< Ezekieli 7 >
1 Yehova anandipatsa uthenga uwu kuti,
Кувынтул Домнулуй мь-а ворбит астфел:
2 “Iwe mwana wa munthu, Ine Ambuye Yehova ndikuwuza dziko la Israeli kuti: “Chimaliziro! Chimaliziro chafika ku ngodya zinayi za dziko.
„Ши ту, фиул омулуй, аскултэ! Аша ворбеште Домнул Думнезеу деспре цара луй Исраел: ‘Вине сфыршитул, вине сфыршитул песте челе патру марӂинь але цэрий!
3 Chimaliziro chili pa iwe tsopano. Mkwiyo wanga ndidzawuthira pa iwe. Ndidzakuweruza molingana ndi machitidwe ako ndi kukulanga chifukwa cha zonyansa zako.
Акум вине сфыршитул песте тине; Ымь вой тримите мыния ымпотрива та, те вой жудека дупэ фаптеле тале. Ши те вой педепси пентру тоате урычуниле тале.
4 Ine sindidzakumvera chisoni kapena kukuleka. Ndidzakulanga ndithu chifukwa cha ntchito zako zoyipa komanso chifukwa cha miyambo yako yonyansa imene ili pakati pako. Pamenepo udzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
Окюл Меу ва фи фэрэ милэ пентру тине ши ну Мэ вой ындура, чи те вой педепси дупэ фаптеле тале, ку тоате кэ урычуниле тале вор фи ын мижлокул тэу ши ар требуи сэ те ажуте. Ши вець шти кэ Еу сунт Домнул.’
5 “Zimene ndikunena Ine Ambuye Yehova ndi izi: “Chiwonongeko! Chiwonongeko chimene sichinamvekepo! Taona chikubwera!
Аша ворбеште Домнул Думнезеу: ‘Ятэ, вине о ненорочире, о ненорочире немайпоменитэ!
6 Chimaliziro chafika! Chimaliziro chafika! Chiwonongeko chakugwera. Taona chafika!
Вине сфыршитул, вине сфыршитул; се трезеште ымпотрива та! Ятэ кэ а ши венит!
7 Inu anthu okhala mʼdziko, chiwonongeko chakugwerani. Nthawi yafika, tsiku layandikira; tsiku la chisokonezo osati la chimwemwe pa mapiri.
Ыць вине рындул, локуитор ал цэрий! Вине время, се апропие зиуа де неказ, ши ну де букурие, пе мунць!
8 Ine ndili pafupi kukukwiyirani, ndipo ukali wanga udzathera pa iwe; Ine ndidzakuweruza molingana ndi machitidwe ako ndiponso ndidzakulanga chifukwa cha miyambo yako yonyansa.
Акум Ымь вой вэрса ын курынд урӂия песте тине, Ымь вой потоли мыния песте тине; те вой жудека дупэ фаптеле тале ши те вой педепси пентру тоате минчуниле тале.
9 Ine sindidzakumvera chisoni kapena kukuleka. Ndidzakulanga malingana ndi ntchito zako ndiponso chifukwa cha miyambo yako yonyansa pakati pako.
Окюл Меу ва фи фэрэ милэ ши ну Мэ вой ындура; те вой педепси дупэ фаптеле тале, мэкар кэ урычуниле тале вор фи ын мижлокул тэу ши ар требуи сэ те ажуте. Ши вець шти кэ Еу сунт Домнул, Чел че ловеште!
10 “Taona, tsikulo! Taona, lafika! Chiwonongeko chako chabwera. Ndodo yaphuka mphundu za maluwa. Kudzitama kwaphuka.
Ятэ зиуа! Ятэ-о кэ вине! Ыць вине рындул! Ынфлореште тоягул, одрэслеште мындрия!
11 Chiwawa chasanduka ndodo yowakwapulira chifukwa cha kuyipa kwawo. Palibe mwa anthu amenewo amene adzatsale. Palibe ndi mmodzi yemwe mwa unyinji wawo. Palibiretu ndipo sipadzapezeka munthu wowalira maliro.
Силничия с-а ынэлцат ка сэ служяскэ де тояг рэутэций; ну май рэмыне нимик дин ей, нич дин глоата лор гэлэӂиоасэ, нич дин богэция лор! Ши нимень ну-й бочеште!
12 Nthawi yafika! Tsiku layandikira! Munthu wogula asakondwere ndipo wogulitsa asamve chisoni, popeza ukali wanga uli pa gulu lonse.
Вине время, се апропие зиуа! Сэ ну се букуре кумпэрэторул, сэ ну се мыхняскэ вынзэторул! Кэч избукнеште мыния ымпотрива ынтреӂий лор мулцимь.
13 Wogulitsa sadzazipezanso zinthu zimene anagulitsa kwa wina chinkana onse awiri akanali ndi moyo, pakuti chilango chidzagwera onsewo ndipo sichingasinthike. Chifukwa cha machimo awo, palibe aliyense amene adzapulumutsa moyo wake.
Ну, вынзэторул ну ва май кэпэта ынапой че а вындут, кяр дакэ ар май фи принтре чей вий; кэч пророчия ымпотрива ынтреӂий лор мулцимь ну ва фи скимбатэ ши, дин причина нелеӂюирий луй, ничунул ну-шь ва пэстра вяца.
14 “Lipenga lalira, ndipo zonse zakonzeka. Koma palibe ndi mmodzi yemwe amene akupita ku nkhondo, pakuti mkwiyo wanga uli pa gulu lonse.
Сунэ трымбица, тотул есте гата, дар нимень ну мерӂе ла луптэ, кэч урӂия Мя избукнеште ымпотрива ынтреӂий лор мулцимь.
15 Ku bwalo kuli kumenyana ndipo mʼkati muli mliri ndi njala. Anthu okhala ku midzi adzafa ndi nkhondo. Iwo okhala ku mizinda adzafa ndi mliri ndi njala.
Афарэ бынтуе сабия, ын касэ, чума ши фоаметя! Чине есте ла кымп ва мури де сабие, яр чине есте ын четате ва фи мынкат де фоамете ши чумэ.
16 Onse amene adzapulumuka ndi kumakakhala ku mapiri, azidzalira ngati nkhunda za ku zigwa. Aliyense azidzabuwula chifukwa cha machimo ake.
Фугарий лор, кынд скапэ, стау пе мунць, ка ниште порумбей ай вэилор, вэйтынду-се тоць, фиекаре де нелеӂюиря луй.
17 Dzanja lililonse lidzalefuka, ndipo bondo lililonse lidzalobodoka ngati madzi.
Мыниле тутурор ау слэбит ши ӂенункий тутурор се топеск ка апа.
18 Iwo adzavala ziguduli ndipo adzagwidwa ndi mantha. Adzakhala ndi nkhope zamanyazi ndipo mitu yawo adzameta mpala.
Се ынчинг ку сачь ши-й апукэ гроаза. Тоате фецеле сунт акоперите де рушине ши тоате капетеле сунт расе.
19 “Iwo adzataya siliva wawo mʼmisewu ndipo golide wawo adzakhala chinthu chonyansa. Siliva ndi golide wawo sizidzatha kuwapulumutsa pa tsiku la ukali wa Yehova. Chuma chawochi sichidzawathandiza kuthetsa njala, kapena kukhala okhuta, pakuti ndicho chinawagwetsa mʼmachimo.
Ышь вор арунка арӂинтул пе улице ши аурул лор ле ва фи о скырбэ. Арӂинтул сау аурул лор ну поате сэ-й скапе ын зиуа урӂией Домнулуй; ну поате нич сэ ле сатуре суфлетул, нич сэ ле умпле мэрунтаеле, кэч ел й-а арункат ын нелеӂюиря лор.
20 Iwo ankanyadira zodzikongoletsera zawo zamakaka ndipo ankazigwiritsa ntchito kupanga mafano awo onyansa ndi zonyansa zawo zina. Nʼchifukwa chake Ine ndidzazisandutsa kukhala zowanyansa.
Се фэляу ку подоаба лор мэряцэ ши ку еа ау фэкут икоанеле урычунилор лор, але идолилор лор. Де ачея ле-о вой префаче ын скырбэ пентру ей.
21 Ndidzazipereka kwa alendo kuti azifunkhe. Anthu oyipa a dziko lapansi adzazilanda ndi kudziyipitsa.
О вой да де жаф ын мыниле стрэинилор ши ка прадэ нелеӂюицилор пэмынтулуй ка с-о пынгэряскэ.
22 Ine ndidzawalekerera anthuwo ndipo adzayipitsa malo anga apamtima. Adzalowamo ngati mbala ndi kuyipitsamo.
Ымь вой ынтоарче фаца де ла ей ши Ми се ва пынгэри Локашул Меу чел Сфынт; да, прэдэторий вор пэтрунде ын ел ши-л вор пынгэри.
23 “Konzani maunyolo, chifukwa dziko ladzaza ndi anthu opha anzawo ndipo mzinda wadzaza ndi chiwawa.
Прегэтиць ланцуриле! Кэч цара есте плинэ де оморурь ши четатя есте плинэ де силничие.
24 Ndidzabweretsa mitundu ya anthu oyipitsitsa kuti idzalande nyumba zawo. Ndidzathetsa kunyada kwa anthu amphamvu pamene anthu akunja adzalowa mʼmalo awo achipembedzo ndi kuyipitsamo.
Вой адуче попоареле челе май реле ка сэ пунэ мына пе каселе лор; вой пуне капэт мындрией челор путерничь ши сфинтеле лор локашурь вор фи пынгэрите.
25 Nkhawa ikadzawafikira adzafunafuna mtendere koma osawupeza.
Вине прэпэдул! Ей каутэ скэпаре, дар скэпаре ну-й!
26 Tsoka lidzatsatana ndi tsoka linzake, ndipo mphekesera idzatsatana ndi mphekesera inzake. Iwo adzayesa kufuna masomphenya kuchokera kwa mneneri. Adzasowa ansembe owaphunzitsa malamulo, ndipo anthu akuluakulu sadzakhalanso ndi uphungu.
Вине ненорочире песте ненорочире, звон дупэ звон. Ей чер ведений пророчилор, дар преоций ну май куноск Леӂя, ши бэтрыний ну май пот да сфатурь.
27 Mfumu idzalira, kalonga adzagwidwa ndi mantha. Manja a anthu a mʼdzikomo azidzangonjenjemera ndi mantha. Ine ndidzawalanga molingana ndi machitidwe awo, ndipo ndidzawaweruza molingana ndi momwe anaweruzira anzawo.
Ымпэратул желеште, воеводул се ынспэймынтэ ши мыниле попорулуй цэрий тремурэ. Ле вой фаче дупэ умблетеле лор, ый вой жудека дупэ кувиинцэ ши вор шти кэ Еу сунт Домнул.’”