< Yesaya 25 >
1 Yehova ndinu Mulungu wanga; ine ndidzakukwezani ndi kutamanda dzina lanu, pakuti mwachita zodabwitsa zimene munakonzekeratu kalekale mokhulupirika kwambiri.
O Yahweh, sika ti Diosko; itan-okka, idayawko ti naganmo; ta nagaramidka kadagiti nakaskasdaaw a banbanag, banbanag a naplano iti nabayagen a tiempo, a matungpal nga awan pagkuranganna.
2 Inu mwasandutsa mzinda uja kukhala mulu wamiyala. Ndipo mzinda wamalinga wasanduka bwinja, linga la anthu achilendo lero si mzindanso ndipo sidzamangidwanso.
Ta pinagbalinmo a gabsuon ti siudad, siudad a nasarikedkedan, nadadael ken pinagbalinmo nga awan serserbina ti pagkamangan a siudad dagiti kabusor.
3 Nʼchifukwa chake anthu amphamvu adzakulemekezani; mizinda ya mitundu ya anthu ankhanza idzakuopani.
Ngarud, idayawdakanto ti nabibileg a tattao; agbutengto kenka ti siudad dagiti nararanggas a nasion.
4 Inu mwakhala ngati populumukira pa anthu osauka, mwakhala ngati kobisalirako munthu wovutika pa nthawi ya masautso ake. Mwakhala ngati pobisalirapo pa nthawi ya mphepo yamkuntho ndi mthunzi pa nthawi ya dzuwa. Pakuti anthu ankhanza ali ngati mphepo yamkuntho yowomba pa khoma,
Ta sika ket salaknib kadagiti napanglaw, mangay-aywan iti marigrigat iti tiempo ti panagrigat, pagkamangan manipud iti bagyo, paglinongan manipud iti darang ti init, iti tiempo a dumarup dagiti naranggas a tattao a kasla bagyo a mangdungpar iti pader.
5 ndiponso ngati kutentha mʼdziko lowuma. Inu mumaletsa phokoso la anthu achilendo. Monga momwe mthunzi wa mtambo umachepetsa kutentha, inu munaletsa nyimbo za anthu ankhanza.
Kas iti pudot iti tiempo ti kalgaw, pagsardengemto ti ariwawa dagiti ganggannaet; kas iti pudot iti linong ti ulep, mapasardengto ti kanta dagiti naranggas.
6 Pa phiri ili Yehova Wamphamvuzonse adzakonzera anthu a mitundu yonse madyerero a zakudya zokoma ndi vinyo wabwino. Phwando la nyama yonona ndi vinyo wabwino kwambiri.
Iti daytoy a bantay, mangipaayto ni Yahweh a Mannakabalin-amin iti maysa a padaya a para kadagiti amin a tattao a pakaidasaranto dagiti agkakaimas a taraon, agkakaimas nga arak, dagiti agkakalukneng a karne, ti kababaakan ken kaiimasan nga arak.
7 Iye adzachotsa kulira kumene kwaphimba anthu ngati nsalu. Adzachotsa chinsalu chimene chakuta mitundu yonse ya anthu.
Dadaelennanto iti daytoy a bantay ti nangabbong kadagiti amin a tattao, ti kasla nalaga a saput a nangabbong kadagiti amin a nasion.
8 Yehova adzathetsa imfa mpaka muyaya, Ambuye Yehova adzapukuta misozi mʼmaso mwa munthu aliyense; adzachotsa manyazi a anthu ake pa dziko lonse lapansi, Yehova wayankhula.
Alun-onenna ti patay iti agnanayon, ken punasento ni Apo a Yahweh dagiti lulua dagiti tattao; ikkatennanto ti pakaibabainan dagiti tattaona iti entero a daga, ta kinuna daytoy ni Yahweh.
9 Tsiku limenelo iwo adzati, “Ndithudi, uyu ndiye Mulungu wathu; ife tinamudalira ndipo anatipulumutsa. Uyu ndiye Yehova, ife tinamudalira; tiyeni tikondwe ndi kusangalala chifukwa watipulumutsa.”
Maibaganto iti dayta nga aldaw, “Kitaenyo, daytoy ti Diostayo; inur-uraytayo isuna, ket isalakannatayo. Daytoy ni Yahweh; inur-uraytayo isuna, agragsak ken agrag-otayo iti panangisalakanna.
10 Yehova adzateteza phiri limeneli ndi dzanja lake; ndipo Amowabu adzawapondereza pomwe alilipo, ngati mmene amapondera manyowa mʼdzenje.
Ta iti daytoy a bantay, iyunnatto ni Yahweh ti imana; ket maipayatpayatto ti Moab, a kas iti pannakaipayatpayat ti garami iti abut a napunno iti takki.
11 Amowabuwo adzatambasula manja awo mʼmenemo, ngati mmene amachitira munthu wosambira. Koma Mulungu adzathetsa kunyada kwawo ngakhale luso la manja awo.
Iyunnatdanto dagiti imada iti tenga ti abut, kas iti panangiyunnat ti lumalangoy kadagiti imana tapno aglangoy; ngem imamegto ni Yahweh ti pagpanpannakkelda iti likudan ti panangikagumaan dagiti imada.
12 Iye adzagumula malinga awo ataliatali ndipo adzawagwetsa ndi kuwaponya pansi, pa fumbi penipeni.
Rebbaennanto dagiti nangato a sarikedked a paderyo ket pagbalinenna a tapok.