼombe zazimuna zothamanga, phokoso la magaleta ake ndi kulira kwa mikombero yake. Makolo sadzatembenuka kuti athandize ana awo; manja awo adzangoti khoba.
for the noise of boost of armed men, and of werriours of hym, and for mouyng of hise cartis, and multitude of hise wheelis. Fadris bihelden not sones with clumsid hondis,
4 Pakuti tsiku lafika lowononga Afilisti onse ndi kupha onse otsala, onse amene akanatha kuthandiza Turo ndi Sidoni. Yehova ali pafupi kuwononga Afilisti, otsala ochokera ku zilumba za ku Kafitori.
for the comyng of the dai in which alle Filisteis schulen be destried; and Tirus schal be destried, and Sidon with alle her othere helpis. For the Lord hath destried Palestyns, the remenauntis of the ile of Capadocie.
5 Anthu a ku Gaza ameta mipala; anthu a ku Asikeloni akhala chete. Inu otsala a ku chigwa, mudzakhala mukudzichekacheka mpaka liti?
Ballidnesse cam on Gaza; Ascolon was stille, and the remenauntis of the valei of tho.
6 “Mukulira kuti, ‘Aa, lupanga la Yehova, kodi udzapumula liti? Bwerera mʼmalo ako; ukhale momwemo ndipo ukhale chete.’
Hou longe schalt thou falle doun, O! swerd of the Lord, hou long schalt thou not reste? Entre thou in to thi schethe, be thou refreischid, and be stille.
7 Koma lupangalo lidzapumula bwanji pamene Yehova walilamulira kuti lithire nkhondo Asikeloni ndi anthu a mʼmbali mwa nyanja?”
Hou schal it reste, whanne the Lord comaundide to it ayens Ascalon, and ayens the see coostis therof, and there hath seide to it?

< Yeremiya 47 >