< 2 Timoteyo 3 >

1 Koma dziwa izi: Mʼmasiku otsiriza kudzafika nthawi zoopsa kwambiri.
Yi ban k bona kul gbem yogu ba paa hal bocienl.
2 Anthu adzakhala odzikonda, okonda ndalama, odzitama, onyada, achipongwe, osamvera makolo awo, osayamika, wopanda chiyero.
Bi nub ba waan b ba paa, k ba bua elig ciam bi ba duond bi ba yen ki kan cɔoln nul, bi ba sugd o tienu, yen bi go kan cɔoln b danb, bi ba tie mundanb kan cɔln o tienu bona.
3 Adzakhala wopanda chikondi, osakhululuka, osinjirira, osadziletsa, ankhanza, osakonda zabwino,
bi kan muɔ bi ñunŋim yen sugl nub, bi ba tie fagu danb bi kan fid kub bi ba, bi ba tie nkum danb yen bi ka bua boŋanl.
4 opereka anzawo kwa adani awo, osaopa zoyipa, odzitukumula, okonda zowasangalatsa mʼmalo mokonda Mulungu.
Biba tie yaal ki bi buɔ yal, kba waan biba. Biba kuɔr binub, biba buɔ bobiigu cie O tienu.
5 Adzakhala ndi maonekedwe achipembedzo koma mphamvu yake ndi kumayikana. Anthu amenewa uziwapewa.
Ama bkaan fini yaa tie danka mɔni, kelima babuɔ yale tie U tienu Fuoŋaam yaa palo. Da ŋuɔ laa nubi.
6 Iwowa ndi anthu aja amene amayendayenda mʼmakomo a anthu nʼkumanyenga akazi ofowoka mʼmaganizo, olemedwa ndi machimo ndiponso otengeka ndi zilakolako zoyipa zamitundumitundu,
Bitiam baa fidi kuɔ a diena botienni ke ñuun ñɔk bi puo yaab k ka haal yoko.
7 amaphunzira nthawi zonse koma samatha kuzindikira choonadi.
Ya puo n pia ŋanduna buam hal bocienl, ama ba fid bang li mumuni.
8 Monga momwe Yanesi ndi Yambere anawukira Mose, momwemonso anthu amenewa amawukira choonadi. Nzeru zawo ndi zowonongeka ndipo pa za chikhulupiriro, ndi okanidwa.
Nan Jannes yen Jambile n den yiie Moiis maam, lan Jab moko yie e mɔamɔan. Bi tie ya nub ya malm n ki ŋan, bi dandanl moko ki pa a bigna yogunu.
9 Koma sadzapita nazo patali kwambiri zimenezi, pakuti anthu onse adzaona kupusa kwawo monga anachitira Yanesi ndi Yambere.
Bi kaan fidi ya di kca, kelima yua kul baa la bi garem. L den tien o nan ya bomlieb fakodaanpo
10 Tsono iwe, umadziwa zonse zimene ndimaphunzitsa, makhalidwe anga, cholinga changa, chikhulupiriro changa, kuleza mtima kwanga, chikondi changa, ndi kupirira kwanga,
Ama fini, a den tien nania k cɔal n maam, n yeyie nu, n yaan jaga, n ddaan, n junl, n buam, n faala.
11 mazunzo anga, masautso anga, monga zinandichitikira ku Antiokeya, ku Ikoniya ndi ku Lusitra. Ndinazunzika kwambiri. Koma Ambuye anandipulumutsa pa zonsezi.
Fini mɔro a den la binuba dmabni ŋlire yen n den la ya falaa paa Antiyɔsini, Ikoniɔm yen Listri dogoni. N den la ya falaa kuli a n den kobiyen yokuli n Yɔmdaan den faabni.
12 Kunena zoona, munthu aliyense amene akufuna kukhala moyo wolemekeza Mulungu mwa Khristu Yesu, adzazunzikadi,
Moni yab kul tuo ke biba fo yen U tien, yen Yesu Kristi ba la falaa.
13 pomwe anthu oyipa ndi onyenga adzanka nayipirayipira, kunamiza ena, iwo nʼkumanamizidwanso.
Amaa, a nub biada yen atigbadaan yok kuul ba kuɔ li tuolbidini, bina tund kua ti tuondbidini ki buande biba yen biliem.
14 Koma iwe pitiriza zimene waziphunzira ndi kuzivomereza, chifukwa ukudziwa amene anakuphunzitsa zimenezi.
Ama fini ŋam yaakub a den baang yali yen dandal kul len yua kan ka den baango.
15 Kuyambira uli wamngʼono wakhala ukudziwa Malemba Oyera, amene akhoza kukupatsa nzeru zokupulumutsa kudzera mʼchikhulupiriro cha mwa Yesu Khristu.
haal nan a den tie big, a den baang o tienu omaama mɔni, yal ba fid ten yal ŋan ki tien faabu yesu kilisu nni.
16 Malemba onse anawalembetsa ndi Mulungu, ndipo othandiza pophunzitsa, podzudzula, pokonza cholakwika ndi polangiza za chilungamo
Kelma minmɔn kul ñan o tien kan yal ñan ki ba fid tund o nul nni, ki ba fid ki jalgo. Ki ba ŋangd o yen ki ba fid ki paago, o yeyienu ya naani yen o tienu buam ya saanu.
17 kuti munthu wa Mulungu akonzekere bwino lomwe kugwira ntchito iliyonse yabwino.
Lan ba tod otienu nulo wan ya bobd oba cain ki suan tuonl ŋanl kul.

< 2 Timoteyo 3 >