< Yesaya 62 >

1 Chifukwa chokonda Ziyoni sindidzakhala chete, chifukwa chokonda Yerusalemu sindidzakhala chete, mpaka chilungamo chake chitaoneka poyera ngati kuwala, ndi chipulumutso chake chitaoneka ngati sakali yoyaka.
من برای اورشلیم دعا خواهم کرد و ساکت نخواهم نشست تا آن هنگام که اورشلیم نجات یابد و پیروزی او مانند مشعلی در تاریکی بدرخشد.
2 Mitundu ya anthu idzaona iwe utapambana pa nkhondo ndipo mafumu onse adzaona ulemerero wako. Adzakuyitanira dzina latsopano limene adzakupatse ndi Yehova.
ای اورشلیم، قومها پیروزی تو را به چشم خواهند دید و پادشاهان شکوه و عظمت تو را مشاهده خواهند کرد. خداوند نام جدیدی بر تو خواهد نهاد،
3 Udzakhala ngati chipewa chaulemerero mʼdzanja la Yehova, ndi ngati nduwira yaufumu mʼdzanja la Mulungu wako.
و تو برای خداوند تاج افتخار خواهی بود.
4 Sadzakutchanso “Wosiyidwa,” ndipo dziko lako silidzatchedwanso “Chipululu.” Koma dzina lako latsopano lidzakhala “Ndakondwera naye.” Ndipo dziko lako lidzatchedwa “Wokwatiwa.” Chifukwa Yehova akukondwera nawe, ndipo adzakhala ngati mwamuna wa dziko lako.
تو را دیگر «شهر متروک» نخواهند خواند و اسرائیل را «سرزمین ترک شده» نخواهند نامید. نام جدید تو «شهر محبوب خدا» و نام جدید اسرائیل، «عروس خدا» خواهد بود، زیرا خداوند به تو رغبت خواهد داشت و اسرائیل را همسر خود خواهد دانست.
5 Monga mnyamata amakwatira namwali, momwenso mmisiri wodzakumanga adzakukwatira; monga mkwati amakondwera ndi mkwatibwi, chonchonso Mulungu adzakondwera nawe.
همان‌گونه که یک مرد جوان، دوشیزه‌ای را به عقد خود درمی‌آورد، آفرینندهٔ تو نیز تو را همسر خود خواهد ساخت. همان‌گونه که داماد به تازه عروسش دل می‌بندد، خداوند نیز به تو دل خواهد بست.
6 Iwe Yerusalemu, pa malinga ako ndayikapo alonda; sadzakhala chete usana kapena usiku. Inu amene mumakumbutsa Yehova za malonjezo ake musapumule.
ای اورشلیم، بر حصارهایت دیدبانانی گماشته‌ام که روز و شب دعا می‌کنند. آنان ساکت نخواهند شد تا هنگامی که خداوند به وعده‌هایش عمل کند. ای کسانی که دعا می‌کنید، خداوند را آرامی ندهید تا هنگامی که اورشلیم را استوار کند و آن را محل عبادت تمام مردم جهان سازد.
7 Musamupatse mpata wopuma mpaka atakhazikitsa Yerusalemu kukhala mzinda umene dziko lapansi lidzawutamande.
8 Yehova analumbira atakweza dzanja lake. Anati, “Sindidzaperekanso tirigu wako kuti akhale chakudya cha adani ako, ndipo alendo sadzamwanso vinyo wako watsopano pakuti unamuvutikira.
خداوند برای اورشلیم قسم خورده و با قدرت خویش به آن عمل خواهد کرد. او گفته است: «دیگر اجازه نخواهم داد دشمنان تو بر تو یورش آورند و غله و شرابت را که برایش زحمت کشیده‌ای غارت کنند.
9 Koma amene amakakolola ndiwo amene adzadye buledi ndi kutamanda Yehova, ndipo amene amasonkhanitsa pamodzi mphesa ndiwo amene adzamwe vinyo mʼmabwalo a Nyumba yanga.”
ساکنان تو نانی را که از غلهٔ خود به دست آورده‌اند خواهند خورد و خداوند را شکر خواهند گفت؛ آنها شرابی را که با دست خود درست کرده‌اند در صحن خانهٔ خداوند خواهند نوشید.»
10 Tulukani, dutsani pa zipata! Konzerani anthu njira. Lambulani, lambulani msewu waukulu! Chotsani miyala. Kwezani mbendera kuti mitundu ya anthu izione.
ای مردم اورشلیم از شهر خارج شوید و جاده‌ای برای بازگشت قوم خود آماده سازید! سنگها را از سر راه بردارید و پرچم را برافرازید تا قومها آن را ببینند و بدانند
11 Yehova walengeza ku dziko lonse lapansi kuti, Awuzeni anthu a ku Yerusalemu kuti, “Taonani, chipulumutso chanu chikubwera; Yehova akubwera ndi mphotho yake akubwera nazo zokuyenerani.”
که خداوند به تمام مردم جهان اعلام می‌کند که به شما بگویند: «ای مردم اورشلیم، خداوند به نجات شما می‌آید و قوم خود را که آزاد ساخته است همراه خود می‌آورد!»
12 Iwo adzatchedwa Anthu Opatulika, owomboledwa a Yehova; ndipo adzakutchani “Okondwa a Yehova” “Mzinda umene Yehova sanawusiye.”
ای مردم اورشلیم، شما «قوم مقدّس خدا» و «نجات یافتگان خداوند» نامیده خواهید شد و اورشلیم «شهر محبوب خدا» و «شهر مبارک خداوند» خوانده خواهد شد.

< Yesaya 62 >