< Hoseya 4 >

1 Inu Aisraeli, imvani mawu a Yehova, chifukwa Yehova ali ndi mlandu ndi inu amene mumakhala mʼdzikoli: “Mʼdziko mwanu mulibe kukhulupirika, mulibe chikondi mulibe kulabadira za Mulungu.
E HOOLOHE oukou, e na mamo a Iseraela, i ka olelo a Iehova: no ka mea, he hakaka ko Iehova me na kanaka o ka aina; No ka mea, aohe oiaio, aohe aloha, aohe ike i ke Akua ma ka aina.
2 Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha. Kuba ndi kuchita chigololo; machimo achita kunyanya ndipo akungokhalira kuphana.
O ka hoohiki ino, ka hoopunipuni, ka pepehi kanaka, ka aihue, a me ka moe kolohe, ka lakou i hoomahuahua ae ai, a pili aku no ke koko i ke koko.
3 Chifukwa chake dziko likulira ndipo onse amene amakhalamo akuvutika; zirombo zakuthengo ndi mbalame zamumlengalenga ndiponso nsomba zamʼnyanja zikufa.
No ia mea, e kanikau auanei ka aina, A e nawaliwali na mea a pau e noho ana maluna ona, Me na holoholona o ke kula, a me na manu o ka lewa; Oia, e laweia'ku hoi na ia o ke kai.
4 “Koma wina asapeze mnzake chifukwa, wina aliyense asayimbe mlandu mnzake, pakuti anthu ako ali ngati anthu amene amayimba mlandu wansembe.
Aka, mai hakaka kekahi kanaka, aole hoi e papa aku ia hai: No ka mea, o kou poe kanaka, ua like lakou me ka poe e hakaka ana me ke kahuna.
5 Mumapunthwa usana ndi usiku ndipo aneneri amapunthwa nanu pamodzi. Choncho ndidzawononga amayi anu.
Nolaila e hina oe i ke ao, O ke kaula hoi, e hina pu ia me oe i ka po; A e luku aku au i kou makuwahine.
6 Anthu anga akuwonongeka chifukwa chosadziwa. “Pakuti mwakana kudziwa, Inenso ndidzakukanani monga ansembe anga; chifukwa mwayiwala lamulo la Mulungu wanu, Inenso ndidzayiwala ana anu.
Ua lukuia ko'u poe kanaka no ka ike ole: No ka mea, ua hoowahawaha oe i ka ike, E hoowahawaha aku hoi au ia oe, Aole oe e malama i ka oihanakahuna na'u: A no kou hoopoina ana i ke kanawai o kou Akua, Owau hoi kekahi e hoopoina i kau poe keiki.
7 Ansembe ankati akachuluka iwo ankandichimwiranso kwambiri; iwo anasinthanitsa ulemerero wawo ndi chinthu china chonyansa.
E like me ko lakou nui ana, pela lakou i hana hewa mai ai ia'u: A e hoololi au i ko lakou nani i mea hilahila.
8 Amalemererapo pa machimo a anthu anga ndipo amafunitsitsa kuti anthuwo azipitiriza kuchimwa.
Ua ai lakou i ka hewa o kuu poe kanaka, A ua kau i ko lakou mau naau ma ko lakou la hala.
9 Ndipo zidzakhala motere: zochitikira anthu ena, zidzachitikiranso ansembe. Ndidzawalanga onsewo chifukwa cha njira zawo, ndidzawabwezera chifukwa cha machitidwe awo.
A e like auanei me na kanaka, pela no me ke kahuna: A e hoopai aku au ia lakou e like me ko lakou mau aoao, A e hoouku aku au ia lakou e like me ka lakou hana ana.
10 “Iwo azidzadya koma sadzakhuta; azidzachita zachiwerewere koma sadzachulukana, chifukwa anasiya Yehova kuti adzipereke
A e ai lakou, aole nae e maona, A e moe kolohe lakou, aole nae e mahuahua ae; No ka mea, ua hooki lakou i ka malama ia Iehova.
11 ku zachiwerewere, ku vinyo wakale ndi watsopano, zimene zimachotsa nzeru zomvetsa zinthu
O ka moe kolohe, o ka waina, a me ka waina hou, oia ke lawe aku i ka naau.
12 za anthu anga. Anthu anga amapempha nzeru ku fano lamtengo ndipo ndodo yawo yamtengo imawayankha. Mzimu wachiwerewere umawasocheretsa; iwo sakukhulupirika kwa Mulungu wawo.
Ke ninau nei kuu poe kanaka i ko lakou kii laau, A ua hoike mai ko lakou kookoo ia lakou; No ka mea, ua hooauwana ka naau moe kolohe ia lakou; Ua hele moe kolohe lakou mai lalo ae o ko lakou Akua.
13 Amapereka nsembe pamwamba pa mapiri ndi kufukiza lubani pa zitunda, pa tsinde pa mtengo wa thundu, mnjale ndi mkundi, pamene pali mthunzi wabwino. Nʼchifukwa chake ana anu aakazi akuchita zachiwerewere ndipo akazi a ana anu akuchita zigololo.
Kaumaha aku la lakou ma kahi kiekie o na mauna, A kuni i ka mea ala maluna o na puu, Malalo o ka laau oka, a me ka laau popela, a me ka laau kaa, No ka mea, ua oluolu kona malumalu: No ia mea, e moe kolohe ka oukou poe kaikamahine, A e moe kolohe ka oukou poe hunona wahine.
14 “Ine sindidzalanga ana anu aakazi pamene iwo adzachita zachiwerewere, kapena akazi a ana anu pamene adzachita zigololo. Paja inu nomwe amunanu mumayenda ndi akazi achiwerewere, ndipo mumapereka nsembe pamodzi ndi akazi achiwerewere a ku malo opembedzerako. Anthu amene alibe nzeru adzawonongeka ndithu!
Aole au e hoopai aku i ka oukou poe kaikamahine no ko lakou moe kolohe ana, A i ka oukou poe hunona wahine no ko lakou moe kolohe ana: No ka mea, ua hookaawale pu lakou ia lakou iho me na wahine hookamakama, A ua mohai pu lakou me na wahine moe kolohe: A o ka poe kanaka ike ole, e make no lakou.
15 “Ngakhale umachita chigololo, iwe Israeli, Yuda asapezeke ndi mlandu wotere. “Usapite ku Giligala. Usapite ku Beti-Aveni. Ndipo usalumbire kuti, ‘Pali Yehova wamoyo!’
Ina o oe, e ka Iseraela, i moe kolohe, mai hana hewa o ka luda: A mai hele oukou i Gilegala, Mai pii ae oukou i Betavena, Mai hoohiki, E ola o Iehova.
16 Aisraeli ndi nkhutukumve, ngosamva ngati ana angʼombe. Kodi Yehova angathe kuwaweta bwanji ngati ana ankhosa pa msipu wabwino?
No ka mea, ua paakiki o ka Iseraela, e like me ka paakiki o ka bipiwahine hou: Ano e hanai o Iehova ia lakou, e like me ke keikihipa ma kahi akea.
17 Efereimu waphathana ndi mafano; mulekeni!
Ua hui pu o Eperaima me na kii, e waiho aku ia ia.
18 Ngakhale pamene zakumwa zawo zatha, amapitiriza kuchita zachiwerewere; atsogoleri awo amakonda kwambiri njira zawo zochititsa manyazi.
Ua hewa ka lakou ahainu, Ua mau ko lakou moe kolohe ana; A ake kona poe alii i ka hilahila.
19 Adzachotsedwa ndi kamvuluvulu ndipo adzachita manyazi chifukwa cha nsembe zawo.
Ua hoopaa ka makani ia ia iloko o kona mau eheu, A e hilahila auanei lakou i ka lakou mau mohai.

< Hoseya 4 >