< Deuteronomo 27 >

1 Mose ndi akuluakulu a Israeli analamula anthu kuti, “Sungani malamulo onse amene ndikukupatsani lero lino.
و موسی و مشایخ اسرائیل، قوم را امرفرموده، گفتند: «تمامی اوامری را که من امروز به شما امر می‌فرمایم، نگاه دارید.۱
2 Mukawoloka mtsinje wa Yorodani kulowa mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, muyimiritse miyala ingapo ikuluikulu ndi kuyikulungiza.
و درروزی که از اردن به زمینی که یهوه، خدایت، به تومی دهد عبور کنید، برای خود سنگهای بزرگ برپاکرده، آنها را با گچ بمال.۲
3 Mulembepo mawu onse a malamulo amenewa pamene muwoloka kulowa mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, dziko loyenda mkaka ndi uchi, monga momwe Yehova Mulungu wa makolo anu anakulonjezerani.
و بر آنها تمامی کلمات این شریعت را بنویس، هنگامی که عبور نمایی تابه زمینی که یهوه، خدایت، به تو می‌دهد، داخل شوی، زمینی که به شیر و شهد جاری است، چنانکه یهوه خدای پدرانت به تو وعده داده است.۳
4 Ndipo mukawoloka Yorodani muyimike miyala iyi pa Phiri la Ebala monga momwe ndikukulamulirani lero lino ndipo muyikulungize.
و چون از اردن عبور نمودی این سنگها راکه امروز به شما امر می‌فرمایم در کوه عیبال برپاکرده، آنها را با گچ بمال.۴
5 Pamenepo mumange guwa lansembe la miyala la Yehova Mulungu wanu. Musagwiritse ntchito chida chilichonse chachitsulo pa miyalapo.
و در آنجا مذبحی برای یهوه خدایت بنا کن، و مذبح از سنگها باشد و آلت آهنین بر آنها بکار مبر.۵
6 Mumange guwa lansembe la Yehova Mulungu wanu ndi miyala yakutchire ndi kuperekerapo nsembe yopsereza kwa Yehova Mulungu wanu.
مذبح یهوه خدای خودرا از سنگهای ناتراشیده بنا کن، و قربانی های سوختنی برای یهوه خدایت، بر آن بگذران.۶
7 Muperekerepo nsembe zopereka za chiyanjano, muzidye ndi kukondwera pamaso pa Yehova Mulungu wanu.
وذبایح سلامتی ذبح کرده، در آنجا بخور و به حضور یهوه خدایت شادی نما.۷
8 Ndipo pa miyalapo mudzalembepo mawu onse a malamulo ndi malemba akuluakulu.”
و تمامی کلمات این شریعت را بر آن به خط روشن بنویس.»۸
9 Kenaka Mose ndi ansembe, amene ndi Alevi anati kwa Aisraeli onse, “Khalani chete Aisraeli inu ndipo mumvetsere! Tsopano inu ndinu anthu a Yehova Mulungu wanu.
پس موسی و لاویان کهنه تمامی اسرائیل را خطاب کرده، گفتند:۹
10 Muzimvera Yehova Mulungu wanu ndi kutsata malamulo ake ndi malangizo ake omwe ndikukupatsani lero lino.”
«ای اسرائیل خاموش باش و بشنو. امروز قوم یهوه خدایت شدی.۱۰
11 Tsiku lomwelo Mose analamula anthu kuti:
پس آواز یهوه خدایت را بشنو و اوامر وفرایض او را که من امروز به تو امر می‌فرمایم، بجاآر.»۱۱
12 Mukawoloka Yorodani, mafuko awa akayimirire pa Phiri la Gerizimu ndi kudalitsa anthu: Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Yosefe ndi Benjamini.
«چون از اردن عبور کردید، اینان یعنی شمعون و لاوی و یهودا و یساکار و یوسف وبنیامین بر کوه جرزیم بایستند تا قوم را برکت دهند.۱۲
13 Ndipo mafuko awa akayimirire pa Phiri la Ebala ndi kutchula matemberero: Rubeni, Gadi, Aseri, Zebuloni, Dani ndi Nafutali.
و اینان یعنی روبین و جاد و اشیر وزبولون و دان و نفتالی بر کوه عیبال بایستند تانفرین کنند.۱۳
14 Alevi adzayankhula mokweza kwa Aisraeli onse kuti:
و لاویان جمیع مردان اسرائیل رابه آواز بلند خطاب کرده، گویند:۱۴
15 “Ndi wotembereredwa munthu amene asema chifanizo kapena kupanga fano, ndi kuchiyika mobisa, pakuti chimenechi ndi chinthu chodetsedwa pamaso pa Yehova, ntchito za manja a anthu.”
«ملعون باد کسی‌که صورت تراشیده یاریخته شده از صنعت دست کارگر که نزد خداوندمکروه است، بسازد، و مخفی نگاه دارد.» و تمامی قوم در جواب بگویند: «آمین!»۱۵
16 “Ndi wotembereredwa munthu amene sachitira ulemu abambo ake kapena amayi ake.”
«ملعون باد کسی‌که با پدر و مادر خود به خفت رفتار نماید.» و تمامی قوم بگویند: «آمین!»۱۶
17 “Ndi wotembereredwa munthu amene amasuntha mwala wa malire wa mnzake.”
«ملعون باد کسی‌که حد همسایه خود راتغییر دهد.» و تمامی قوم بگویند: «آمین!»۱۷
18 “Ndi wotembereredwa munthu amene amasocheretsa munthu wosaona pa msewu.”
«ملعون باد کسی‌که نابینا را از راه منحرف سازد.» و تمامی قوم بگویند: «آمین!»۱۸
19 “Ndi wotembereredwa munthu amene sachitira chilungamo mlendo, ana amasiye kapena mkazi wamasiye.”
«ملعون باد کسی‌که داوری غریب و یتیم وبیوه را منحرف سازد.» و تمامی قوم بگویند: «آمین!»۱۹
20 “Ndi wotembereredwa munthu amene agonana ndi mkazi wa abambo ake pakuti iye sachitira ulemu pogona pa abambo ake.”
«ملعون باد کسی‌که با زن پدر خود همبسترشود، چونکه دامن پدر خود را کشف نموده است.» و تمامی قوم بگویند: «آمین!»۲۰
21 “Ndi wotembereredwa munthu amene achita chigololo ndi nyama ya mtundu uli wonse.”
«ملعون باد کسی‌که با هر قسم بهایمی بخوابد.» و تمامی قوم بگویند: «آمین!»۲۱
22 “Ndi wotembereredwa munthu amene agonana ndi mlongo wake, mwana wamkazi wa abambo ake kapena mwana wamkazi wa amayi ake.”
«ملعون باد کسی‌که با خواهر خویش چه دختر پدر و چه دختر مادر خویش بخوابد.» وتمامی قوم بگویند: «آمین!»۲۲
23 “Ndi wotembereredwa munthu amene agonana ndi apongozi ake.”
«ملعون باد کسی‌که با مادر‌زن خودبخوابد.» و تمامی قوم بگویند: «آمین!»۲۳
24 “Ndi wotembereredwa munthu amene apha mnzake mwachinsinsi.”
«ملعون باد کسی‌که همسایه خود را درپنهانی بزند.» و تمامی قوم بگویند: «آمین!»۲۴
25 “Ndi wotembereredwa munthu amene alandira chiphuphu kuti aphe munthu wosalakwa.”
«ملعون باد کسی‌که رشوه گیرد تا خون بی‌گناهی ریخته شود.» و تمامی قوم بگویند: «آمین!»۲۵
26 “Ndi wotembereredwa aliyense amene sachita kapena sasunga mawu a malamulo awa.”
«ملعون باد کسی‌که کلمات این شریعت رااثبات ننماید تا آنها را بجا نیاورد.» وتمامی قوم بگویند: «آمین!»۲۶

< Deuteronomo 27 >