< Aefeso 1 >

1 Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu mwachifuniro cha Mulungu. Kulembera oyera mtima a ku Efeso, okhulupirika mwa Khristu Yesu:
Xoossa shene mala Yesus Kiristossa Haware gidida Phawulossape. Yesus Kirstosan diza amanetizaytas Efesonen amaniza asas.
2 Chisomo ndi mtendere kwa inu zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu.
Nu aawa Xoossafe Goda Yesus Kiristossape kiyatethine sarotethi intes gido.
3 Tiyamike Mulungu, Atate a Ambuye athu Yesu Khristu, amene anatipatsa madalitso onse a uzimu kumwamba mwa Khristu.
Nu Goda Yesuss Kiristossa bagara sallon ayana anjjo wurison nuna anjjuda Goda Yesuss Kirisitossa aaway Xoossi anijjeto.
4 Dziko lapansi lisanalengedwe, Mulungu anatisankhiratu mwa Khristu kuti tikhale oyera mtima ndi wopanda cholakwa pamaso pake. Mwa chikondi chake,
Nu iza sinthan geshatana wothoy bayndayta gidana mala buro alamey medhetanape kasse ba siqon Kirstosa bagara nuna dorides.
5 Iye anakonzeratu kuti ife titengedwe ngati ana mwa Yesu Khristu, molingana ndi kukonda kwake ndi chifuniro chake.
Yesus Kiristossa bagara nu iza na gidana mala ba loo7o qofan koyro wursi wothides.
6 Anachita zimenezi kuti tiziyamika ulemerero wa chisomo chake, umene watipatsa kwaulere mwa Khristu amene amamukonda.
Hesika ba dosizade bagara coo mela nusu imetida boncho kiiyatethay galatistan malakko.
7 Mwa Yesu Khristu, chifukwa cha magazi ake, ife tinawomboledwa ndi kukhululukidwa machimo athu molingana ndi kuchuluka kwa chisomo cha Mulungu
Xoossa adho kiyatethan Yesuss sunthan nagarape nu maretidos.
8 chimene anatipatsa mosawumira. Mwa nzeru zonse ndi chidziwitso,
Izi ba kiyatethane cincateth nu bolla kezi darsides.
9 Iye watiwululira chifuniro chake chimene chinali chobisika, chimene anachikonzeratu mwa Khristu, molingana ndi kukoma mtima kwake.
Kiristossa bagara Xoossi nuus qopida xuura qofa Kirstosa bagara nuna erisides.
10 Chimene anakonza kuti chichitike nʼchakuti, ikakwana nthawi yake asonkhanitsa pamodzi mwa Khristu zinthu zonse za kumwamba ndi pa dziko lapansi.
Burope wode wurisethan hanana diza iza qofay sallo bolane biita bolla dizaytas wurisos hu7e gidida Yesuss Kiristossape wursi garse oothanaskko.
11 Iye anatisankhiratu mwa Khristu, atatikonzeratu molingana ndi machitidwe a Iye amene amachititsa zinthu zonse kuti zikwaniritse cholinga cha chifuniro chake,
Wurisikka ba shene mala oothiza iza shenemala nuka iza koyroka izi dorida gish nuni izan doretidosu.
12 nʼcholinga chakuti, ife amene tinali oyamba kukhala ndi chiyembekezo mwa Khristu, tiyamike ulemerero wake.
Nuni kasetidi Kiristossa bagara ekana gidi ufaysan nagizayti Xoossa boncho galatan qoncisansikko.
13 Ndipo inunso pamene munamva mawu a choonadi, Uthenga Wabwino wa chipulumutso chanu, munayikidwanso mwa Khristu. Mutakhulupirira, anakusindikizani chizindikiro pokupatsani Mzimu Woyera amene Iye analonjeza.
Inteka qase tuma qaala hesika intena ashiza mishiracho qaala siydi Kiristosan amanidista. Iza amanidi kase imistana getetida xiilo ayanan atametidista.
14 Mzimu Woyerayo ndi chikole chotsimikizira kuti tidzalandira madalitso athu, ndipo kuti Mulungu anatiwombola kuti tikhale anthu ake. Iye anachita zimenezi kuti timuyamike ndi kumulemekeza.
He ayanazikka iza boncho galatan qoncisana mala Xoossi bees gididayta worsota wozana gakanas nu latas ooythoko.
15 Choncho, kuyambira pamene ndinamva za chikhulupiriro chanu mwa Ambuye Yesu ndi za chikondi chanu pa oyera mtima onse,
Hesa gish inte Goda Yesussa amannida gishine amaniza asa inte siqizaysa ta siyosope ha simin intena qopa qopa ekada tani ta wosan inte gish Xoossas galata shisho agabeyke.
16 ine sindilekeza kuyamika Mulungu chifukwa cha inu. Ndimakukumbukirani mʼmapemphero anga.
17 Ndimapemphera kuti Mulungu wa Ambuye athu Yesu Khristu, Atate a ulemerero akupatseni mzimu wa nzeru ndi wa vumbulutso, kuti mumudziwe kwenikweni.
Boncho aawa gidida nu Goda Yesuss Kiristossa awa Xoossi inte loo7ethi eranamala qonccisiza ayanayinne eratetha ayanay intes imistana mala ta intes paccey baynda wosays.
18 Ndimapempheranso kuti maso a mitima yanu atsekuke ndi cholinga choti mudziwe chiyembekezo chimene Iye anakuyitanirani, chuma cha ulemerero chomwe chili mwa anthu oyera mtima.
Hessathokka inte izan xeygetida ufaysay hessikka amanizayta achan diza iza latisiza duretethay azakone inte erana mala inte wozina ayfey po7ana mala wosays.
19 Ndiponso ndikufuna kuti mudziwe mphamvu zake zazikulu koposa zimene zili mwa ife amene timakhulupirira. Mphamvuyi ndi yofanana ndi mphamvu yoposa ija
Amaniza nunan oothiza wursofe bolla gidida gitta Xoossa wolqa inte erana mala ta wosays. He wolqaykka oonikka teqontayssanne mulekka daburontaysakko.
20 imene inagwira ntchito pamene Mulungu anaukitsa Khristu kwa akufa, namukhazika Iye ku dzanja lake lamanja mʼdziko la kumwamba.
Kirstosa hayqoppe denthidi salon Xoossa ushachan utisiday he wolqakko.
21 Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn g165)
Aysizaytape godatethape woliqafene kawotethappe qaseka ha7i xala gidonta burope yana wodeka gidin sunthu wurisofe izi bollakko. (aiōn g165)
22 Ndipo Mulungu anayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake ndi kumusankha Iyeyo kukhala mutu pa chilichonse chifukwa cha mpingo,
Xoossi hara wursi iza tope garissan harisides. Wossa keeththanka wuriso bolla hu7e histides.
23 umene ndi thupi lake, chidzalo cha Iye amene adzaza chilichonse mu njira iliyonse.
Wossa keethiya kirstossa asatethikko. Kirstosaykka wossa keethaynine awanka wuriso miishi kunthes.

< Aefeso 1 >