< Ahebri 5 >
1 Mkulu wa ansembe aliyense amasankhidwa kuchokera pakati pa anthu ndipo amayikidwa kuti aziwayimirira pamaso pa Mulungu, kuti azipereka mphatso ndi nsembe chifukwa cha machimo.
Banghangziam cile thiampi sang te sia mihing sung pan in a kiteal hi a, letsong te le mawna atu biakpiakna te sia Pathian tung ah mihing te atu pia tu in nasep piak te a hihi.
2 Popeza kuti iye mwini ali ndi zofowoka zake, amatha kuwalezera mtima amene ali osadziwa ndi osochera.
Ama in a mawmaw te le lampial te tung ah hesuak theina nei hi; banghangziam cile ama tatak zong thaneamna in kiimum hi.
3 Chifukwa cha ichi, iye amadziperekera nsembe chifukwa cha machimo ake omwe ndiponso chifukwa cha machimo a anthu ena.
Hi thu hang in ngual mawna atu biakpiakna piaksak a kul bangma in, ama mawna atu zong biakpiak kul veve hi.
4 Palibe amene amadzipatsa yekha ulemu wotere, koma amachita kuyitanidwa ndi Mulungu monga momwe anayitanidwira Aaroni.
Aaron bang in Pathian sapna a sang te simngawl, kuama in hi upatna sia ama atu in la ngawl hi.
5 Nʼchifukwa chake Khristu sanadzipatse yekha ulemu wokhala Mkulu wa ansembe. Koma Mulungu anamuwuza kuti, “Iwe ndiwe Mwana wanga; Ine lero ndakhala Atate ako.”
Tasia bangma in Christ zong thiampi sang a suak tu in ama le ama ki minthangsak ngawl hi; ahihang ama tung ah, Nangma sia ka Tapa na hihi, tu ni in kong nei zo hi, ci hi.
6 Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
Mundang zong ah, nangma sia Melchizedek bang in tawntung thiampi na hihi, ci hi. (aiōn )
7 Yesu, pa nthawi imene anali munthu pa dziko lapansi pano, anapereka mapemphero ake ndi zopempha mofuwula ndi misozi kwa Iye amene akanamupulumutsa ku imfa, ndipo anamumvera chifukwa anagonjera modzipereka.
Ama sia cilesa taw a omlai in, thina pan ama a ngum thei pa tung ah nasiatak au in thitui taw a thungetna le ama atu thungetna te a vawt ciang in, Pathian a zatak hu in a thungetna za hi;
8 Ngakhale Iye anali Mwana wa Mulungu anaphunzira kumvera pomva zowawa.
Ama sia Tapa hi napi, a thuakna te pan in thunitna sin hi;
9 Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios )
Taciang Ama a cialcin zawkciang in, thu ni te theampo atu in tawntung ngupna i kipatna hong suak a; (aiōnios )
10 Ndipo Mulungu anamuyika kukhala Mkulu wa ansembe, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.
Pathian in ama sia Melchizedek pan a kilua susuk thiampi in saang hi.
11 Tili ndi zambiri zoti tinganene pa zimenezi, koma ndi zovuta kukufotokozerani chifukwa ndinu ochedwa kuphunzira.
Melchizedek thu note kong son nop tam mama om napi, note sia thu hehak mama na hi uh hu in thu son tu haksa mama hi.
12 Ngakhale kuti pa nthawi ino munayenera kukhala aphunzitsi, pakufunikabe munthu wina kuti abwerezenso kudzakuphunzitsani maphunziro oyambira a choonadi cha Mulungu. Ndinu ofunika mkaka osati chakudya cholimba!
Banghangziam cile hun te zong ngei zo ahi bangma sya na sep tu uh kilawm zo napi, Pathian kammal te sia a kipat pan in hil na kul lai uh a, ansak nei zo ngawl lai in noai bek a dawn zo te na hi uh hi.
13 Aliyense amene amangodya mkaka okha, akanali mwana wakhanda, sakudziwa bwino chiphunzitso cha chilungamo.
Banghangziam cile noai bek a nete sia nausen ahikom in, thutang suana thu sung ah bangma thiamna nei ngawl lai hi.
14 Koma chakudya cholimba ndi cha anthu okhwima msinkhu, amene pogwiritsa ntchito nzeru zawo, aphunzira kusiyanitsa chabwino ndi choyipa.
Ahihang antak sia a picing te atu hi a, amate sia a thu ngaisutna te le a heakna te a zak uh hu in a pha le pha ngawl zong khentel thei uh hi.