< Filemoni 1 >

1 Kuchokera kwa Paulo, amene ndili mʼndende chifukwa cha Khristu Yesu ndi Timoteyo mʼbale wathu. Kulembera Filemoni, bwenzi lathu lokondedwa ndi mtumiki mnzathu.
Jesus Christ hang in thong a tak keima Paul le i suapui Timothy in ka it mama uh le ka naseppui uh a hi Philemon,
2 Kwa Apiya mlongo wathu, Arkipo msilikali mnzathu, ndiponso mpingo umene umasonkhana mʼnyumba mwanu.
Ka it mama uh Apphia, ka ngalkap seppui Archippus le na inn a om pawlpi te tung ah:
3 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale ndi inu.
I Pa Pathian le Topa Jesus Christ tung pan thuthiamna le thinnopna hong om tahen.
4 Ine ndimayamika Mulungu wanga nthawi zonse ndikakukumbukira iwe mʼmapemphero anga.
Ka thunget na theampo ah nangma hong phawk tawntung in ka Pathian tung lungdam ka ko hi,
5 Pakuti ndamva za chikondi chako, za chikhulupiriro chako mwa Ambuye Yesu ndiponso za chikondi chako pa oyera mtima onse.
Banghangziam cile, Topa Jesus le mithiangtho te tung ah na nei itna le upna thu ka za hi;
6 Ine ndikupemphera kuti mgwirizano wako ndi ife mʼchikhulupiriro ukhale opindulitsa pozamitsa nzeru zako zozindikira zinthu zilizonse zabwino zimene timagawana chifukwa cha Khristu.
Christ Jesus sung ah, nasung a om napha theampo heakna hang in na upna sia ngualdang na hil ciang vang nei tu in thu kong ngetsak hi.
7 Mʼbale, chikondi chako chandipatsa chimwemwe chachikulu ndi chilimbikitso, chifukwa umatsitsimutsa mitima ya anthu a Ambuye.
Banghangziam cile, suapui pa awng, na itna sung ah, lungdamna le hanthotna lian mama nei khu hi, banghangziam cile mithiangtho te thinsung ah, nangma hang in thathak hong dim hi.
8 Tsopano ngakhale kuti mwa Khristu nditha kulimba mtima ndi kulamulira kuti uchite zimene uyenera kuchita,
Tua ahikom Christ sung ah hangsantak in thu kong piak tu hunnuam hong suak hi.
9 komabe ndikupempha mwachikondi. Ine Paulo, munthu wokalamba, ndipo tsopano ndili mʼndende chifukwa cha Khristu Yesu,
Ahihang kum tam zo le tu zong in Jesus Christ hang in thong a tak keima Paul in, itna taw in kong thum nuam zaw hi.
10 ndikukupempha chifukwa cha mwana wanga Onesimo, amene ndamubala ndili mu unyolo.
Kolhawng taw hen na ka thuak lai in ka nei ka tapa Onesimus atu kong thum hi:
11 Anali wopanda phindu kwa iwe, koma tsopano wasanduka wa phindu kwa iwe ndi kwa inenso.
A bosa hun sung ah nang atu in bangma phatuam ngawl hi, ahihang tu in nangma le keima atu in phatuam mama hi:
12 Ine ndikumutumizanso kwa iwe tsopano, koma potero ndikukhala ngati ndikutumiza mtima wanga weniweni.
Ama kong heakkik sak hi: tua ahikom, ka thinsung laingil bang in na sang in:
13 Ndikanakonda ndikanakhala naye kuno kuti iyeyo azinditumikira mʼmalo mwako pamene ndili mu unyolo chifukwa cha Uthenga Wabwino.
Lungdamna thu hang in kolhawng taw ka om laitak in, nangma tang in hong khoi tu in ama sia ka kung ah omsak nuam khi hi:
14 Koma sindikufuna kuchita kanthu osakufunsa, nʼcholinga chakuti chilichonse chabwino ungandichitire chikhale mwakufuna kwako osati mokakamiza.
Ahitazong, na thukim na sia, kong sawl hamtang hang hi ngawl in, nangma thinsung suak in na khensat a hi thei natu in, nong heakpui ngawl in bangma ka ngamta nuam bua hi.
15 Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios g166)
Hun tomno sung a tai na thu sia a tawntung in na nei kik thei natu hi zaw tu hi; (aiōnios g166)
16 Osati ngati kapolo, koma woposa kapolo, ngati mʼbale wokondedwa. Iyeyu ndi wokondedwa kwambiri kwa ine koma kwa iweyo ndi wokondedwa koposa, ngati munthu komanso ngati mʼbale mwa Ambuye.
Tu in ama sia sila bang hi ngawl in, sila sang in a sangzaw in ama na sang in, ama sia keima atu, a tuan in ka it suapui hi a, cilesa lam le Topa lam ah nangma atu in bangza in pha seseam tu ziam?
17 Tsono ngati umati ndine mnzako, umulandire iyeyu monga momwe ukanandilandirira ineyo.
Tua ahikom naseppui bangin nong ngaisun a hile, keima nong san tu bangin, ama na sangkik in.
18 Ngati anakulakwira kapena kukongola kanthu kalikonse, ndidzalipira ineyo.
Nang tung ah khial a hile, a hibale nangtung ah bat hong nei a hile, keima bat bang in hong ngaisutsak tan;
19 Ine, Paulo ndikulemba zimenezi ndi dzanja langa. Ine ndidzalipira. Nʼkosafunika kukukumbutsa kuti iweyo ngongole yako kwa ine ndi moyo wakowo.
Keima Paul in ka khut tatak tawma in hong at khi hi, keima in hong lokik tu khi hi: ahihang keima tung tatak ma ah nangma in zong hong ba ni hi, kong ci bua hi.
20 Mʼbale, ndikufuna kuti ndipindule nawe mwa Ambuye; tsono tsitsimutsa mtima wanga mwa Khristu.
Hi hi, suapui pa, Topa sung ah nangma hang in lungdamna hong neisak tan: Topa sung ah ka thinsung laingil thathak hong dimsak tan.
21 Ine ndili ndi chitsimikizo cha kumvera kwako pamene ndikukulembera kalatayi. Ndikulemba ndikudziwa kuti udzachita ngakhale kuposa zimene ndakupemphazi.
Thu ni na hi na sung ah muanna nei in na tung ah lai hong at khi hi, kong son za sang a tam zaw seam tu ni hi, ci kong he hi.
22 Chinthu chinanso ndi ichi: undikonzere malo, chifukwa ndikukhulupirira kuti Mulungu adzamvera mapemphero anu ndi kundibwezera kwa inu.
Tabang cikteak ma in ka ngia natu mun hong puakholsak tan: banghangziam cile na thungetna uh hang in note kung ah hong theng thei tu khi hi, ci zong lametna ka nei hi.
23 Epafra, wamʼndende mnzanga chifukwa cha Khristu Yesu akupereka moni.
Christ Jesus hang in ka thongtakpui Epaphras;
24 Atumiki anzanga awa, Marko, Aristariko, Dema ndi Luka, akuperekanso moni.
Ka naseppui Marcus, Aristarchus, Demas le Lucas te in hong nukset hi.
25 Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi mzimu wako.
I Topa Jesus Christ i hesuakna na tha taw hong om tahen. Amen.

< Filemoni 1 >